< Ngeche 28 >

1 Jaricho ringo kaonge ngʼama lawe, to joma kare jochir ka sibuor.
Munthu woyipa amathawa ngakhale palibe wina womuthamangitsa, koma wolungama ndi wolimba mtima ngati mkango.
2 Ka piny toke tek, to en gi jotelo mangʼeny, to ngʼat mawinjo wach kendo man-gi ngʼeyo rito chik.
Pamene mʼdziko muli kuwukirana, dzikolo limakhala ndi olamulira ambiri, koma anthu omvetsa ndi odziwa zinthu bwino ndiwo angakhazikitse bata mʼdzikolo nthawi yayitali.
3 Jatelo mahinyo jochan chalo kaka kodh oula maywero cham oko.
Munthu wosauka amene amapondereza osauka anzake ali ngati mvula yamkuntho imene imawononga mbewu mʼmunda.
4 Jogo ma ok rit chik pako ngʼat marach, to jogo marito chik dagi jogo maricho.
Amene amakana malamulo amatamanda anthu oyipa, koma amene amasunga malamulo amatsutsana nawo.
5 Jomaricho ok ongʼeyo adiera, to jogo madwaro Jehova Nyasaye ongʼeyo adiera chutho.
Anthu oyipa samvetsa za chiweruzo cholungama, koma amene amafuna kuchita zimene Yehova afuna amachimvetsetsa bwino.
6 Ber ngʼat ma jachan ma wuodhe ok cha, moloyo ngʼat ma ja-mwandu ma yorene richo.
Munthu wosauka wa makhalidwe abwino aposa munthu wolemera wa makhalidwe okhotakhota.
7 Ngʼat marito chik en wuowi mariek, to bedo osiep jawuoro kelo wichkuot ne wuon mare.
Amene amasunga malamulo ndi mwana wozindikira zinthu, koma amene amayenda ndi anthu adyera amachititsa manyazi abambo ake.
8 Ngʼat mamedo mwandu gi ohala ma malangʼ choko mwandu ne ngʼat machielo, mabiro bedo mangʼwon gi jochan.
Amene amachulukitsa chuma chake polandira chiwongoladzanja chochuluka amakundikira chumacho anthu ena, amene adzachitira chifundo anthu osauka.
9 Ka ngʼato odino ite ne chik, kata mana lemone bende richo.
Wokana kumvera malamulo ngakhale pemphero lake lomwe limamunyansa Yehova.
10 Ngʼat matero ngʼat moriere tir e yo mar richo biro podho e obetone owuon, to ngʼat ma ok cha biro yudo pok maber.
Amene amatsogolera anthu olungama kuti ayende mʼnjira yoyipa adzagwera mu msampha wake womwe, koma anthu opanda cholakwa adzalandira cholowa chabwino.
11 Jamoko nyalo paro owuon ni oriek, to jachan man-gi paro matut neno gik manie chuny jamokono.
Munthu wolemera amadziyesa kuti ndi wanzeru, koma munthu wosauka amene ali ndi nzeru zodziwa zinthu amamutulukira.
12 Ka ngʼat makare oloyo, nitie mor maduongʼ, to ka ngʼat marach omi teko mondo otel, ji ringo dhiyo kar pondo.
Pamene olungama apambana pamakhala chikondwerero chachikulu; koma pamene anthu oyipa apatsidwa ulamuliro, anthu amabisala.
13 Ngʼat mapando richone ok dhi maber, to ngʼat ma hulo richone kendo oweyogi yudo ngʼwono.
Wobisa machimo ake sadzaona mwayi, koma aliyense amene awulula ndi kuleka machimowo, adzalandira chifundo.
14 En ngʼama ogwedhi ngʼat moluoro Jehova Nyasaye kinde duto, to ngʼatno ma chunye tek donjo e chandruok.
Ndi wodala munthu amene amaopa Yehova nthawi zonse, koma amene aumitsa mtima wake adzagwa mʼmavuto.
