< Nehemia 2 >

1 E dwe mar Nisan e higa mar piero ariyo mar loch Ruoth Artaksases, kane okelne divai, ne akawo divai mi amiyo ruoth. Ne pok abedo ka an gi kuyo e nyime nyaka nene;
Pa mwezi wa Nisani, mʼchaka cha makumi awiri cha ufumu wa Aritasasita, atabwera ndi vinyo pamaso pa mfumu ine ndinatenga vinyoyo ndi kupereka kwa mfumu. Koma ndinali ndisanakhalepo ndi nkhope yachisoni pamaso pake.
2 omiyo ruoth nopenja niya, “Ere gima omiyo ikuyo to ok ituo? Ma ok en kuyo akuya makmana ni en mar chuny.” Ne aluor ahinya,
Tsono mfumu inandifunsa kuti, “Nʼchifukwa chiyani nkhope yako ikuoneka yachisoni pamene iwe sukudwala? Ichi si chinthu china koma chisoni cha mu mtima.” Ine ndinachita mantha kwambiri.
3 makmana ne awachone ruoth niya, “Mad ruoth dag amingʼa! Dabed gi mor nade ka dala maduongʼ mane kwerena oyikie omukore, kendo dhorangeyene osewangʼ gi mach.”
Ndinawuza mfumu kuti, “Mfumu ikhale ndi moyo wamuyaya! Kodi nkhope yanga ilekerenji kuoneka yachisoni pamene mzinda umene kuli manda a makolo anga, wasanduka bwinja ndipo zipata zake zinawonongedwa ndi moto?”
4 Ruoth nowachona niya, “En angʼo midwaro?” Bangʼe to ne alamo Nyasach Polo,
Apo mfumu inandifunsa kuti, “Tsono ukufuna kundipempha chiyani?” Ndipo ine ndinapemphera kwa Mulungu Wakumwamba.
5 mi adwoko ruoth niya, “Ka berne ruoth kendo ka jatichni oyudo ngʼwono e wangʼe, to ber mondo oora e dala maduongʼ man Juda kama kwerena oikie mondo agere kendo.”
Ndipo ndinayankha kuti, “Ngati amfumu chingakukondweretseni, ngati mungakomere mtima mtumiki wanune, mundilole kuti ndipite ku Yuda, ku mzinda kumene kuli manda a makolo anga kuti ndikawumangenso.”
6 Eka ruoth, kaachiel gi mikache kobedo bathe nopenja niya, “Wuodhino biro kawo thuolo maromo nade, to ibiro duogo karangʼo?” Ne berne ruoth mondo oora; omiyo ne achiwo odiechiengʼ monego awuogie.
Tsono mfumu, mfumukazi itakhala pambali pake, anandifunsa kuti, “Kodi kumeneko ukakhalako masiku angati ndipo udzabwera liti?” Ndinayiwuza mfumu nthawi yake ndipo inandilola kuti ndipite.
7 Bende ne awachone niya, “Ka berne ruoth, to mad miya barupe mondo aterne jotelo man loka aora Yufrate, mondo omi gibi gimiya rit makare nyaka achopi Juda?
Ndipo ndinatinso kwa mfumu, “Ngati zikondweretse mfumu, mundipatse makalata oti ndikapereke kwa abwanamkubwa a ku chigawo cha Patsidya pa Yufurate, kuti akandilole kudutsa mwamtendere mpaka nditakafika ku Yuda.
8 Kendo mad imiya baruwa ma aterone Asaf, ma jarit yiend bunge magi, mondo obi omiya sirni migerogo dhoranga dala maduongʼ mochomore gi hekalu kendo alosgo ohinga mar dala kod ot mabiro dakie?” To nikech lwet Nyasacha ma jangʼwono ne ni koda, ruoth noyie gi kwayona duto.
Mundipatsenso kalata yokapereka kwa Asafu woyangʼanira nkhalango ya mfumu, kuti akandipatse mitengo yokapangira mitanda ya zipata za nsanja yoteteza Nyumba ya Mulungu, mitanda ya khoma la mzinda ndi ya nyumba yokhalamo ine.” Mfumu indipatse zomwe ndinapempha popeza Yehova wokoma mtima anali nane.
9 Omiyo ne adhi ir jotelo man loka aora Yufrate mi amiyogi barupe ruoth. Ruoth noora gi jotend jolweny kod jolweny makedo koidho farese.
Choncho ndinanyamuka ulendo wanga ndipo ndinafika kwa abwanamkubwa a chigawo cha Patsidya pa Yufurate ndipo ndinawapatsa makalata a mfumu. Mfumu nʼkuti itatumiza akulu ankhondo ndi okwera pa akavalo kuti atsagane nane.
10 Kane Sanbalat ma ja-Horon kod Tobia ja-Amon ma jatelo nowinjo ma, negibedo kod achiedh-nade ahinya ni ngʼato osebiro madwaro kelo dongruok ni jo-Israel.
Sanibalati wa ku Horoni ndi Tobiya wa ku Amoni atamva zimenezi, iwo anayipidwa kwambiri kuti wina wabwera kudzachitira zabwino Aisraeli.
