< Ezekiel 36 >

1 “Wuod dhano, kor wach kuom gode mag Israel, kendo wachnegi ni, ‘Yaye gode mag Israel, winjuru wach Jehova Nyasaye.
“Iwe mwana wa munthu, yankhula kwa mapiri a Israeli ndipo unene kuti, ‘Inu mapiri a Israeli, imvani mawu a Yehova.’
2 Ma e gima Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto wacho: Wasigu nogoyonu siboi kawacho niya, “Donge uwuoro! Gode machon maboyo koro osedoko mawa.”’
Ine Ambuye Yehova ndikuti: Mdani wanu ankanena kuti, ‘Aa! Dziko lamapiri lakalekale lija lasanduka lathu.’
3 Kuom mano, kor wach kiwacho kama: ‘Ma e gima Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto wacho: Nikech negimonjo pinyu ma giketho kuonde duto mage mine udongʼ maonge nyalo e kind ogendini mamoko, kane gijarou kendo giwuoyo kuomu marach,
Choncho nenera ndipo uwawuze kuti, ‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Popeza anakusakazani ndi kukuponderezani ku mbali zonse motero kuti munakhala mʼmanja mwa anthu a mitundu ina yonse ndipo anthu ankakunenani ndi kukunyozani,
4 kuom mano, yaye un gode mag Israel, winjuru gima an Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto wacho ni gode madongo gi matindo, kaachiel gi aore kod holni, gi kuonde modongʼ gundni, mane ogendini mokiewo gi jo-Israel oyako kendo oyiero.
choncho, inu mapiri a Israeli, imvani zimene Ine Ambuye Yehova ndikuwuza mapiri ndi magomo, zigwembe ndi zigwa, mabwinja ndi mizinda yosiyidwa imene yakhala ikufunkhidwa komanso kunyozedwa ndi anthu a mitundu ina okuzungulirani.
5 Ma e gima Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto wacho: Asewuoyo ka an gi nyiego maliel ka mach kuom ogendini mamoko duto, kendo kuom piny Edom duto, nikech negiloko pinya margi, kendo ne giyako lege mage, ka chunygi opongʼ gi mor.’
Tsono Ine Ambuye Yehova ndikuti: Mu mkwiyo wanga woopsa ndinayankhula kuyimba mlandu mitundu ina yonse ya anthu makamaka a ku Edomu. Iwowa mwa chimwemwe chodzaza tsaya ndi mwa nkhwidzi analanda dziko langa ndi kulisandutsa lawo ndi kutengeratu dziko la msipu kukhala lawo.’
6 Kuom mano, kor wach kuom piny Israel, kendo wach ni gode madongo gi matindo, kaachiel gi rogo kod holni kama: ‘Ma e gima Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto wacho: Awuoyo ka an gi mirima mager, nikech usewinjo marach ka ogendini jarou.
Nʼchifukwa chake, lengeza ku dziko la Israeli, ndipo uwuze mapiri ndi magomo, zigwembe ndi zigwa kuti, ‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Ine ndikuyankhula ndi mtima wokwiya kwambiri chifukwa inu munalandira chitonzo cha anthu a mitundu ina.’
7 Emomiyo ma e gima Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto wacho: Akwongʼora ni ogendini molworou noyud wichkuot.
Ine Ambuye Yehova ndikuti: Ndikulumbira nditakweza dzanja langa kuti mitundu ya anthu idzatozedwanso.
8 “‘To un, joga Israel, yien nochak odong e gode mag Israel, mi nyagnu olembe, nikech ubiro dok e piny machiegni.
“Koma Inu mapiri a Israeli mudzaphukanso nthambi ndipo mudzawabalira zipatso anthu anga a Israeli, pakuti ali pafupi kubwerera kwawo.
9 Aikora mar konyou kendo abiro rangou gi ngʼwono; mi puotheu pur mi pidhie kothe, un oganda mar dhood Israel duto,
Taonani, Ine ndili mbali yanu ndipo ndidzakukomerani mtima. Mudzalimidwa ndi kudzalidwa.
