< Ngeche 27 >
1 Kik isungri kuom kiny, nikech ok ingʼeyo gima odiechiengʼ nyalo kelo.
Usamanyadire za mawa, pakuti sudziwa zimene zidzachitike pa tsikulo.
2 We ngʼat moro ema opaki, to ok dhogi iwuon; ngʼato machielo, to ok lewi iwuon.
Munthu wina akutamande, koma osati wekha; mlendo akakutamanda, ndiponi koma osati ndi pakamwa pako.
3 Kidi pek to kuoyo bende pek, to chandruok ma ngʼat mofuwo kelo pek moloyo gik moko ariyogo.
Mwala ndi wolemera ndipo mchenganso ndi wolemera kwambiri, koma makani a chitsiru ndi oposa zonsezo kulemera kwake.
4 Mirima kwiny to gero pek moloyo, to en ngʼa manyalo chomore gi nyiego?
Mkwiyo umadzetsa nkhanza ndipo kupsa mtima kumachititsa zoopsa. Koma nsanje imachita zoopsa zopambana.
5 Kwero ngʼato ratiro ber moloyo hera mopandi.
Kudzudzula munthu poyera nʼkwabwino kuposa chikondi chobisika.
6 Adhonde moa kuom osiep inyalo geno, to jasigu medo mana nyoth mar masira.
Munthu amene amakukonda ngakhale akupweteke zili bwino, koma mdani wako amakupsompsona mwachinyengo.
7 Ngʼat moyiengʼ ok dwar mor kich, to ngʼatno modenyo kata mana gima kech mitne.
Iye amene wakhuta amayipidwa ndi chisa cha uchi, koma kwa munthu wanjala ngakhale chimene chili chowawa chimamukomera.
8 Mana kaka winyo mabayo moa e ode e kaka ngʼatno mabayo aa e dalane.
Munthu amene wasochera ku nyumba kwake, ali monga mbalame imene yasochera pa chisa chake.
9 Moo mangʼwe ngʼar gi ubani kelo mor ne chuny, to ber mar osiep ngʼato wuok kuom ngʼado rieko gi adiera.
Mafuta ndi zonunkhira zimasangalatsa mtima, ndipo kukoma mtima kwa bwenzi kwagona pa malangizo ake.
10 Kik ijwangʼ osiepni kod osiep wuonu, to kik idhi e od owadu ka chandruok omaki, ber dhi ir jabuti machiegni moloyo owadu man mabor.
Usasiye bwenzi lako ndiponso bwenzi la abambo ako, ndipo usapite ku nyumba ya mʼbale wako pamene wakumana ndi mavuto; mnzako wokhala naye pafupi amaposa mʼbale wako wokhala kutali.
11 Bed mariek, wuoda kendo imi chunya mor eka anyalo dwoko ngʼato moro amora machaya.
Mwana wanga, khala wanzeru, ndipo ukondweretse mtima wanga; pamenepo ine ndidzatha kuyankha aliyense amene amandinyoza.
12 Ngʼat mariek neno masira kabiro kendo opondo, to ngʼat mofuwo dhiyo adhiya nyime ma ohinyre.
Munthu wochenjera akaona choopsa amabisala, koma munthu wopusa amangopitirira ndipo amakumana ndi mavuto.
13 Kaw law ngʼatno mochungʼne ngʼat mokia kaka singo; kawe ka okete singo kar dhako mabayo.
Utenge chovala cha munthu amene waperekera mlendo chikole; ngati chigwiriro chifukwa waperekera chikole mlendo wosadziwika.
14 Ka ngʼato ogwedho jabute e lela gokinyi mangʼich, to ochalo mana gi ngʼama kwongʼe.
Ngati munthu apatsa mnzake moni mofuwula mmamawa kwambiri, anthu adzamuyesa kuti akutemberera.
15 Dhako ma jakoko chalo gi kodh ajiki,
Mkazi wolongolola ali ngati mvula yamvumbi.
16 kwerogo chalo gi gengʼo yamo kata mako moo gi lwedo.
Kumuletsa mkazi wotereyu zimenezi zili ngati kuletsa mphepo kapena kufumbata mafuta mʼdzanja.
17 Kaka nyinyo piago nyinyo, e kaka ngʼato piago nyawadgi.
Chitsulo chimanoledwa ndi chitsulo chinzake, chomwechonso munthu amanoledwa ndi munthu mnzake.
18 Ngʼat mopidho ngʼowu biro chamo olembe, to ngʼatno marito ruodhe ibiro miyo luor.
Amene amasamalira mtengo wamkuyu adzadya zipatso zake, ndipo iye amene amasamalira mbuye wake adzalandira ulemu.
19 Kirango pi, to wangʼi iwuon ema ineno, kendo kinono chunyi, to in iwuon ema inenori.
Monga momwe nkhope imaonekera mʼmadzi, chomwechonso mtima wa munthu umadziwika ndi ntchito zake.
20 Tho kod kethruok ok rom ngangʼ, to kata mana wenge dhano bende ok rom. (Sheol )
Manda sakhuta, nawonso maso a munthu sakhuta. (Sheol )
21 Dhahabu gi fedha itemo gi mach, to dhano itemo gi pak moyudo.
Siliva amasungunulira mu uvuni ndipo golide mʼngʼanjo, chomwechonso munthu amadziwika ndi zomwe akudzitamandira nazo.
22 Kata bed ni iyoko ngʼat mofuwo e pany, iyoke kaka cham miswago, ok inigol fupe oa kuome.
Ngakhale utakonola chitsiru mu mtondo ndi musi ngati chimanga, uchitsiru wakewo sudzachoka.
23 Bed ni ingʼeyo maber kaka jambi chalo; bende rit maber kwethgi;
Uzidziwe bwino nkhosa zako momwe zilili. Kodi usamalire bwino ziweto zako?
24 nimar mwandu ok sik mochwere, to osimbo mar loch ok nobed ne tiengʼ ka tiengʼ.
Paja chuma sichikhala mpaka muyaya, ndipo ufumu sukhala mpaka mibado yonse.
25 Ka ongʼad lum oko eka manyien twi, to ka ichoko ne jambi lum manie kor got,
Pamene udzu watha, msipu nʼkumera; ndipo atatuta udzu wa ku mapiri,
26 eka iniyud yie rombe milosgo lewni, kendo iningʼiew lowo gi pesa miyudo kuom diek.
ana ankhosa adzakupatsani chovala ndipo pogulitsa mbuzi mudzapeza ndalama yogulira munda.
27 Ibiro bedo gi chak mangʼeny mar diek ma ibiro pidhorigo gi joodi kendo pidho nyiri matiyoni.
Mudzakhala ndi mkaka wambuzi wambiri kuti muzidya inuyo ndi banja lanu ndi kudyetsa antchito anu aakazi.