< Isaya 46 >

1 Bel kod Nebo ma nyisechegi miywayo gi farese opodho piny. Nyisechegi mosebedo kitingʼo atingʼa osekelo chandruok ma giolo joma otingʼogi.
Beli wagwada pansi, Nebo wawerama; nyama zonyamula katundu za nyamula milungu yawo. Mafano awo asanduka katundu wolemera pa msana pa ngʼombe. Asandukadi ngati katundu pa msana pa nyama zotopa.
2 Gipodho piny giduto; ma ok ginyal kelo resruok ne joma lamogi, ka gin giwegi otergi e twech.
Nyamazo zikuwerama ndi kufuna kugwa ndi milunguyo; sizikutha kupulumutsa katunduyo, izo zomwe zikupita ku ukapolo.
3 Winjuru wachna, yaye od Jakobo, un jo-Israel duto modongʼ, un duto ma aseyiero nyaka aa chakruok kendo ma aserito nyaka aa e nywolu.
Mverani Ine, Inu nyumba ya Yakobo, inu nonse otsala a mʼnyumba ya Israeli, Ine ndakhala ndi kukusamalirani kuyambira mʼmimba ya amayi anu, ndakhala ndikukunyamulani chibadwire chanu.
4 Kata ka udoko moti ma wiu otimo lwar, to pod An mana en, An ema abiro tingʼou mi aresu.
Mpaka pamene mudzakalambe ndi kumera imvi ndidzakusamalirani ndithu. Ndinakulengani ndipo ndidzakunyamulani, ndidzakusamalirani ndi kukulanditsani.
5 To en ngʼa ma unyalo pimago kata ma unyalo kwano ni rom koda? Koso ere ngʼama dichal koda ma dwapimrego?
“Kodi inu mudzandifanizira ndi yani, kapena mufananitsa ndi yani? Kodi mudzandiyerekeza kapena kundifanizitsa ndi yani?
6 Jomoko olo dhahabu piny koa ei okepegi kendo pimo fedha e ratil; bangʼe gichulo jatheth, mondo olesnegigo nyasaye, kendo gikulore piny mi gilame.
Anthu ena amakhuthula golide mʼzikwama zawo ndipo amayeza siliva pa masikelo; amalemba ntchito mʼmisiri wosula kuti awapangire mulungu, kenaka iwo amagwada pansi ndikupembedza kamulunguko.
7 Gitingʼe malo ma gikete e gokgi; eka gikete e kare monego obedie kendo kanyo ema osikoe. Kama oketeno ok onyal chorore. Kata bed ni ngʼato nyalo ywagorene to ok onyal dwoko; bende ok onyal rese e chandruokne.
Amanyamula nʼkumayenda nayo milunguyo pa mapewa awo; amayikhazika pa malo pake ndipo imakhala pomwepo. Singathe kusuntha pamalo pakepo. Ngakhale wina apemphere kwa milunguyo singathe kuyankha; kapena kumupulumutsa ku mavuto ake.
8 Paruru wachni, keturu e pachu kendo pareuru e chunyu un joma ongʼanyo.
“Kumbukirani zimenezi ndipo muchite manyazi, Muzilingalire mu mtima, inu anthu owukira.
9 Paruru gik mosekadho, gigo mane otimore chon, An e Nyasaye kendo onge moro machielo, bende An e Nyasaye kendo onge moro machalo koda.
Kumbukirani zinthu zakale zinthu zamakedzana; chifukwa Ine ndine Mulungu ndipo palibe wina ofanana nane.
10 Anyiso giko mar gimoro mana e kinde mochakore, bende asebedo kahulo gik mapok otimore. Awacho ni: Gima awacho nyaka timre kendo abiro timo gimoro amora mahero.
Ndinaneneratu zakumathero kuchokera pachiyambi pomwe. Kuyambira nthawi yamakedzana ndinaloseratu zoti zidzachitike. Ndikanena zimene ndifuna kuchita ndipo zimachitikadi. Chilichonse chimene ndafuna ndimachichita.
11 Koa yo wuok chiengʼ nakel winyo mager, koa e piny mabor anakel ngʼato machopo dwarona. Gima asewacho nyaka chop kare, gima asechano ema abiro timo.
Ndikuyitana chiwombankhanga kuchokera kummawa. Ndikuyitana kuchokera ku dziko lakutali munthu amene adzakwaniritsa cholinga changa. Zimene ndanena ndidzazikwaniritsadi; zimene ndafuna ndidzazichitadi.
12 Winjauru, un joma chunygi tek kendo mabor gi adiera.
Ndimvereni, inu anthu owuma mtima, inu amene muli kutali ndi chipulumutso.
13 Akelo adiera mara machiegni, ok en mabor; kendo warruokna ok nodeki. Abiro kelo resruok ni Sayun, kendo duongʼna nobed Israel.
Ndikubweretsa pafupi tsiku la chipulumutso changa; sichili kutali. Tsikulo layandikira ndipo sindidzachedwa kukupulumutsani ndi kupereka ulemerero wanga kwa Israeli.

< Isaya 46 >