< Isaya 15 >

1 Wach nofwenyore kuom jo-Moab ni: Ar manie Moab okethi, omuke ei otieno achiel! Kir manie Moab bende okethi, omuke ei otieno achiel!
Uthenga wonena za Mowabu: Popeza kuti mu usiku umodzi wokha mzinda wa Ari wa ku Mowabu wawonongedwa, wawonongedwa pa usiku umodzi wokha. Mzinda wa Kiri wawonongedwa, wawonongedwa pa usiku umodzi wokha.
2 Jo-Dibon dhiyo e kargi mar lemo, gidhiyo e hembko mag-gi mondo giywagi; kendo jo-Moab goyo nduru nikech Nebo gi Medeba osekethi. Ngʼato ka ngʼato oliel wiye kod tike.
Anthu a ku Diboni akupita ku nyumba ya milungu yawo, akupita ku malo awo achipembedzo kukalira; anthu a ku Mowabu akulirira mofuwula mzinda wa Nebo ndi wa Medeba. Mutu uliwonse wametedwa mpala, ndipo ndevu zonse zametedwa.
3 E yore, girwako pien gugru; to ewi udi kod laru maduongʼ, giduto giywak ka gidengo kendo gingʼielore e lowo.
Mʼmisewu akuvala ziguduli; pa madenga ndi mʼmabwalo aliyense akulira mofuwula, misozi ili pupupu.
4 Jo-Heshbon kod jo-Eleale ywak, kendo ywakgi winjore nyaka Jahaz. Kuom mano jolweny mag jo-Moab ywak kendo kihondko omakogi.
Anthu a ku Hesiboni ndi Eleali akulira mofuwula, mawu awo akumveka mpaka ku Yahazi. Kotero asilikali a ku Mowabu akulira mofuwula, ndipo ataya mtima.
5 Chunya ywago jo-Moab; nimar ogandane ringo kadhi pondo Zoar, ma gichopo nyaka Eglath Shelishiya. Gidhi ka giluwo yo mochomo Luhith ka giywak, e yo madhi Horonaim giywak malit nikech kethruokgi.
Inenso ndikulirira Mowabu; chifukwa othawa nkhondo ake akupita akulira ku chikweza cha Luluti mpaka ku Zowari ndi Egilati-Selisiya akupita akulira ku chikweza cha Luhiti, Akulira mosweka mtima pa njira yopita ku Horonaimu; akulira mosweka mtima chifukwa cha chiwonongeko chawo.
6 Pige mag Nimrim oseduono, kendo lum bende osener, kendo oboke orumo, maonge gimoro amora modongʼ ka ngʼich.
Madzi a ku Nimurimu aphwa ndipo udzu wauma; zomera zawonongeka ndipo palibe chomera chobiriwira chatsala.
7 Omiyo mwandu mane giseloso kendo kano negitingʼo magingʼadogo Holo ma Omburi otiye.
Kotero kuti chuma chomwe anachipeza ndi kuchisunga, achitenga kuti awoloke nacho chigwembe cha Misondozi.
8 Ywakgi winjore nyaka e tongʼ Moab, nduru margi chopo nyaka Eglaim, kendo dengo margi landore nyaka Beer Elim.
Kulira kwawo kukumveka mʼdziko lonse la Mowabu; kulira kwawo kosweka mtima kukumveka mpaka ku Egilaimu ndi Beeri-Elimu.
9 Pige mag Dimon opongʼ gi remo, to kata kamano named kelo masiche ne Dimon, ne joge maringo koa Moab mondo opondi kod jogo modongʼ e pinyno nomak gi sibuor.
Madzi a ku Dimoni afiira ndi magazi, komabe ndidzabweretsa zina zambiri pa Dimoni, mkango woti udzagwire aliyense othawa mu Mowabu ndi aliyense wotsala mʼdzikomo.

< Isaya 15 >