< Rapar Mar Chik 7 >

1 Ka Jehova Nyasaye ma Nyasachu okelou e piny ma udhi donjoe mondo ukaw obed maru, mi oriembonu ogendini mangʼeny kaka jo-Hiti, jo-Girgash, jo-Amor, jo-Kanaan, jo-Perizi, jo-Hivi kod jo-Jebus, ma gin pinje abiriyo madongo kendo maroteke moloyou.
Pamene Yehova Mulungu wanu wakufikitsani mʼdziko limene mukukalowa ndi kulilanda ndi kuthamangitsa pamaso panu mitundu ya anthu iyi: Ahiti, Agirigasi, Aamori, Akanaani, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi; yomwe ndi mitundu isanu ndi iwiri yayikulu ndi yamphamvu kuposa inu;
2 Kendo ka Jehova Nyasaye ma Nyasachu osechiwo gi e lwetu mi uloyogi, to une ni utiekogi duto. Kik ulos winjruok kodgi bende kik utimnegi ngʼwono.
Yehova Mulungu wanu akadzawapereka mʼmanja mwanu, ndipo inu mukadzawagonjetsa, mudzawawononge kwathunthu. Musadzachite mgwirizano ndi anthuwo ndiponso musadzawachitire chifundo.
3 Kik ukendru kodgi. Kik uchiw nyiu ni yawuotgi kata kik yawuotu okend nyigi,
Musadzakwatirane nawo. Musadzapereke ana anu aakazi kwa ana awo aamuna kapena kutenga ana anu aamuna ndi kuwapereka kwa ana awo aakazi.
4 nimar ginimi yawuotu weya mitine nyiseche mamoko kendo mano dimi mirima mak Jehova Nyasaye mitieku mapiyo nono.
Mukadzatero, iwo adzasocheretsa ana anu aamuna kuti asanditsatire ndi kutumikira milungu ina. Motero Yehova adzakukwiyirani ndi kukuwonongani mwachangu.
5 Ma e gima onego utimnegi: Mukuru kendegi mag misengini, touru kitegi mopa milamo, tongʼuru sirnigi mag Ashera kendo wangʼuru kido mag-gi milamo e mach.
Koma mukachite izi: Mukagumule maguwa awo ansembe, mukaswe miyala yawo yachipembedzo, mukadule mitengo yawo ya Asera, ndi kutentha mafano awo pa moto.
6 Nimar un oganda mowal ne Jehova Nyasaye ma Nyasachu. Jehova Nyasaye ma Nyasachu oseyierou kuom ogendini duto manie piny mondo ubed joge, joge owuon mogeno.
Pakuti inu ndinu anthu opatulika kwa Yehova Mulungu wanu. Yehova Mulungu wanu anakusankhani pakati pa anthu onse pa dziko lapansi kuti mukhale ake, chuma chake cha mtengo wapatali.
7 Jehova Nyasaye ne ok oherou mi oyierou nikech ne ungʼeny moloyo ogendini mamoko, nimar un e oganda matinie moloyo,
Yehova sanakukondeni chifukwa choti munali ochuluka kuposa ena pakuti inuyo ndiye munali ochepetsetsa mwa anthu onse.
8 to Jehova Nyasaye noyierou nikech noherou kendo orito singruok mane otimo gi kwereu kane ogolou gi tekone maduongʼ kendo warou e piny mane unie wasumbini, e lwet Farao ruodh Misri.
Koma chifukwa chakuti Yehova anakukondani nasunga lumbiro lake limene analumbira kwa makolo anu. Ndi chifukwa chake anakutulutsani ndi mphamvu yake yopanda malire ndi kukupulumutsani ku dziko la ukapolo, kuchoka mʼmanja mwa Farao mfumu ya ku Igupto.
9 Ngʼeuru ni Jehova Nyasaye ma Nyasachu en Nyasaye. En Nyasaye ma ja-adiera; marito singruokne mar hera ne tienge gana gi gana mohere kendo rito chikene.
Choncho dziwani kuti Yehova Mulungu wanu, ndi Mulungu. Iye ndi Mulungu wokhulupirika, wosunga pangano lake la chikondi chosasinthika ku mibadomibado, kwa iwo amene amamukonda nasunga malamulo ake.
10 To jogo mochaye obiro kumo motiekgi mana ka gineno, adier ok obi deko ma ok okumo jogo mochaye.
Koma iwo amene amamuda adzawabwezera powawononga pamaso pawo; sadzachedwa kuwabwezera iwo amene amadana naye.
11 Kuom mano rituru yorene, buchene kod chikene adimba ma amiyou kawuono.
Choncho muziyesetsa kusunga malamulo, malangizo ndi maphunziro amene ndikukulamulani lero lino kuti muchite.
12 Ka uchiko itu ne chikegi kendo uritogi adimba, eka Jehova Nyasaye ma Nyasachu norit singruokne mar hera kodu kaka ne osingore ne kwereu.
Mukamvera malamulo amenewa, ndi kusamala kuwatsata, ndiye kuti Yehova Mulungu wanu adzasunga pangano lake la chikondi chosasinthika ndi inu, monga analumbira kwa makolo anu.
13 Obiro herou, gwedhou kendo miyo unyaa mangʼeny, obiro gwedho nyithindo munywolo, cham manie puotheu, decheu, divai manyien, mo, nyiroye ma dhou onywolo kod nyithi jambu e piny mane osingore ne kwereu ni nomigi.
