< Jona 2 >

1 Kane Jona ne ni ei rech, nolamo Jehova Nyasaye.
Yona ali mʼmimba mwa chinsomba chija anapemphera kwa Yehova Mulungu wake.
2 Nowacho niya, “Ei masichena naluongo Jehova Nyasaye kendo nodwoka. Ei bur matut ne aywak mondo ikonya mane iwinjo ywakna. (Sheol h7585)
Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. (Sheol h7585)
3 Niluta kuma tut mar nam, nyaka kama tutne ogikie piny, mi ataro noketa diere; kendo apaka kod ahiti madongo duto nokadho kuoma.
Munandiponya mʼnyanja yozama, mʼkati mwenimweni mwa nyanja, ndipo madzi oyenda anandizungulira; mafunde anu onse ndi mkokomo wake zinandimiza.
4 Ne awacho ni, ‘Oseriemba e wangʼi; to kata kamano, pod abiro siko ka angʼiyo hekalu mari maler.’
Ndinati, ‘Ine ndachotsedwa pamaso panu; komabe ndidzayangʼananso ku Nyumba yanu yopatulika.’
5 Pi mane olwora nobwoga kendo kude mag nam bende noima kendo buya mag nam nogajore e wiya.
Madzi wondimiza anandichititsa mantha, nyanja yozama inandizungulira; udzu wa mʼmadzi zinakuta mutu wanga.
6 Nalutora nyaka e tiend gode mag nam kendo piny nouma chuth nyaka chiengʼ. To nigola oko kangima e bur matut, yaye Jehova Nyasaye, ma Nyasacha.
Ndinatsikira kunsi ndithu, mʼtsinde mwa mapiri; mipiringidzo ya dziko inanditsekereza kosatha. Koma Inu munatulutsa moyo wanga mʼmandamo, Inu Yehova Mulungu wanga.
7 “Ka chunya ne dwaro aa ne apari Jehova Nyasaye, kendo lemona nochopo nyaka e hekalu mari maler.
“Pamene moyo wanga umachoka mwa ine, ine ndinakumbukira Inu Yehova, ndipo pemphero langa linafika kwa inu, ku Nyumba yanu yopatulika.
8 “Joma otwere kalamo nyiseche manono, jwangʼo ngʼwono mado bedo margi.
“Iwo amene amagwiritsitsa mafano achabechabe amataya chisomo chawo.
9 An to napaki kod wend goyo erokamano mi natimni misango. Gima asesingora nachop kare nikech warruok wuok kuom Jehova Nyasaye.”
Koma ine ndidzapereka kwa Inu nsembe ndikuyimba nyimbo yamayamiko. Chimene ndinalonjeza ndidzachikwaniritsa. Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.”
10 Kendo Jehova Nyasaye nowuoyo gi rech mi rechno nongʼogo Jona oko e dho wath kama otwo.
Ndipo Yehova analamula chinsomba chija, ndipo chinakamusanza Yonayo mʼmbali mwa nyanja.

< Jona 2 >