< Ayub 27 >

1 Ayub nochako wuoyo kendo mowacho niya,
Ndipo Yobu anapitiriza kuyankhula kwake:
2 “Akwongʼora gi nying Jehova Nyasaye Maratego mosetamore ngʼadona bura makare, kendo mosemiyo chunya obedo malit,
“Ndithu pali Mulungu wamoyo, amene wakana kundiweruza molungama, Wamphamvuzonse, amene wawawitsa mtima wanga,
3 bende asingora ni kapod angima kendo kapod Nyasaye omiya muya ma ayweyo,
nthawi zonse pamene ndili ndi moyo, mpweya wa Mulungu uli mʼmphuno mwanga,
4 to dhoga ok nowach gimoro marach, kendo lewa ok nowach miriambo.
pakamwa panga sipadzatuluka mawu oyipa, lilime langa silidzayankhula zachinyengo.
5 Ok abi yie ngangʼ ni un kare; ok anasiki mana ka awacho ni aonge ketho nyaka atho.
Sindidzavomereza kuti inu mukunena zoona; mpaka imfa yanga, sindidzataya ungwiro wanga.
6 Abiro siko mana ka awacho ni an kare ndalona duto; kendo pacha ler e wachni e ndalo duto.
Ndidzasunga chilungamo changa ndipo sindidzalola kuti chindichokere; chikumbumtima changa sichidzanditsutsa nthawi yonse ya moyo wanga.
7 “Mad wasika duto mapiem koda, yud kum mana ka joricho!
“Mdani wanga akhale ngati woyipa, wondiwukira akhale ngati munthu wosalungama!
8 Koso geno mane ma ngʼama ok ongʼeyo Nyasaye dibedgo ka ongʼad ndalone, kendo ka Nyasaye okawo ngimane?
Nanga chiyembekezo cha munthu wosapembedza nʼchiyani pamene aphedwa, pamene Mulungu achotsa moyo wake?
9 Bende Nyasaye chiko ite ne ywakne ka masira obirone?
Kodi Mulungu amamva kulira kwake pamene zovuta zamugwera?
10 Bende onyalo bedo gi mor kuom Jehova Nyasaye Maratego? Bende doywagne Nyasaye seche duto?
Kodi adzapeza chikondwerero mwa Wamphamvuzonse? Kodi adzapemphera kwa Mulungu nthawi zonse?
11 “Abiro puonji kaka teko Nyasaye chalo; ok abi pandoni yore mag Jehova Nyasaye Maratego.
“Ndidzakuphunzitsani za mphamvu ya Mulungu ndipo sindidzabisa njira za Wamphamvuzonse.
12 Un duto ngʼato ka ngʼato useneno ma gi wangʼu koro weche manonogi to uwacho nangʼo?
Inu mwadzionera nokha zonsezi. Nanga bwanji mukuyankhula zopanda pake?
13 “Chandruok ma Nyasaye ochano ne ngʼama timo timbe mahundu, kendo girkeni mar ngʼama timo timbe marichogo yudo koa kuom Jehova Nyasaye Maratego ema:
“Pano pali chilango chimene Mulungu amasungira woyipa, cholowa chimene munthu wankhanza amalandira kuchokera kwa Wamphamvuzonse.
14 Kata ne bed ni nyithinde ngʼeny manade, to ligangla ema ochomogi; kendo nyithinde ok noyud chiemo moromogi nyaka chiengʼ.
Angakhale ana ake achuluke chotani adzaphedwa ndi lupanga ndipo zidzukulu zake zidzasowa zakudya.
15 Tuo noneg joma otony e lweny, kendo mon ma chwogi otho ma giweyo ok noywag-gi.
Amene adzatsalireko adzafa ndi mliri, ndipo akazi awo amasiye sadzawalira.
16 Kata jaricho chok fedha mangʼeny manade, kod lewni bende mangʼeny,
Ngakhale aunjike siliva ngati fumbi, ndi kukundika zovala ngati mchenga,
17 to gik mochokogo joma kare ema biro rwako, kendo joma onge ketho nopogre mwanduge mag fedha.
zimene wasungazo wolungama ndiye adzavale, ndipo anthu osalakwa ndiwo adzagawane siliva wakeyo.
18 Ot mogero yomyom ka mbuyi mar otiengʼ, kata ka abila ma jarito ogero.
Nyumba imene akuyimanga ili ngati mokhala kadziwotche, ili ngati msasa umene mlonda amamanga.
19 Onindo ka en gi mwandu, to ochiewo gi lwete nono; ka wangʼe yawore nii to mwandune duto oserumo.
Amapita kokagona ali wolemera koma kutha kwake nʼkomweko; akatsekula maso ake, chuma chake chonse chapita.
20 Masiche nomakgi ka ohula motuch apoya; kendo yamb otieno nokegi mabor.
Zoopsa zimamukokolola ngati madzi achigumula; mphepo yamkuntho imamunyamula usiku.
21 Yamb ugwe tingʼe midhi kode, mi olal nono; oywere mi ogole kare.
Mphepo ya kummawa imamuwulutsa ndipo iye saonekanso ndipo imamuchotsa pamalo pake.
22 Enogo kuomgi koko matek ma ok oweyonigi thuolo, kolawogi matek gi tekone maduongʼ.
Imakuntha pa iye osamuchitira chisoni, pamene akuyesa kuthawa mphamvu zake mwaliwiro.
23 Yamo nokudh kuomgi ka giringo kendo tekone malich nomi kihondko makgi.”
Mphepoyo imamuwomba ndithu ndipo kuchokera pamalo pake imamuopseza.”

< Ayub 27 >