10 abiro miyo unyaa mi udok mangʼeny. Mier matindo ji biro dakie, kendo kuonde momukore ibiro gero kendo.
Ndidzachulukitsa chiwerengero cha anthu anu, nyumba yonse ya Israeli. Mʼmizinda mudzakhalanso anthu ndipo mabwinja adzamangidwanso.
11 Abiro medo kar kwan mar ji kod mar jamni modak e dieru, kendo gibiro medore mi gidok mathoth mokalo akwana. Abiro miyo ji gedo kuomu kaka chon, kendo abiro miyo unyaa moloyo kaka chon. Eka unungʼe ni An e Jehova Nyasaye.
Ndidzachulukitsa chiwerengero cha amuna pamodzi ndi ziweto zomwe, ndipo adzachuluka kwambiri ndi kubereka ana ambiri. Ndidzakhazika anthu mʼdzikomo monga analili kale, ndi kukulemeretsani kuposa kale. Pamenepo inu mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
12 Abiro keto ji, ma gin joga Israel, mondo owuoth kuomu. Gibiro kawou, kendo ubiro bedo girkeni margi, kendo ok unuchak umagi nyithindgi.
Ndidzachititsa anthu kuyenda pa inu, ndiye kuti inu anthu anga Aisraeli. Iwowo adzakhazikika pa inu, ndipo inu mudzakhala cholowa chawo. Simudzalandanso ana awo.
13 “‘Ma e gima Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto wacho: Nikech ji wachonu niya, “Unego ji kendo umayo ogandau nyithindgi,”
“Ine Ambuye Yehova ndikuti: Popeza anthu amanena kuti, ndiwe dziko limene limadya anthu ake ‘kulanda ana a mtundu wake,’
14 omiyo koro ok ubi nego ji kata miyo ogandau dongʼ migumba, Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto owacho.
nʼchifukwa chake, simudzadyanso anthu kapena kulanda ana a mtundu wako. Ine Ambuye Yehova ndikutero.
15 Ok anachak ayie uwinj siboi mar ogendini; kendo ok unuchak une malit ka ji jarou kata ka gimiyo pinyu podho, Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto osewacho.’”
Sindidzakulolaninso kumva mnyozo wa anthu a mitundu ina, kapena kupirira kunyogodola kwawo kapenanso kupunthwitsanso anthu a mʼdziko lako. Ndikutero Ine Ambuye Yehova.”
16 Wach Jehova Nyasaye nochako obirona kendo kama:
Yehova anandiyankhulanso kuti:
17 “Wuod dhano, ka oganda mar jo-Israel ne pod odak e pinygi giwegi, ne gidwanye gi yoregi kod timbegi mamono. Timbegi ne ogak kaka gak mar dhako e nyima e kinde ma oneno malo.
“Iwe mwana wa munthu, pamene anthu a Israeli ankakhala mʼdziko lawolawo, analiyipitsa ndi makhalidwe awo ndiponso zochita zawo. Machitidwe awo pamaso panga anali onyansa pa zachipembedzo ngati msambo wa mkazi amene ali pa nthawi yake.
18 Omiyo ne aolo mirimba kuomgi nikech ne gisechwero remo e piny, kendo nikech ne gisedwanye gi nyisechegi mopa.
Tsono ndinawalanga chifukwa cha magazi amene anakhetsa mʼdzikomo, ndiponso chifukwa anayipitsa dziko ndi mafano awo.
19 Ne akeyogi e dier ogendini, kendo negidak e kind ogendini mopogore opogore. Ne angʼadonegi bura kaluwore gi yoregi kod timbegi mamono.
Ndinawamwaza pakati pa anthu a mitundu ina ndipo anabalalikira mʼmayiko onse. Ndinawalanga molingana ndi makhalidwe awo ndi zochita zawo.
