< Jeremia 21 >

1 Wach nobiro ne Jeremia koa ir Jehova Nyasaye kane Ruoth Zedekia noorone Pashur wuod Malkija kod jadolo Zefania wuod Maseya. Negiwacho:
Mfumu Zedekiya inatuma Pasuri mwana wa Malikiya ndi wansembe Zefaniya mwana wa Maseya kwa Yeremiya.
2 “Koro lamnwa Jehova Nyasaye nikech Nebukadneza ruodh Babulon monjowa. Sa moro Jehova Nyasaye nyalo timonwa honni mana kaka osetimonwa e kinde mosekalo mondo omi oa kuomwa.”
Iwo amati akanene kwa Yeremiya mawu akuti, “Tinenere kwa Yehova chifukwa Nebukadinezara mfumu ya Babuloni akutithira nkhondo. Mwina mwake Yehova nʼkutichitira zodabwitsa kuti Nebukadinezarayo achoke kwathu kuno.”
3 To Jeremia nodwokogi niya, “Nyisuru Zedekia,
Koma Yehova anawuza Yeremiya kuti ayankhe Pasuri ndi Zefaniya kuti, “Kamuwuzeni Zedekiya kuti,
4 ‘Ma e gima Jehova Nyasaye, Nyasach Israel, wacho: Achiegni loko gige lweny manie lwetugo mondo ogou, magin mago mutiyogo mondo ukedgo gi ruodh Babulon kod jo-Babulon mantiere oko mar ohinga. Kendo anachokgi duto ei dala maduongʼni.
‘Yehova, Mulungu wa Israeli akuti ndikulandeni zida zimene zili mʼmanja mwanu zimene mukugwiritsa ntchito polimbana ndi mfumu ya ku Babuloni ndi ankhondo ake amene akuzingani kunja kwa lingali. Ndipo ndidzasonkhanitsa zidazo mʼkati mwa mzindawu.
5 An awuon abiro kedo kodi ka iya owangʼ kendo ka an gi mirima mager.
Ineyo mwini wakene ndi mkono wotambasula ndi dzanja lamphamvu, ndidzachita nanu nkhondo ndili wokwiya, wokalipa ndi waukali.
6 Ananeg jogo modak e dala maduongʼni, chwo kaachiel gi le kendo masira malich noneg-gi.
Ndidzakantha amene amakhala mu mzinda muno, anthu pamodzi ndi zirombo, ndipo zidzafa ndi mliri woopsa.
7 Bangʼ mano, Jehova Nyasaye wacho, anachiw Zedekia ruodh Juda, jotende kod joma ni e dala maduongʼni ma notony e masira, ligangla kod kech, ne Nebukadneza ruodh Babulon to gi wasikgi madwaro ngimagi. Enoneg-gi gi ligangla; ok enowenegi kata kechogi kata ngʼwononegi.’
Pambuyo pake, ndidzapereka Zedekiya mfumu ya ku Yuda, nduna zake pamodzi ndi anthu a mu mzinda muno amene adzapulumuke pa nthawi ya mliri, lupanga ndi njala kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni ndi kwa adani awo amene ankafuna kuwapha. Iye adzawapha ndi lupanga. Sadzawachitira chifundo kapena kuwamvera chisoni kapenanso kuwakomera mtima.’
8 “To bende, med nyiso ji ni, ‘Ma e gima Jehova Nyasaye wacho: Ne, aketo e nyimi yor ngima kod yor tho.
“Yehova anati ndiwawuzenso anthu amenewa kuti asankhe pakati pa moyo ndi imfa.
9 Ngʼato angʼata modak e dala maduongʼni noneg gi ligangla, kech kod masira. To ngʼatno mowuok kendo otingʼo bade ne jo-Babulon molworou; notony gi ngimane.
Aliyense amene akhale mu mzinda muno adzaphedwa ndi lupanga, njala kapena mliri. Koma aliyense amene apite kukadzipereka kwa Ababuloni amene akuzinganiwa adzakhala ndi moyo, adzapulumuka.
10 Aramo mar timo ne dala maduongʼni marach ma ok maber, Jehova Nyasaye owacho. Enochiwe e lwet ruodh Babulon, kendo enotieke gi mach.’
Ine ndatsimikiza kuchitira mzinda uno choyipa osati chabwino, akutero Yehova. Udzaperekedwa mʼdzanja la mfumu ya ku Babuloni, ndipo iyeyo adzawutentha ndi moto.
11 “Kuom mano, wachne od joka ruoth mar od Juda ni, ‘Winj wach Jehova Nyasaye;
“Komanso, uwuze banja laufumu la Yuda kuti, ‘Imva mawu a Yehova;
12 Yaye od Daudi, ma e gima Jehova Nyasaye wacho: “‘Ngʼad bura makare okinyi ka okinyi; kony ngʼatno ma imayo e lwet joma thire, ka ok kamano to mirimba noolre oko, kendo liel ka mach nikech timbe mamono misetimo nowangʼ, maonge ngʼama nyalo kweye.
inu a mʼbanja la Davide, Yehova akuti, “‘Weruzani mwachilungamo mmawa uliwonse; pulumutsani mʼdzanja la wozunza aliyense amene walandidwa katundu wake, kuopa kuti ukali wanga ungabuke ndi kuyaka ngati moto wosazimitsika chifukwa cha zoyipa zimene mwachita.
13 Ok adwari, in Jerusalem, un jogo modak ewi holoni, e got mar mesa motimo lwanda, Jehova Nyasaye owacho; un ma uwacho niya, “En ngʼa manyalo kwedowa? En ngʼa manyalo donjo kar pondowa?”
Ndidzalimbana nanu, inu amene mukukhala pamwamba pa chigwa, inu okhala ngati thanthwe lapachidikha, akutero Yehova. Inu amene mumanena kuti, ‘Ndani amene angabwere kudzalimbana nafe? Ndani amene angathe kulowa mʼmalinga mwathu?’
14 Anakumu moromo gi timbeu, Jehova Nyasaye owacho. Anamok mach e bunge magu manowangʼ gimoro amora machiegni kodu.’”
Ndidzakulangani molingana ndi ntchito zanu, akutero Yehova. Ndidzatentha nkhalango zanu; moto udzapsereza zonse zimene zakuzungulirani.’”

< Jeremia 21 >