< Hosea 11 >

1 “Ka Israel ne pod nyathi, ne ahere, kendo ne aluongo wuoda ka agolo Misri.
“Israeli ali mwana, ndinamukonda, ndipo ndinayitana mwana wanga kuti atuluke mu Igupto.
2 To kaka ne amedo luongo Israel e kaka nomedo dhi mabor koda. Negichiwo misengini ne Baal kendo wangʼo ubani ne kido molosi.
Koma ndimati ndikamapitiriza kuyitana iwo amandithawa kupita kutali. Ankapereka nsembe kwa Abaala ndipo ankafukiza lubani kwa mafano.
3 An owuon ema napuonjo Efraim wuotho, ka amakogi gi bedegi, to ne ok gifwenyo ni ne en An mane ochangogi.
Ndi Ine amene ndinaphunzitsa Efereimu kuyenda, ndipo ndinawagwira pa mkono; koma iwo sanazindikire kuti ndine amene ndinawachiritsa.
4 Ne atelonegi gi ngʼwono mathoth kaachiel gihera ma ok rum; ne agolo jok mapek e ngʼutgi kendo akulora piny mondo apidhgi.
Ndinawatsogolera ndi zingwe zachifundo cha anthu ndi zomangira za chikondi; ndinachotsa goli mʼkhosi mwawo ndipo ndinawerama nʼkuwadyetsa.
5 “Donge ginidog Misri kendo Asuria nobedi gi loch kuomgi, nikech gitamore weyo richogi?
“Sadzabwerera ku Igupto, koma Asiriya ndiye adzakhala mfumu yawo pakuti akana kutembenuka.
6 Ligangla nomil e miechgi madongo manoketh lodi mag rangeyegi, kendo chenro duto magin-go norum.
Malupanga adzangʼanima mʼmizinda yawo, ndipo adzawononga mipiringidzo ya zipata zawo nadzathetseratu malingaliro awo.
7 Joga oramo chuth mondo oweya. Kata giluong Nyasaye Man Malo Moloyo, to ok notingʼ-gi malo e yo moro amora.
Anthu anga atsimikiza zondifulatira Ine. Ngakhale atayitana Wammwambamwamba, sizidzatheka kuti Iye awakwezenso.
8 “Ere kaka anyalo jwangʼou, Efraim? Ere kaka dabolu Israel? Ere kaka datiu ka Adma? Ere kaka damiu ubed machal gi Zeboim? Ok anyal timonu kamano; nikech aseloko pacha kendo akechou.
“Kodi ndingakusiye bwanji iwe Efereimu? Kodi ndingakupereke bwanji iwe Israeli? Kodi ndingakuchitire bwanji zimene ndinachitira Adima? Kodi ndingathe bwanji kukuchitira zimene ndinachitira Zeboimu? Mtima wanga wakana kutero; chifundo changa chonse chikusefukira.
9 Ok anaol mirimba mager bende ok analokra mi aketh Efraim bende. Nimar an Nyasaye, ok an dhano, Jal Maler e dieru. Ok anabi gi mirima.
Sindidzalola kuti ndikulange ndi mkwiyo wanga woopsa, kapena kutembenuka ndi kuwononga Efereimu. Pakuti Ine ndine Mulungu osati munthu, Woyerayo pakati panu. Sindidzabwera mwaukali.
10 Gibiro luwo Jehova Nyasaye, noruti ka sibuor. Kuruto, to nyithinde duto nobi ire katetni kagiwuok yo podho chiengʼ.
Iwo adzatsatira Yehova; Iye adzabangula ngati mkango. Akadzabangula, ana ake adzabwera akunjenjemera kuchokera kumadzulo.
11 Ginibi ire ka gitetni ka winy moa Misri, ka akuche moa Asuria. Anami gibed e miechgi,” Jehova Nyasaye owacho.
Adzabwera akunjenjemera ngati mbalame kuchokera ku Igupto, ngati nkhunda kuchokera ku Asiriya. Ine ndidzawakhazikanso mʼnyumba zawo,” akutero Yehova.
12 Efraim oselwora gi miriambo, od jo-Israel en kar wuond. Juda ok winj Nyasaye; adier ok giwinj Jal Maler ma ja-adiera.
Efereimu wandizungulira ndi mabodza, nyumba ya Israeli yandizungulira ndi chinyengo. Ndipo Yuda wawukira Mulungu, wawukira ngakhale Woyerayo amene ndi wokhulupirika.

< Hosea 11 >