20 Kendo kuonde duto mane gidhiyoe e dier ogendini to ne gichayo nyinga maler, nikech ji ne wuoyo kuomgi kawacho ni, ‘Magi gin jo-Jehova Nyasaye, to ne oriembogi e lope.’
Atafika kwa anthu a mitundu ina, kulikonse kumene anapitako, anayipitsa dzina langa loyera. Zinatero popeza anthu ponena za iwo ankanena kuti, ‘Awa ndi anthu a Yehova, komatu anachotsedwa ku dziko lake.’
21 Ne aparo mondo atim gimoro ne nyinga maler, ma dhood Israel nosedwanyo e dier ogendini kuonde mane gidhiye.
Koma Ine ndinkadera nkhawa dzina langa loyera, limene Aisraeli analiyipitsa pakati pa anthu a mitundu ina kumene anapitako.
22 “Emomiyo wachne dhood Israel ni, ‘Ma e gima Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto wacho: Ok abi timo gigo nikech un, yaye dhood Israel, to abiro timogi nikech nyinga maler, ma usedwanyo e dier ogendini kuonde duto musedhiyoe.
“Nʼchifukwa chake awuze Aisraeliwo kuti Ine Ambuye Yehova ndikuti: Ine ndidzachita zimene ndidzachitezo osati chifukwa cha inuyo Aisraelinu ayi, koma chifukwa cha dzina langa, limene mwaliyipitsa pakati pa anthu a mitundu ina kumene munapitako.
23 Abiro nyiso kaka nyinga marahuma musedwanyo e dier ogendini, ler, nyingno musechido e diergi. Eka ogendini nongʼe ni An e Jehova Nyasaye, chiengʼ ma ananyisra kaka ngʼama ler ka uneno gi wangʼu, Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto osewacho.
Ndidzaonetsa chiyero cha dzina langa lotchuka, limene layipitsidwa pakati pawo. Anthu a mitundu inayo atadzazindikira kuti ndaonetsa kudzera mwa inu kuti dzina langa ndi loyera, iwo adzadziwanso kuti Ine ndine Yehova. Ndikutero Ine Ambuye Yehova.
24 “‘Nikech abiro golou oko e dier ogendini; chokou kagolou e pinje duto mi aduogu kendo e lopu uwegi.
“Pakuti Ine ndidzakuchotsani pakati pa anthu a mitundu ina. Ndidzakusonkhanitsani kuchoka ku mayiko onse ndi kukubwezerani ku dziko lanulanu.
25 Abiro kiro pi maler kuomu mi udok jomaler; abiro pwodhou kuom timbeu mamono kendo kuom nyisecheu duto mopa.
Ndidzakuwazani madzi oyera, ndipo mudzakhala oyera mtima. Zonse zimene zimakuyipitsani zidzachoka. Ndidzakuyeretsani pochotsa mafano anu onse.
26 Abiro miyou chuny manyien kod paro manyien; kendo anagol kuomu chuny matek ka lwanda mi amiu chuny mayom ka ringʼo.
Ndidzakupatsani mtima watsopano ndi kulowetsa mzimu watsopano mwa inu. Ndidzachotsa mwa inu mtima wanu wowuma ngati mwala ndi kukupatsani mtima wofewa ngati mnofu.
27 Abiro olo Roho mara kuomu, mi aket ulu buchena kendo uket chunyu mar rito chikena.
Ndipo ndidzayika Mzimu wanga mwa inu ndipo ndidzakuthandizani kutsatira malangizo anga ndi kukusungitsani mosamala kwambiri malamulo anga.
28 Ubiro dak e piny mane amiyo kwereu; unubed joga to anabed Nyasachu.
Mudzakhala mʼdziko limene ndinapatsa makolo anu. Mudzakhala anthu anga, ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wanu.
29 Abiro resou kuom gik moko duto ma dimi ubed mogak. Abiro kelonu cham mi ubed gi cham mogundho kendo ok anawe ubed gi kech.
Ndidzakupulumutsani ku zonse zokuyipitsani. Ndidzakuchulukitsirani tirigu ndipo sindidzakugwetseraninso njala.