15 Kaka sibuor maruto kata ondiek madwaro kecho e kaka ngʼat marach motelone joma ok nyal.
Ngati mkango wobuma kapena chimbalangondo cholusa ndi mmenenso amakhalira munthu woyipa akamalamulira anthu osauka.
16 Ruoth ma jasunga onge gi rieko, to ngʼatno mamon gi gik moyud e yo marach biro dak amingʼa.
Wolamulira amene samvetsa zinthu ndiye amakhala wankhanza koma amene amadana ndi phindu lopeza mwachinyengo adzakhala ndi moyo wautali.
17 Ngʼat moneko chunye chandore enobed gi kuyo nyaka otho; omiyo kik ngʼato konye.
Munthu amene wapalamula mlandu wopha munthu adzakhala wothawathawa mpaka imfa yake; wina aliyense asamuthandize.
18 Ngʼatno ma ja-adiera ibiro rito maonge hinyruok, to ngʼatno ma yorene richo biro podho apoya nono.
Amene amayenda mokhulupirika adzapulumutsidwa koma amene njira zake ndi zokhotakhota adzagwa mʼdzenje.
19 Ngʼat matiyo e puothe biro bedo gi chiemo mogundho, to ngʼat mabayo abaya biro bedo jachan mochwere.
Amene amalima mʼmunda mwake adzakhala ndi chakudya chochuluka, koma amene amangosewera adzakhala mʼmphawi.
20 Ngʼat ma ja-adiera ibiro gwedho mangʼeny, to ngʼat madwaro gi teko bedo ja-mwandu ok notony ma ok okume.
Munthu wokhulupirika adzadalitsika kwambiri, koma wofuna kulemera mofulumira adzalangidwa.
21 Dok ne ngʼato kayiem ka oketho ok ber, to ngʼato biro timo marach mana ni mondo oyud asoya matin.
Kukondera si kwabwino, ena amachita zolakwazo chifukwa cha kachidutswa ka buledi.
22 Ngʼat ma iye lit dwaro ahinya ni mondo obed gi mwandu to ok ongʼeyo ni chan orite.
Munthu wowumira amafunitsitsa kulemera koma sazindikira kuti umphawi udzamugwera.
23 Ngʼatno makwero ngʼato gikone obiro yudo pwoch mangʼeny moloyo ngʼatno man-gi lep mawuondo.
Amene amadzudzula mnzake potsiriza pake mnzakeyo adzamukonda kwambiri, kupambana amene amanena mawu oshashalika.
24 Ngʼat mamayo wuon mare kata min, to owacho niya, “Timo kamano ok rach,” ochal gi ngʼat maketho gimoro.
Amene amabera abambo ake kapena amayi ake namanena kuti “kumeneko sikulakwa,” ndi mnzake wa munthu amene amasakaza.
25 Ngʼat ma jawuoro thoro kelo miero, to ngʼat mogeno kuom Jehova Nyasaye biro dhiyo maber.
Munthu wadyera amayambitsa mikangano, koma amene amadalira Yehova adzalemera.
26 Ngʼat moketo genone kuome owuon ofuwo, to ngʼatno mawuotho e rieko, oritore maonge hinyruok.
Amene amadzidalira yekha ndi chitsiru, koma amene amatsata nzeru za ena adzapulumuka.
27 Ngʼat mamiyo jochan ok nochand gimoro, to ngʼat ma gengʼo wangʼe ne jochan noyud kwongʼ mangʼeny.
Amene amapereka kwa osauka sadzasowa kanthu, koma amene amatsinzina maso ake adzatembereredwa kwambiri.
28 Ka jaricho oketi e teko mondo otel, ji dhiyo kar pondo; to ka jaricho otho joma kare dhiyo nyime.
Pamene anthu oyipa apatsidwa ulamuliro anthu amabisala, koma anthu oyipa akawonongeka olungama amapeza bwino.

< Ngeche 28 >