< Zaburi 80 >

1 Kuom jatend wer. E dwol mar “Ondanyo mar Singruok.” Mar Asaf. Zaburi. Chiknwa iti, yaye Jakwadh jo-Israel, in mitelo ne Josef ka kweth mar dhok. In mibet e kom loch e kind kerubi, koro rieny ane
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Kakombo wa Pangano.” Salimo la Asafu. Tcherani khutu Inu mʼbusa wa Israeli, Inu amene mumatsogolera Yosefe monga nkhosa; Inu amene mumakhala pa mpando waufumu pakati pa akerubi, walani
2 e nyim Efraim, gi Benjamin gi Manase. Nyis tekri, kendo bi mondo ireswa.
kwa Efereimu, Benjamini ndi Manase. Utsani mphamvu yanu; bwerani ndi kutipulumutsa.
3 Dwogwa iri, yaye Nyasaye; mi wangʼi orienynwa, eka mondo wayud warruok.
Tibwezereni mwakale Inu Mulungu; nkhope yanu itiwalire kuti tipulumutsidwe.
4 Yaye Jehova Nyasaye, ma Nyasaye Maratego, mirimbi biro siko koyienyo, gi lamo mar jogi nyaka karangʼo?
Inu Mulungu Wamphamvuzonse, mpaka liti mkwiyo wanu udzanyeka kutsutsana ndi mapemphero a anthu anu?
5 Isemiyo gichamo pi wangʼ ka kuon kendo isemiyo gimodho pi wangʼ agwetni modhuro.
Mwawadyetsa buledi wa misozi; mwachitisa iwo kumwa misozi yodzaza mbale.
6 Isemiyo wadoko rachwany ne jobutwa, kendo wasikwa jarowa.
Mwachititsa kuti tikhale gwero la mikangano pakati pa anansi athu, ndipo adani athu akutinyoza.
7 Dwogwa iri, yaye Nyasaye Maratego; mi wangʼi orienynwa, eka mondo wayud warruok.
Tibwezereni mwakale Inu Mulungu Wamphamvuzonse, nkhope yanu itiwalire kuti tipulumutsidwe.
8 Ne igolo mzabibu moro e piny Misri, kendo ne iriembo ogendini mi ipidhe kargi.
Munatulutsa mpesa kuchoka ku Igupto; munathamangitsa anthu a mitundu ina ndi kuwudzala mpesawo.
9 Ne ilosone lowo maber, kendo nochwoyo tiendene piny mi opongʼo piny.
Munawulimira munda wamphesawo, ndipo unamera ndi kudzaza dziko.
10 Tipo Nyasaye noimo gode duto, mana ka yiende sida ma odongo ma bedene olak.
Mapiri anaphimbidwa ndi mthunzi wake, mikungudza yamphamvu ndi nthambi zake.
11 Noyaro bedene madongo nyaka e Nam Mediterania kendo noloth mochweyo nyaka e Aora Yufrate.
Unatambalitsa nthambi zake mpaka ku nyanja, mphukira zake mpaka ku mtsinje.
12 Koro angʼo momiyo isemuko ohinga mage, momiyo ji duto makadho pone ka olemo.
Chifukwa chiyani mwagwetsa makoma ake kuti onse amene akudutsa athyole mphesa zake?
13 Mbithe moa e bungu kethe, kendo le mag bungu chame.
Nguluwe zochokera mʼnkhalango zikuwononga ndipo zirombo za mthengo zimawudya.
14 Duog irwa, yaye Nyasaye Maratego! Ngʼi piny gie polo mondo ine! Ngʼi mzabibu maber,
Bweraninso kwa ife Inu Mulungu Wamphamvuzonse! Yangʼanani pansi muli kumwambako ndipo muone! Uyangʼanireni mpesa umenewu,
15 yien ma lweti ma korachwich ema nopidho gi tiende, ma en wuodi misepidho in iwuon.
muzu umene dzanja lanu lamanja ladzala, mwana amene inu munamukuza nokha.
16 Mzabibu mari osetongʼ mi owangʼ gi mach, jogi lal nono nikech isekwerogi.
Mpesa wanu wadulidwa ndi kutenthedwa ndi moto; pakudzudzula kwanu anthu anu awonongeka.
17 Mad lweti bed kuom ngʼat mobet e bathi korachwich, ma en wuod dhano misemiyo teko in iwuon.
Dzanja lanu likhale pa munthu amene ali ku dzanja lanu lamanja, mwana wa munthu amene mwalera nokha.
18 Eka ok wanachak walokre waweyi; konywa wabed mangima, kendo wabiro pako nyingi.
Ndipo ife sitidzatembenukira kumbali kuchoka kwa Inu; titsitsimutseni ndipo tidzayitana pa dzina lanu.
19 Dwogwa iri, yaye Jehova Nyasaye, ma Nyasaye Maratego; mi wangʼi orienynwa, eka mondo wayud warruok.
Tibwezereni mwakale Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse nkhope yanu itiwalire kuti tipulumutsidwe.

< Zaburi 80 >