< Zaburi 16 >
1 Miktam mar Daudi. Rita maber, yaye Nyasaye nikech in e kar pondona.
Mikitamu ya Davide. Ndisungeni Inu Mulungu, pakuti ine ndimathawira kwa Inu.
2 Ne awacho ne Jehova Nyasaye niya, “In e Ruodha; onge gima ber machielo ma an-go makmana in.”
Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga; popanda Inu, ine ndilibe chinthu chinanso chabwino.”
3 To jomaler manie piny, to gin kaka joma nigi duongʼ ma ahero gi chunya duto.
Kunena za oyera mtima amene ali pa dziko, amenewa ndi olemekezeka, amene ndimakondwera nawo.
4 Joma lawo nyiseche mamoko kuyo margi biro medore. Misengini magi mag remo ok abi olo oko kendo kata nying-gi ok abi hulo gi dhoga.
Anthu amene amathamangira kwa milungu ina mavuto awo adzachulukadi. Ine sindidzathira nawo nsembe zawo zamagazi kapena kutchula mayina awo ndi pakamwa panga.
5 Jehova Nyasaye, isemiya pok makora kod okombena; iserita maber gi giga duto.
Yehova, Inu mwandipatsa cholowa changa ndi chikho changa; mwateteza kolimba gawo langa.
6 Kiepena duto ochopo kuonde mabeyo; adier, girkeni maga duto moro wangʼ adier.
Malire a malo anga akhala pabwino; ndithudi, ine ndili cholowa chokondweretsa kwambiri.
7 Abiro pako Jehova Nyasaye mangʼadona rieko; kata gotieno chunya puonja.
Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu; ngakhale usiku mtima wanga umandilangiza.
8 Asiko aketo Jehova Nyasaye e nyima ndalo duto. Nikech ka entie e lweta korachwich, to onge gima nyalo yienga.
Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse. Popeza Iyeyo ali kudzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.
9 Emomiyo chunya mor kendo lewa yot; ringra bende biro yweyo gi kwe,
Choncho mtima wanga ndi wosangalala ndipo pakamwa panga pakukondwera; thupi langanso lidzakhala pabwino,
10 nikech ok inijwangʼa ei liel, to bende ok niyie Ngʼati Maler tow. (Sheol )
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol )
11 Isenyisa yor ngima; inipongʼa gi mor mogundho ka an e nyimi, kendo gi mor mosiko e badi korachwich.
Inu mwandidziwitsa njira ya moyo; mudzandidzaza ndi chimwemwe pamaso panu, ndidzasangalala mpaka muyaya pa dzanja lanu lamanja.