< Isaya 4 >

1 E kindeno mon abiriyo biro laro dichwo achiel, kagiwacho niya, “Wanacham chiembwa wawegi kendo wanarwak lepwa wawegi, makmana yienwa mondo oluongwa gi nyingi mondo igolnwa wichkuot!”
Tsiku limenelo akazi asanu ndi awiri adzagwira mwamuna mmodzi, nʼkunena kuti, “Ife tizidya chakudya chathuchathu, ndi kuvala zovala zathu; inu mungotilola kuti tidziyitanidwa ndi dzina lanu. Tichotseni manyazi aumbeta!”
2 E kindeno Bad Yath mar Jehova Nyasaye nobed maber kendo man-gi duongʼ, kendo olemo mar piny nobed mor kod duongʼ ne jo-Israel motony.
Tsiku limenelo Nthambi ya Yehova idzakhala yokongola ndi yaulemerero, ndipo chipatso cha mʼdziko chidzakhala chonyaditsa ndi chopereka ulemerero kwa onse opulumuka mu Israeli.
3 Eka joma noyud kotony e Sayun kod Jerusalem noluong ni jomaler, ma gin kar romb ji duto moyud kangima e Jerusalem
Iwo amene adzatsale mu Ziyoni, amene adzatsalire mu Yerusalemu, adzatchedwa oyera, onse amene mayina awo alembedwa pakati pa anthu amoyo okhala mu Yerusalemu.
4 Ruoth Nyasaye noluok richo mag mond Sayun; kendo enopwodh remo manochwer Jerusalem gi roho mar ngʼado bura kod roho mar mach.
Ambuye adzasambitsa akazi a Ziyoni ndi kuchotsa zonyansa zawo. Adzatsuka magazi amene anakhetsedwa mu Yerusalemu ndi mzimu wachiweruzo ndiponso mzimu wamoto.
5 Bangʼe Jehova Nyasaye nokel rumbi mar iro ne ji godiechiengʼ kendo ligek mach mangʼangʼni gotieno e Got Sayun. Duongʼni nobed ka yath maduongʼ makelo tipo.
Tsono Yehova adzayika mtambo wake pamwamba ponse pa phiri la Ziyoni, ndipo pa onse amene asonkhana masana padzakhala mtambo wa utsi ndipo usiku padzakhala malawi amoto. Pamwamba pa zonse padzakhala ulemerero wa Yehova.
6 Nobed mana ka tado makelo tipo ka chiengʼ rieny kendo ka kama ji ringo tonyie ka bwok ne koth kod ahiti maduongʼ.
Ulemerero wake udzakhala mthunzi wothawiramo kutentha kwa masana, udzakhala malo opeweramo mphepo ndi owusiramo mvula.

< Isaya 4 >