< Ngeche 9 >

1 Rieko osegero ode, osechungo sirnige abiriyo.
Nzeru inamanga nyumba yake; inayimika nsanamira zake zisanu ndi ziwiri.
2 Oseiko ringe kendo oloso divai mare moru mamit, bende osepedho mesa mare.
Inapha ziweto zake ndipo yasakaniza vinyo wake; inasakaniza vinyo wake ndi kuyala tebulo lake.
3 Oseoro jotichne ma nyiri, kendo oluongo ji ka en kuonde motingʼore e dala maduongʼ.
Nzeruyo inatuma adzakazi ake, kuti akakhale pamwamba penipeni pa mzinda ndi kukalengeza kuti,
4 “Weuru ji duto mangʼeyogi tin obi kae!” Owacho ni jogo maonge gi rieko mar ngʼado bura.
“Aliyense amene ali munthu wamba, abwere kuno!” Kwa onse opanda nzeru inkanena kuti,
5 Biuru, chamuru chiemba kendo madhuru divai ma aseruwo.
“Bwerani, dzadyeni chakudya changa ndipo dzamweni vinyo amene ndakonza.
6 Weuru yoreu maonge rieko, eka unubed mangima, wuothuru e yor winjo kod ngʼeyo.
Lekani zopusa zanu kuti mukhale ndi moyo; yendani njira ya nzeru yomvetsa zinthu.”
7 Ngʼat marieyo ja-ajara luongo mana wichkuot, ngʼat makwero ngʼat marach yudo mana ayany.
Aliyense amene amayesa kukonza munthu wonyoza amadziputira minyozo; aliyense amene amadzudzula munthu woyipa amadetsa mbiri yake.
8 Kik ikwer ngʼat ma jaro ji, nikech mano biro miyo obedo mamon kodi, kirieyo ngʼat mariek, to obiro heri.
Usadzudzule munthu wonyoza kuti angadzadane nawe; dzudzula munthu wanzeru ndipo adzakukonda.
9 Puonj ngʼat mariek, to obiro bedo mariek moloyo, puonj ngʼat makare gimoro, to obiro medo puonjore.
Ukalangiza munthu wanzeru ndiye adzapitirira kukhala wanzeru; ukaphunzitsa munthu wolungama ndiye adzawonjezera kuphunzira kwake.
10 Luoro Jehova Nyasaye e chakruok mar rieko, to ngʼeyo Jal Maler miyo ngʼato ngʼeyo tiend wach.
Kuopa Yehova ndiye chiyambi cha nzeru; kudziwa Woyerayo ndiko kukhala womvetsa bwino zinthu.
11 Nimar kuoma ndalogi biro bedo mangʼeny, kendo rieko biro medo hiki.
Chifukwa cha ine nzeru, masiku ako adzachuluka, ndipo zaka za moyo wako zidzawonjezeredwa.
12 Ka iriek, riekoni nomiyi ohala, ka ijajaro, to in iwuon ema ibiro hinyori.
Ngati ndiwe wanzeru, nzeru yakoyo idzakupindulitsa; ngati ndiwe wonyoza ena, udzavutika wekha.
13 Dhako mofuwo en jakoko, ok oritore kendo ngʼeyone tin.
Uchitsiru ndi mkazi waphokoso, wopulikira ndiponso wosadziwa zinthu.
14 Obedo e dhoode, e kom kama otingʼore mar dala maduongʼ,
Iye amakhala pa mpando, pa khomo la nyumba yake, pamalo aatali a mu mzinda,
15 koluongo jogo makadho, madhi e yoregi.
kuti aziyitana anthu ongodutsa, amene akunka nayenda njira zawo.
16 Owacho ni jogo maonge gi rieko mar ngʼado bura niya, “Weuru ji duto mangʼeyogi tin obi kae!”
Amati, “Onse amene ndi anthu wamba abwere kuno,” ndipo kwa wopanda nzeru amati,
17 Nomedo wachonegi niya, “Pi mokwal mit, chiemo michamo apanda ema nigi ndhandhu moloyo!”
“Madzi akuba ndiye amatsekemera; chakudya chodya mobisa ndi chokoma!”
18 To ok gingʼeyo kata matin ni joma otho ni kuno; bende ni joma lime ni e liel matut. (Sheol h7585)
Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol h7585)

< Ngeche 9 >