< Ayub 35 >

1 Eka Elihu nowacho kama:
Ndipo Elihu anawonjeza kunena kuti,
2 “Bende iparo ni itimo gima ber kiwacho ni, ‘In kare e nyim Nyasaye?’
“Kodi mukuganiza kuti mukukhoza? Mukunena kuti, ‘Ndine wolungama pamaso pa Mulungu.’
3 To e iyeno bende ipenjo ni, ‘Mano to konya gangʼo, koso ohala mane ma ayudo ka ok atimo richo?’
Komanso inu mukufunsa kuti, ‘Kodi phindu langa nʼchiyani, ndipo ndimapeza chiyani ndikapanda kuchimwa?’
4 “Daher mondo adwoki in kaachiel gi osiepenigo.
“Ine ndikufuna ndikuyankheni inu pamodzi ndi abwenzi anu omwe.
5 Ngʼiuru polo malo mondo unee boche polo kaka ni kuma bor.
Yangʼanani kumwamba ndipo muone mitambo imene ili kutali ndi inuyo.
6 Ka umedo timo richo, to obadhe gangʼo? Kata ka richou ngʼeny to mano nyalo timone angʼo?
Inuyo mukachimwa, Iye zimamukhudza motani? Ngati machimo anu ndi ochuluka, zimenezo zimachita chiyani kwa Iye?
7 Ka un joma kare to bedou makare miye angʼo, koso en angʼo muchiwone?
Ngati inu ndinu wolungama, mumamupatsa Iyeyo chiyani? Kapena Iye amalandira chiyani chochokera mʼdzanja lanu?
8 Timbeu maricho hinyo mana dhano machal kodu, kendo timbeu makare bedo konyruok mana ne yawuot ji.
Kuyipa kwanu kumangokhudza anthu ngati inuyo, ndipo chilungamo chanu chimakhudza anthu anzanu.
9 “Ji ywak malit nikech tingʼ mapek moyie kuomgi; giywak mana ni mondo ogolgi e bwo loch joma thirogi.
“Anthu akufuwula chifukwa cha kuzunzidwa; akufuna chithandizo kuti achoke pansi pa ulamuliro wa anthu amphamvu.
10 To onge ngʼato kuomgi mawachoe ni, ‘Nyasaye mane ochweya nikanye, Nyasaye mamiyo ji wende gotieno,
Koma palibe amene akunena kuti, ‘Kodi ali kuti Mulungu, Mlengi wanga, amene amatisangalatsa nthawi ya usiku,
11 mapuonjowa gik mathoth moloyo kaka opuonjo le manie piny kendo mamiyo wabedo mariek moloyo winy mafuyo e kor polo?’
amene amatiphunzitsa kupambana nyama za dziko lapansi ndipo amatipatsa nzeru kupambana mbalame zowuluka?’
12 Ok odwok ji ka giywakne nikech wich teko mar joricho.
Iye sayankha pamene anthu akufuwulira kwa Iye chifukwa cha kudzikuza kwa anthu oyipa.
13 Adier, Nyasaye ok chik ite ne ywakgi maonge tiendgi Jehova Nyasaye Maratego ok dewgi.
Ndithu, Mulungu samva kupempha kwawo kopanda pake; Wamphamvuzonse sasamalira zimenezi.
14 Iwacho ni Nyasaye ok winj wecheni ka iwacho ni ok inene, kata obedo ni isetero kwayoni e nyime, kendo pod irite mondo odwoki.
Ndipo ndi bodza lalikulu kunena kuti Iye saona zimene zikuchitika. Iye adzaweruza molungama ngati inu mutamudikira
15 Bende imedo wacho ni kata ji ok okum gi mirimbe mager kendo kata mana richo ma ji timo ok obadhe.
ndiye tsono popeza kuti ukali wake sukupereka chilango, zoyipa zambiri zimene anthu amachita,
16 Omiyo Ayub wuoyo ka ngʼama ofuwo; maonge rieko.”
abambo Yobu mumangoyankhula zopandapake, mukungochulukitsa mawu opanda nzeru.”

< Ayub 35 >