< Ayub 32 >

1 Omiyo ji adekgi noweyo dwokore gi Ayub, nikech noparo ni en ngʼama kare.
Tsono anthu atatuwa analeka kumuyankha Yobu, chifukwa chakuti iyeyo ankadziona kuti ndi wolungama.
2 To Elihu wuod Barakel ja-Buz, mane wuok e anywola mar Ram ne iye owangʼ gi Ayub nikech nopwoyore kende owuon kaka ngʼat makare, ka ok oweyo Nyasaye ema mondo opwoye.
Koma Elihu, mwana wa Barakeli, wa fuko la Buzi, wa banja la Ramu, anapsera mtima kwambiri Yobu chifukwa choti Yobuyo anakana kuvomera kuti anachimwa ndi kuti Mulungu anakhoza pomulanga.
3 Iye nowangʼ bende gi osiepe Ayub adek nikech negisiko mana ka gingʼado ne Ayub bura, to kata obedo nine oonge ketho.
Anapseranso mtima abwenzi ake atatu aja chifukwa sanapeze njira yomutsutsira Yobu, ngakhale iwo anamupeza kuti anali wolakwa.
4 Elihu norito mondi eka oloso gi Ayub nikech ne en ngʼama tin e diergi.
Tsono Elihu anadikira kuti ayankhule ndi Yobu chifukwa choti abwenziwo anali akuluakulu kupambana iyeyo.
5 To kane oneno ka ji adekgo osewuoyo mi wechegi orumo, to mirima nomake.
Koma Elihu ataona kuti anthu atatuwo analibe mawu oti ayankhulenso, iye anapsa mtima.
6 Eka Elihu wuod Barakel ja-Buz nowacho kama: “An atin kuom higni, kendo un joma dongona; mano emomiyo naluor, kendo ne ok an gichir mar nyisou gima angʼeyo.
Choncho Elihu mwana wa Barakeli wa fuko la Buzi anati: “Ine ndine wamngʼono, inuyo ndinu akuluakulu, nʼchifukwa chake ndimaopa, ndimachita mantha kuti ndikuwuzeni zimene ndimadziwa.
7 Naparo e chunya ni, ‘Higa ema mondo owuo; kendo dak amingʼa e piny ema mondo opuonj rieko!’
Ndimaganiza kuti, ‘Ayambe ndi akuluakulu kuyankhula; anthu amvulazakale ndiwo amaphunzitsa nzeru.’
8 To ngʼeuru ni chuny manie i dhano, ma en much Jehova Nyasaye Maratego, ema miyo dhano winjo tiend weche.
Koma mzimu wa Mulungu mwa munthu, mpweya wa Wamphamvuzonse, ndi umene umapereka nzeru zomvetsa zinthu.
9 Jomadongo kende ok ema nigi rieko, kata ok ni joma hikgi ngʼeny ema nigi ongʼeyo gima kare.
Si okalamba amene ali ndi nzeru, si amvulazakale okha amene ali ndi nzeru zomvetsa zinthu zimene zili zoyenera.
10 “Kuom mano, awacho kama: Winjauru; an bende koro adwaro nyisou gima angʼeyo.
“Nʼchifukwa chake ndikuti, ‘Mvereni; inenso ndikukuwuzani zimene ndikuzidziwa.’
11 Uwinjo, ne arito mondi kane uwuoyo, ne achiko ita ne wecheu mukwano ni nigi rieko; kinde mane umanyo weche monego uwachi,
Ndadikira nthawi yonseyi, ndimamvetsera mwachidwi zimene mumayankhula, pamene mumafunafuna mawu oti muyankhule,
12 ne achikonu ita adimba kinde mane uwuoyo, to onge ngʼato kuomu moseyudo Ayub gi ketho; kendo onge ngʼato kuomu mosedwoko weche Ayub.
ineyo ndinakumvetseranidi. Koma palibe ndi mmodzi yemwe wa inu amene anatsutsa Yobu; palibe aliyense wa inu amene anamuyankha mawu ake.
13 Kik uwach ni, ‘Ngʼatni riek motamo wangʼwa, Nyasaye ema mondo okwere, to ok dhano!’
Musanene kuti, ‘Ife tapeza nzeru; Mulungu ndiye amutsutse, osati munthu.’
14 To Ayub pod ok omino koda wach, omiyo ok abi dwoke kaka usebedo ka uduokeno.
Koma Yobu sanayankhule motsutsana ndi ine, ndipo ine sindimuyankha monga mmene inu mwamuyankhira.
15 “Jogi dhogi omoko, gionge gima ginyalo dwoko; weche orumonegi.
“Iwo asokonezeka ndipo alibe choti ayankhulenso; mawu awathera.
16 Gichungʼ achungʼa maonge gima giwachi, koro pod arit arita kata obedo ni gilingʼ kamano?
Kodi ine ndidikire chifukwa iwo sakuyankhula tsopano, pakuti angoyima phee wopanda yankho?
17 An bende koro abiro wacho makora; kendo abiro nyisi gima angʼeyo.
Inenso ndiyankhulapo tsopano; nanenso ndinena zimene ndikudziwa.
18 Nikech weche opongʼo chunya, kendo gichuna nyaka anyisigi;
Pakuti ndili nawo mawu ambiri, ndipo mtima wanga ukundikakamiza;
19 bende achalo gi chupa ma divai opongʼo iye kendo ka pien divai manyien madwaro barore.
mʼkati mwanga ndili ngati botolo lodzaza ndi vinyo, ngati matumba a vinyo watsopano amene ali pafupi kuphulika.
20 Nyaka awuo eka abed gi kwe; omiyo nyaka adwoki.
Ndiyenera kuyankhula kuti mtima utsike; ndiyenera kutsekula pakamwa panga ndi kuyankha.
21 Ok abi dewo wangʼ ngʼato bende ok abi wuondo ngʼato;
Sindidzakondera munthu wina aliyense, kapena kuyankhula zoshashalika,
22 nikech ka dine bed ni alony e wuondo ji to Jachwechna ditieka piyo nono.
pakuti ndikanakhala wa luso loyankhula moshashalika, Mlengi wanga akanandilanga msanga.”

< Ayub 32 >