< Zaburi 16 >

1 Miktam mar Daudi. Rita maber, yaye Nyasaye nikech in e kar pondona.
Mikitamu ya Davide. Ndisungeni Inu Mulungu, pakuti ine ndimathawira kwa Inu.
2 Ne awacho ne Jehova Nyasaye niya, “In e Ruodha; onge gima ber machielo ma an-go makmana in.”
Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga; popanda Inu, ine ndilibe chinthu chinanso chabwino.”
3 To jomaler manie piny, to gin kaka joma nigi duongʼ ma ahero gi chunya duto.
Kunena za oyera mtima amene ali pa dziko, amenewa ndi olemekezeka, amene ndimakondwera nawo.
4 Joma lawo nyiseche mamoko kuyo margi biro medore. Misengini magi mag remo ok abi olo oko kendo kata nying-gi ok abi hulo gi dhoga.
Anthu amene amathamangira kwa milungu ina mavuto awo adzachulukadi. Ine sindidzathira nawo nsembe zawo zamagazi kapena kutchula mayina awo ndi pakamwa panga.
5 Jehova Nyasaye, isemiya pok makora kod okombena; iserita maber gi giga duto.
Yehova, Inu mwandipatsa cholowa changa ndi chikho changa; mwateteza kolimba gawo langa.
6 Kiepena duto ochopo kuonde mabeyo; adier, girkeni maga duto moro wangʼ adier.
Malire a malo anga akhala pabwino; ndithudi, ine ndili cholowa chokondweretsa kwambiri.
7 Abiro pako Jehova Nyasaye mangʼadona rieko; kata gotieno chunya puonja.
Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu; ngakhale usiku mtima wanga umandilangiza.
8 Asiko aketo Jehova Nyasaye e nyima ndalo duto. Nikech ka entie e lweta korachwich, to onge gima nyalo yienga.
Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse. Popeza Iyeyo ali kudzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.
9 Emomiyo chunya mor kendo lewa yot; ringra bende biro yweyo gi kwe,
Choncho mtima wanga ndi wosangalala ndipo pakamwa panga pakukondwera; thupi langanso lidzakhala pabwino,
10 nikech ok inijwangʼa ei liel, to bende ok niyie Ngʼati Maler tow. (Sheol h7585)
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol h7585)
11 Isenyisa yor ngima; inipongʼa gi mor mogundho ka an e nyimi, kendo gi mor mosiko e badi korachwich.
Inu mwandidziwitsa njira ya moyo; mudzandidzaza ndi chimwemwe pamaso panu, ndidzasangalala mpaka muyaya pa dzanja lanu lamanja.

< Zaburi 16 >