< Isaya 51 >

1 Winjauru, un mumanyo tim makare kendo udwaro Jehova Nyasaye: Ngʼi aneuru lwanda mane ogolue, ranganeuru kama ne okuny mogolue;
“Mverani Ine, inu amene mukufuna chipulumutso ndiponso amene mumafunafuna Yehova: Taganizani za thanthwe kumene munasemedwa ndipo ku ngwenya kumene anakukumbani;
2 paruru Ibrahim wuonu kod Sara mane onywolou. Ne en mana ngʼat achiel kende kane aluonge kendo nagwedhe mi aloke oganda maduongʼ.
taganizani za Abrahamu, kholo lanu, ndi Sara, amene anakubalani. Pamene ndinkamuyitana nʼkuti alibe mwana, koma ndinamudalitsa ndi kumupatsa ana ambiri.
3 Jehova Nyasaye biro hoyo chuny Sayun adier; kendo obiro bedo gi kech kuom kuondene mokethore; enolok kuondene motimo ongoro chal ka Eden, kendo kuondene modongʼ gunda chal ka puoth Jehova Nyasaye. Mor gi ilo kaachiel gi erokamano gi wer mamit noyud kuome.
Yehova adzatonthozadi Ziyoni, ndipo adzachitira chifundo mabwinja ake onse; Dziko lake la chipululu adzalisandutsa ngati Edeni, malo ake owuma ngati munda wa Yehova. Anthu adzayimba nyimbo zonditamanda ndi kundiyamika.
4 Winjauru un joga, chikuru itu un ogandana: Abiro golo chik kendo bucha makare nobed ler ne ogendini.
“Mverani Ine, anthu anga: tcherani khutu, inu mtundu wanga: malangizo adzachokera kwa Ine; cholungama changa chidzawunikira anthu a mitundu yonse.
5 Adiera mara sudo machiegni piyo, warruokna chiegni, kendo abiro ngʼado bura makare ne ogendini. Joma odak e dho nembe biro ngʼiya ka gin gi geno ni abiro resogi gi tekona.
Ndili pafupi kubwera kudzawombola anthu anga. Ndidzabwera mofulumira ngati kuwunika kudzapulumutsa anthu anga; ndipo ndidzalamulira anthu a mitundu yonse. Mayiko akutali akundiyembekezera. Iwo akudikira kuti ndidzawapulumutse.
6 Tingʼ wangʼi malo ingʼi polo, bende rang piny gie polo, nikech polo nolal nono mana ka iro, to piny bende biro ti mana ka law kendo oganda modak e iye notho mana ka lwangʼni. To resruok makelo nosiki nyaka chiengʼ kendo adiera mara ok norum.
Kwezani maso anu mlengalenga, yangʼanani pansi pa dziko; mlengalenga udzazimirira ngati utsi, dziko lapansi lidzatha ngati chovala ndipo anthu ake adzafa ngati nsabwe. Koma chipulumutso changa chidzakhala mpaka muyaya, chilungamo changa chidzakhala cha nthawi zonse.
7 Winjauru un joma ongʼeyo tim makare, un oganda mondiko chikena e chunyu: Kik uluor weche midiro mag dhano kata luoro ayany mag ji.
“Mverani Ine, inu amene mukudziwa choonadi, anthu inu amene mukusunga malangizo anga mʼmitima yanu; musaope kudzudzulidwa ndi anthu kapena kuopsezedwa akamakulalatirani.
8 Nimar olwenda biro chamogi duto ka law; kendo kudni nochamgi mana ka yie rombe. To adiera mara nosiki manyaka chiengʼ, kendo resruok makelo ok norum e kind tienge gi tienge.
Pakuti njenjete idzawadya ngati chovala; mbozi idzawadya ngati thonje. Koma chilungamo changa chidzakhala mpaka muyaya, chipulumutso changa chidzakhala mpaka mibadomibado.”
9 Aa malo, Aa malo! Jiw badi motegno, yaye Jehova Nyasaye; aa malo kendo ijiwri, mana kaka ne ijiwori chon e ndalo mokadho. Donge in ema nitieko ondiek nam miluongo ni Rahab, mingʼado matindo tindo?
Dzambatukani, dzambatukani! Valani zilimbe, Inu Yehova; dzambatukani, monga munkachitira masiku amakedzana, monga nthawi ya mibado yakale. Si ndinu kodi amene munaduladula Rahabe, amene munabaya chinjoka cha mʼnyanja chija?
10 Donge in ema nomiyo nam oduono, ma gin pige mano chokore kuonde matut, kendo niloso yo e kind nam matut mondo joma ne ireso ongʼadi kadhi loka cha?
Kodi sindinu amene munawumitsa nyanja yayikulu, madzi ozama kwambiri aja? Kodi sindinu amene munapanga njira pa madzi ozama, kuti anthu amene munawapulumutsa awoloke powuma?
11 Joma Jehova Nyasaye osereso nodwogi. Ginidonji e dala Sayun ka giwer; mor mochwere nobed kuomgi. Ginibed gi mor kod ilo, kendo kuyo gi parruok nolal nono kuomgi.
