< Ayub 7 >

1 “Donge dhano nigi tich matek e piny? Donge ndalone chalo gi ndalo mag ngʼat mondiki kuom kinde machwok?
“Kodi munthu sakhala ndi ntchito yowawa pa dziko lapansi? Kodi masiku ake sali ngati munthu waganyu?
2 Mana kaka misumba ma gombo ni seche mag odhiambo ochop piyo, kata ka ngʼama ondiki marito chudo mare gi geno,
Monga ngati kapolo wolakalaka mthunzi wa nthawi yamadzulo, kapena ngati munthu waganyu woyembekezera malipiro ake,
3 e kaka an bende osemiya dweche maonge ohala kod otieno mopongʼ gi chandruok.
choncho ine ndapatsidwa nthawi yongovutika pachabe, ndiponso usiku wamasautso wapatsidwa kwa ine.
4 Ka adhi nindo to piny ok runa piyo kendo aparora ni abiro aa malo sa adi? Piny budhona kapok oru, kendo apuodora koni gi koni nyaka okinyi.
Ndikamagona ndimaganiza kuti, ‘Kodi kucha liti?’ Usikuwo umatalika ndipo sindigona tulo mpaka mmawa.
5 Denda kute gi adhonde opongʼo, pien denda mbala omako kendo chwer tutu.
Thupi langa ladzala mphutsi ndi zipsera, khungu langa langʼambika ndipo likutuluka mafinya.
6 “Ndalo mar ngimana dhiyo mapiyo moloyo masind jachwe usi, kendo orumo piyo maonge geno.
“Masiku anga ndi othamanga kupambana makina wolukira nsalu, ndipo amatha wopanda chiyembekezo.
7 Yaye Nyasaye, parie kaka ngimana en mana muya nono; wengena ok nochak one mor kendo.
Inu Mulungu kumbukirani kuti moyo wanga uli ngati mpweya; sindidzaonanso masiku achisangalalo.
8 Wenge makoro nena sani ok nochak onena kendo, gibiro dwara to ok gininena.
Amene akundiona tsopano akundiona; mudzandifunafuna koma sindidzapezekanso.
9 Mana kaka bor polo rumo mi lal nono, e kaka ngʼat miyiko e liel ok duogi. (Sheol h7585)
Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu amene walowa mʼmanda sabwerera. (Sheol h7585)
10 Ok nodwogi e ode kendo; kar dakne ok nongʼeye kendo.
Iye sadzabweranso ku nyumba kwake ndipo onse omudziwa adzamuyiwala.
11 “Emomiyo ok anyal lingʼ; abiro wacho lit manie chunya, abiro nyiso pek ma an-go e chunya nikech mirima ma an-go.
“Nʼchifukwa chake ine sindidzakhala chete; ndidzayankhula mopsinjika mtima, ndidzadandaula mowawidwa mtima.
12 An nam, koso an ondiek nam momiyo ogona agengʼa kama?
Kodi ine ndine nyanja kapena chirombo chamʼnyanja kuti inu mundiyikire alonda?
13 Ka aparo ni kitandana biro hoya kendo ni piendena mayom biro dwoko chandruokna chien,
Pamene ndikuganiza kuti ndidzapeza chitonthozo pa bedi panga ndipo pogona panga padzachepetsa madandawulo anga,
14 to eka pod ibwoga gi lek magalagala kendo imiya luoro gi fweny mayoreyore,
ngakhale nthawi imeneyo mumandiopseza ndi maloto ndi kundichititsa mantha ndi masomphenya,
15 momiyo koro daher mondo adera kendo atho, moloyo bedo gi ringruok ma an-goni.
kotero kuti ndimalakalaka kudzikhweza kapena kufa, kupambana kupirira zowawa zimene ndikuzimva mʼthupi mwanga.
16 Achayo ngimana; ok agomb kata medo bedo mangima. Weya mos; ndalo mag ngimana onge gi tiende.
Ine ndatopa nawo moyo wanga; sindingakonde kukhala moyo nthawi zonse. Ndisiyeni ndekha pakuti moyo wanga ulibe tanthauzo.
17 “Yaye Nyasaye, dhano to en angʼo momiyo ikawe ka gima lich kendo isiko ipare ndalo duto,
“Kodi munthu nʼchiyani kuti muzimuganizira chotere, kuti muzisamala zochita zake,
18 koso angʼo momiyo isiko inone okinyi kokinyi kendo iteme sa ka sa?
kuti muzimusanthula mmawa uliwonse ndi kumamuyesa nthawi yonse?
19 Yaye Nyasaye, bende diweye ngʼiya, kata kuom thuolo matin kende?
Kodi simudzaleka kumandizonda kuti ndipezeko mpata wopumula?
20 Yaye jarang ji-ni, kata bed ni asetimo richo, to en angʼo ma asetimoni? Angʼo momiyo an ema inena? Koso dibed ni asebedoni tingʼ mapek mohingi?
Ngati ine ndachimwa, ndachita chiyani kwa Inu, Inu wopenyetsetsa anthu? Chifukwa chiyani mwachititsa kuti ndikhale ngati choponyera chandamale chanu? Kodi ndasanduka katundu wolemera kwa Inu?
21 Angʼo momiyo idagi ngʼwonona kuom ketho maga kendo itamori wena richoga? Nikech koro abiro tho machiegni; ibiro manya, to ok enonwangʼa.”
Chifukwa chiyani simukundikhululukira zolakwa zanga ndi kundichotsera machimo anga? Pakuti posachedwa ndilowa mʼmanda; mudzandifunafuna ine koma simudzandionanso.”

< Ayub 7 >