30 Anami olembeu kod cham mag puotheu nyag mangʼeny, kendo ok unuchak une wichkuot e dier ogendini nikech wach kech.
Ndidzachulukitsa zipatso za mʼmitengo yanu ndi zokolola za mʼmunda mwanu, kotero kuti simudzanyozedwanso pakati pa anthu a mitundu ina chifukwa cha njala.
31 Eka unupar yoreu kod timbeu maricho, kendo unucharu kendu nikech richou kod timbeu mamonogo.
Pamenepo mudzakumbukira makhalidwe anu oyipa ndi ntchito zanu zoyipa. Machimo anu ndi ntchito zanu zonyansa zidzakuchititsa nokha manyazi.
32 Adwaro ni ungʼe ni gigi duto ok atim nikech un, Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto osewacho. Yaye dhood Israel, neuru wichkuot kuom timbeu mamono!
Tsono dziwani kuti Ine sindidzachita zimenezi chifukwa cha inuyo ayi, ndikutero Ine Ambuye Wamphamvuzonse. Ndiyetu chitani manyazi ndipo mugwetse nkhope zanu, inu Aisraeli chifukwa cha makhalidwe anu!
33 “‘Ma e gima Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto wacho: Odiechiengʼ ma anapwodhie kuom richoni duto, anami ji odagi e miechi kendo, kendo kuonde momukore magi nochak oger.
“Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pa tsiku limene ndidzayeretse machimo anu onse, ndidzayikamonso anthu mʼmizinda yanu, ndipo ndidzamanganso nyumba pa mabwinja.
34 Piny motwo nopur, ka joma kadho e diergi neno, kendo ok nowegi ginind mbora.
Dziko limene linasanduka chipululu lizidzalimidwanso. Mʼmalo moti aliyense wopitamo alione dzikolo ngati chipululu tsopano adzaliona lolimidwa.
35 Giniwach niya, “Lopni ma yande okethi mowe nono koro osedoko machal gi puoth Eden, kendo mier madongo mane omuki kendo okethi molokore gunda tinde ochiel motegno kendo ji odakie.”
Iwo adzati, ‘Dziko ili, limene linali chipululu, lasanduka munda wa Edeni. Mizinda imene inali mabwinja osiyidwa ndi owonongedwa, tsopano ndi yotetezedwa ndi yokhalamo anthu.
36 Eka ogendini modongʼ molworou nongʼe ni an Jehova Nyasaye ema asegero gik mane omuki, kendo an ema asechako akomo puothe mane odongʼ mbora. An Jehova Nyasaye ema asewuoyo kamano, kendo abiro timo gima awacho.’
Ndipo anthu a mitundu ina okhala pafupi nanu amene anatsala adzadziwa kuti Ine Yehova ndine amene ndinamanganso mizinda yowonongeka ndi kudzalanso zinthu zatsopano mʼmalo mʼmene munali chipululu. Ine Yehova ndayankhula ndipo ndidzazichitadi.’
37 “Ma e gima Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto wacho: Abiro winjo kwayo jo-Israel kendo mi atimnegi kama: Abiro miyo ogendini doko mangʼeny ka rombe,
“Ine Ambuye Yehova ndikuti: Ndidzalolanso Aisraeli kuti andipemphe zoti ndiwachitire: Ndidzachulukitsa anthu awo ngati nkhosa.
38 adier ginibed mangʼeny mana ka jamni mitimogo misango Jerusalem e kinde mag nyasi mitimo higa ka higa. Omiyo mier madongo mokethore biro pongʼ gi kweth mag ji. Eka giningʼe ni An e Jehova Nyasaye.”
Adzachulukadi ngati nkhosa zomwe ankapereka ngati nsembe ku Yerusalemu pa nthawi za chikondwerero. Choncho mizinda ya mabwinja idzadzaza ndi anthu. Zikadzatero adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”

< Ezekiel 36 >