< Zaburi 70 >

1 Kuom jatend wer. Kwayo mar Daudi. Ret piyo mondo iresa, yaye Nyasaye; bi piyo mondo ikonya, yaye Jehova Nyasaye.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho. Fulumirani Mulungu kundipulumutsa; Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.
2 Mad joma dwaro ngimana yud wichkuot kendo pachgi lal; mad ji duto ma gombona hinyruok dog kuma giaye ka giyudo achaya.
Iwo amene akufunafuna moyo wanga achititsidwe manyazi ndi kusokonezedwa; onse amene akukhumba chiwonongeko changa abwezedwe mopanda ulemu.
3 Mad joma wachona niya, “Haa! Haa!” Dog kuma giaye ka wichkuot omakogi.
Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,” abwerere chifukwa cha manyazi awo.
4 To mad ji duto madwari bed moil kendo mamor kuomi; mad joma ohero warruok mari osik kawacho niya, “Jehova Nyasaye mondo oyud duongʼ!”
Koma onse amene akufunafuna Inu akondwere ndi kusangalala mwa Inu; iwo amene amakonda chipulumutso chanu nthawi zonse anene kuti, “Mulungu akuzike!”
5 Adhier kendo achando; bi ira piyo, yaye Nyasaye. In e konyruokna kendo jaresna; kik ideki, yaye Jehova Nyasaye.
Koma ine ndine wosauka ndi wosowa; bwerani msanga kwa ine Inu Mulungu. Inu ndinu thandizo langa ndi momboli wanga; Inu Yehova musachedwe.

< Zaburi 70 >