Iye adzakukondani nakudalitsani ndi kukuchulukitsani. Adzadalitsa chipatso cha mʼmimba mwanu, zokolola za mʼdziko mwanu, tirigu wanu, vinyo wanu ndi mafuta anu, ana angʼombe zanu ndi ana ankhosa zanu mʼdziko limene analumbirira kwa makolo anu kuti akupatseni inu.
14 Ibiro gwedhou moloyo ogendini duto; onge ngʼato kuomu madichwo kata madhako ma ok nobed maonge nyathi, kata jambu manobed maonge nyithindo.
Inu mudzadalitsika kuposa mtundu wina uliwonse wa anthu ndipo palibe mwamuna kapena mkazi aliyense pakati panu amene adzakhale wosabereka. Ziweto zanu nazonso, sipadzapezeka zosabereka.
15 Jehova Nyasaye notiek tuoche duto kuomu; bende ok nokelnu tuoche maricho mane uneno ka un Misri, to tuochego nomak mana wasiku mochayou.
Yehova adzakupewetsani ku matenda aliwonse. Sadzakugwetserani matenda owopsa aja munawadziwa ku Igupto, koma adzawagwetsera pa odana nanu.
16 Nyaka utiek ji duto ma Jehova Nyasaye ma Nyasachu keto e lwetu. Kik ukechgi bende kik ulam nyisechegi, nimar mano nobednu obadho.
Muwononge anthu onse amene Yehova Mulungu wanu awapereka kwa inu. Musawamvere chisoni ndipo musatumikire milungu yawo pakuti umenewo udzakhala msampha kwa inu.
17 Unyalo wacho kendu niya, “Ogendinigi tek moloyowa. Ere kaka wanyalo riembogi oko?”
Mukhoza kunena kuti, “Anthu awa ndi amphamvu kuposa ifeyo. Nanga tingawapirikitse bwanji?”
18 To kik uluorgi; paruru malongʼo gima ne Jehova Nyasaye ma Nyasachu otimone Farao gi piny e Misri duto.
Koma musachite nawo mantha, kumbukirani bwino zimene Yehova Mulungu wanu anachita ndi Farao pamodzi ndi Igupto yense.
19 Ne uneno kod wengeu tem malich, honni madongo tekone kod bat morie mane Jehova Nyasaye ma Nyasachu ogolougo oko. Jehova Nyasaye ma Nyasachu biro timo mano bende ne oganda makoro uluoro.
Munadzionera nokha ndi maso anu mayesero aakulu, zizindikiro zozizwitsa ndi zodabwitsa, mphamvu yake yopanda malire imene Yehova Mulungu wanu anakutulutsirani. Yehova Mulungu adzachita zimenezo ndi anthu onse amene muwaopa tsopano.
20 To bende Jehova Nyasaye ma Nyasachu biro miyo kihondko omakgi ma kata ngʼato pond e dieru manade to ok notony.
Kuwonjezera apo, Yehova Mulungu wanu adzatumiza mavu pakati pawo mpaka atamaliza onse amene adzakubisalirani.
21 Kik gimiu luoro nimar Jehova Nyasaye ma Nyasachu manie dieru duongʼ kendo en Nyasaye man-gi teko.
Musaopsedwe nawo pakuti Yehova Mulungu wanu, amene ali pakati panu, ndi Mulungu wamkulu ndi woopsa.
22 Jehova Nyasaye ma Nyasachu biro riembo ogendinigo kuomu matin tin mana ka uneno. Ok noyienu mondo utiekgi dichiel nimar dipo ka ondiegi onywolore mangʼeny mathagu.
Yehova Mulungu wanu adzapirikitsa anthu a mitundu yonse pamaso panu, pangʼonopangʼono. Sadzakulolani kuti muwathe nthawi imodzi, kuti nyama zakuthengo zingadzaswane mokuzungulirani.
23 To Jehova Nyasaye ma Nyasachu nochiwgi e lwetu, kowito riekogi nyaka ginirum duto.
Koma Yehova Mulungu wanu adzawapereka kwa inu, adzawasokoneza kufikira atawonongedwa.
24 Obiro chiwo ruodhi mag ogendinigo e lwetu kendo unutiek nyingegi e bwo polo. Onge ngʼama nochungʼ masiru kendo unutiekgi duto.
Iye adzapereka mafumu awo mʼdzanja lanu, ndipo adzafafaniza mayina awo pa dziko lapansi. Palibe amene adzalimbana nanu, inu mudzawawononga.
25 Kido mag nyisechegi nyaka uwangʼ e mach. Kik ugomb fedha kod dhahabu ma gin-go, bende kik ukawgi. Ka utimo kamano, to ginibednu obadho nimar gigo gin gigo makwero ne Jehova Nyasaye ma Nyasachu.
Muwawotche pa moto mafano a milungu yawo. Musasirire siliva ndi golide amene ali pa mafanoyo. Musamutenge kuti akhale wanu chifukwa mukatero mudzakodwa naye ngati msampha, pakuti Yehova Mulungu wanu amanyansidwa nazo.
26 Kik ukel gimoro makwero e uteu, nimar un kod gima ukelono nokethi. Kik ubed gi gik machalo kamano nimar enokethgi.
Musabweretse chinthu chonyansa mʼnyumba mwanu kuopa kuwonongedwa ngati chonyasacho. Muziyipidwa ndi kunyansidwa nacho kwambiri pakuti chidzawonongedwanso.

< Rapar Mar Chik 7 >