Anthu amene Yehova anawawombola adzabwerera nakafika ku Ziyoni nyimbo ili pakamwa; chimwemwe chamuyaya chizidzaonekera pa nkhope zawo. Adzakhala ndi chikondwerero ndi chimwemwe, chisoni ndi kubuwula zidzathawa.
12 “An, kendo en An e Jal mahoyo chunyu. Angʼo momiyo uluoro yawuot dhano adhana matho, kendo maner mana ka lum,
Yehova akuti, “Ndinetu amene ndimakutonthozani mtima. Chifukwa chiyani mukuopa munthu woti adzafa? Mukuopa munthu woti monga udzu sadzakhalitsa.
13 momiyo wiwu owil gi Jehova Nyasaye ma Jachwechu, Jal mane oyaro polo kendo oketo mise mar piny, momiyo udak gi kihondko pile, nikech kum muyudo kuom ngʼama sandou, kendo oikore mar tiekou. Jal masandouno, ere gima geroneno ditim?
Koma inu mumayiwala Yehova Mlengi wanu, amene anayala za mlengalenga ndi kuyika maziko a dziko lapansi. Inu nthawi zonse mumaopsezedwa chifukwa cha ukali wa anthu okuponderezani amene angofuna kukuwonongani. Kodi uli kuti tsopano ukali wa anthu okuponderezaniwo?
14 Joma ni e twech ma luoro omako ibiro gony machiegni; ok ginitho e kuondegi mag twech kendo ok ginichand chiemo.
Amʼndende adzamasulidwa posachedwa; sadzalowa mʼmanda awo, kapena kusowa chakudya.
15 Nimar an Jehova Nyasaye ma Nyasachi mamiyo Nam gingore mi apaka wuo, Jehova Nyasaye Maratego e nyinge.
Pakuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndimavundula nyanja kotero mafunde ake amakokoma. Dzina lake ndi Yehova Wamphamvuzonse.
16 Aseketo wechena e dhogi kendo aumi gi tipo mar lweta, an ema ne ayaro polo maketo kare, mi aketo mise mar piny kendo awachone jo-Sayun ni, ‘Un e joga.’”
Ndayika mawu anga mʼkamwa mwanu ndipo ndakuphimbani ndi mthunzi wa dzanja langa. Ine ndimayika pa malo pake zinthu za mlengalenga, ndipo ndinayika maziko a dziko lapansi, ndimawuza anthu a ku Ziyoni kuti, ‘Ndinu anthu anga.’”
17 Aa malo, Aa malo! Chiew, yaye Jerusalem, in misemetho e kikombe mar mirima mager, moa e lwet Jehova Nyasaye, kendo isemadho kikombe mamero ji milungʼo nyaka duro.
Dzambatuka, dzambatuka! Imirira iwe Yerusalemu. Iwe amene wamwa chikho cha mkwiyo chimene Yehova anakupatsa. Iwe amene unagugudiza chikho chochititsa chizwezwe.
18 Kuom yawuowi duto mane onywolo onge moro amora mane nyalo taye kata mane nyalo telone komako lwete.
Mwa ana onse amene anabereka, panalibe ndi mmodzi yemwe anamutsogolera; mwa ana onse amene analera, panalibe ndi mmodzi yemwe anamugwira dzanja.
19 Masiche moluwore osemaki ma en kethruok kod tieki; kech kod ligangla, en ngʼa madihoyi kata duogo chunyi.
Mavuto awiriwa akugwera iwe. Dziko lako lasakazika ndi kuwonongeka. Anthu afa ndi njala ndi lupanga. Ndani angakumvere chisoni? Ndani angakutonthoze?
20 Yawuoti osepodho, giriere piny e yore mana ka mwanda mogengʼne ei obadho. Giyudo kum mager moa kuom Jehova Nyasaye kendo chwat mar Nyasache.
Ana ako akomoka; ali lambalamba pa msewu, ngati mphoyo yogwidwa mu ukonde. Ukali wa Yehova ndi chidzudzulo chake zidzawagwera.
21 Kuom mano winj ma, in miseyudo masira midoko ngʼama omer to ok gi kongʼo.
Nʼchifukwa chake imva izi iwe amene ukuvutika, iwe amene waledzera, koma osati ndi vinyo.
22 Ma e gima Jehova Nyasaye ma Nyasachi Manyalo Gik Moko Duto, ma en Nyasachi machwako joge e bura wacho, Ne, asegolo oko e lweti kikombe mane miyo ithembo, bende ok inichak imethi e kikombe mar mirimba kendo.
Ambuye Yehova wanu, Mulungu amene amateteza anthu ake akuti, “Taona, ndachotsa mʼdzanja lako chikho chimene chimakuchititsa kudzandira; sudzamwanso chikho cha ukali wanga.
23 Anaket kikombe e lwet joma sandou mane wacho ni, “Nind piny mondo wawuoth kuomi. Kendo niloko die ngʼeyi ka yo miwuothoe.”
Ndidzapereka chikhocho kwa anthu amene amakuzunza, amene ankakuwuza kuti, ‘gona pansi tikuyende pa msana.’ Ndipo msana wako anawuyesa pansi popondapo, ngati msewu woti ayendepo.”

< Isaya 51 >