11 Ne adhi Jerusalem, kendo bangʼ kane asetieko ndalo adek kanyo,
Ndinafika ku Yerusalemu, ndipo ndinakhala kumeneko masiku atatu.
12 ne awuok gotieno kod jomoko manok. Ne pod ok anyiso ngʼato angʼata gima Nyasacha noketo e chunya mondo atimne Jerusalem. Ne onge kweth mag farese mane an godo makmana mano mane aidho.
Sindinawuze munthu aliyense za zimene Yehova anayika mu mtima mwanga kuti ndichitire mzinda wa Yerusalemu. Choncho ndinanyamuka usiku pamodzi ndi anthu ena owerengeka. Ndinalibe bulu wina aliyense kupatula amene ndinakwerapo.
13 Kane ochopo otieno ne adhi kaluwo Dhoranga Holo kochiko Soko mar Thuol kod Dhoranga Owuoyo, ka anono ohingni mag Jerusalem, mane osegore piny, kod dhorangeyigi mane osewangʼ gi mach.
Ndinatuluka usiku podzera ku Chipata cha ku Chigwa ndi kuyenda kupita ku Chitsime cha Chirombo Chamʼmadzi mpaka ku Chipata cha Zinyalala. Ndinayangʼana makoma a Yerusalemu, amene anagwetsedwa, ndi zipata zake, zimene zinawonongedwa ndi moto.
14 Bangʼe ne adhi nyime nyaka e Dhoranga Thidhia kod Dago mar Ruoth, makmana ne onge thuolo kama farasa ne nyalo kadhogo;
Kenaka ndinapita ku Chipata cha Kasupe ndi ku Dziwe la Mfumu. Koma panalibe malo okwanira akuti bulu wanga adutse.
15 omiyo nadhi nyaka e holo gotieno, kanono ohinga. Mogik, ne alokora mi achako adonjo kendo gie Dhoranga Holo.
Kotero usikuwo ndinapita ku chigwa, ndikuyangʼana khomalo. Pomaliza ndinabwerera ndi kukalowanso mu mzinda kudzera ku Chipata cha ku Chigwa.
16 Jotelo ne ok ongʼeyo kuma ne adhiyoe, kata gima ne atimo, nikech ne pod ok awacho gimoro ne jo-Yahudi kata jodolo kata joka ruoth kata jotelo kata joma moko mane biro tiyo tijno.
Akuluakulu sanadziwe kumene ndinapita kapena zimene ndimachita, chifukwa pa nthawiyi nʼkuti ndisananene kalikonse kwa Ayuda kapena ansembe, anthu olemekezeka kapena akuluakulu, kapena wina aliyense amene anali woyenera kugwira ntchitoyi.
17 Bangʼe ne awachonegi niya, “Uneno thagruok ma wantiere godo: Jerusalem osemuki, to dhorangeyege osewangʼ gi mach. Biuru wager ohinga mar Jerusalem kendo, to ok wanachak wabed e wichkuot kendo.”
Ndinawawuza kuti, “Inu mukuona mavuto amene tili nawo. Mukuona kuti mzinda wa Yerusalemu wasanduka bwinja ndipo zipata zake zatenthedwa ndi moto. Tsono tiyeni timangenso makoma a Yerusalemu ndipo sitidzachitanso manyazi.”
18 Ne akonegi bende kuom Nyasacha ma jangʼwono mane ni koda kod gima ruoth nowachona. Ne gidwoka niya, “Wachakuru gedo kendo.” Omiyo negichako tich maberni.
Ndinawawuza za mmene Yehova Mulungu wanga anandichitira zabwino ndiponso mawu amene mfumu inandiwuza. Tsono anati, “Tiyeni tiyambenso kumanga.” Kotero analimbitsana mtima kuti ayambenso ntchito yabwinoyi.
19 To ka Sanbalat ma ja-Horon, Tobia ma jatend jo-Amon kod Geshem ma ja-Arabu nowinjo wach gedoni, ne gijarowa kendo buonowa ka gipenjo niya, “Angʼo ma utimoni? Dibed ni ungʼanyo ne ruoth?”
Koma Sanibalati wa ku Horoni, Tobiya wa ku Amoni ndi Gesemu Mwarabu atamva zimenezi, anatiseka ndi kutinyoza. Iwo anafunsa kuti, “Kodi muti ndi chiyani chimene mukuchitachi? Kodi mufuna kuwukira mfumu?”
20 Ne adwokogi niya, “Nyasach polo biro miyowa loch. Wan jotichne wabiro gedo kendo, makmana un, to uonge gi pok e Jerusalem kata dwaro moro amora kata rapar moro amora kuome.”
Koma ndinawayankha kuti, “Mulungu Wakumwamba atithandiza kuti zinthu zitiyendere bwino. Ife antchito ake tiyambapo kumanga. Koma inu mulibe gawo lanu muno mu Yerusalemu. Mulibe chokuyenerezani kulandira malo ano. Mulibenso chilichonse muno chokumbutsa za inu.”

< Nehemia 2 >