< 2 Weche Mag Ndalo 6 >

1 Eka Solomon nowacho niya, “Jehova Nyasaye osewacho ni enodag ei bor polo motimo mudho.
Pamenepo Solomoni anati, “Yehova anati adzakhala mʼmitambo yakuda;
2 Asegeroni hekalu marahuma, kama inidagie nyaka chiengʼ.”
ine ndakumangirani Nyumba yokongola kwambiri, malo woti muzikhalamo mpaka muyaya.”
3 Kane oganda jo-Israel duto ochungʼ kanyo, ruoth nolokore mogwedhogi.
Aisraeli onse ali chiyimire pomwepo, mfumu inatembenuka ndi kuwadalitsa.
4 Eka nowacho niya, “Pak obed ne Jehova Nyasaye, ma Nyasach Israel, mosetimo gi lwete gima ne osingo gi dhoge ni Daudi wuonwa. Nikech nowacho niya,
Ndipo inati, “Atamandike Yehova, Mulungu wa Israeli amene wachita ndi dzanja lake zimene analonjeza ndi pakamwa pake kwa Davide abambo anga. Pakuti Iye anati,
5 ‘Chakre ndalo mane agolo joga koa Misri pok ayiero dala maduongʼ e dhoot moro amora mar Israel mondo oger hekalu kanyo ni Nyinga, to aseyiero Daudi mondo otel ni joga Israel.
‘Kuyambira tsiku limene ndinatulutsa anthu anga ku Igupto, sindinasankhe mzinda wina uliwonse pa fuko lina lililonse la Aisraeli kuti kumeneko andimangire Nyumba kuti ndizikhalamo kapena munthu wina aliyense kuti akhale mtsogoleri wa Aisraeli anthu anga.
6 To koro aseyiero Jerusalem mondo obed kama Nyinga betie kendo aseyiero Daudi mondo otel ni joga Israel.’
Koma tsopano ndasankha Yerusalemu kuti Dzina langa likhale kumeneko ndiponso ndasankha Davide kuti alamulire anthu anga Aisraeli.’
7 “Daudi wuora noketo e chunye mondo oger hekalu moluongo nying Jehova Nyasaye ma Nyasach Israel.
“Abambo anga Davide anali ndi maganizo mu mtima mwawo oti amangire Nyumba Yehova Mulungu wa Israeli.
8 To Jehova Nyasaye nowacho ni Daudi wuora niya, ‘Nitimo maber mondo ibed gi wach gero hekalu ni nyinga e chunyi.
Koma Yehova ananena kwa abambo anga Davide kuti, ‘Popeza zinali mu mtima mwako kumangira Nyumba dzina langa, unachita bwino kukhala ndi maganizo amenewa mu mtima mwakomo.
9 Kata kamano in ok niger hekalu, to wuodi, ma en ringri gi rembi iwuon; en ema noger hekalu ni Nyinga.’
Komatu si iwe amene udzamanga Nyumba ya Mulungu koma mwana wako, mwana amene iwe udzabereke. Iyeyo ndiye amene adzandimangire Nyumba.’
10 “Jehova Nyasaye oserito singruok mane otimo. Asekawo loch wuora Daudi kendo asebet e kom loch mar Israel mana kaka Nyasaye nosingo kendo asegero hekalu ni Nying Jehova Nyasaye ma Nyasach Israel.
“Yehova wasunga zimene analonjeza. Ine ndalowa mʼmalo mwa abambo anga Davide, ndipo tsopano ndili pa mpando waufumu wa Israeli, monga momwe Yehova analonjezera, ndipo ndamangira nyumba Dzina la Yehova Mulungu wa Israeli.
11 Aseketo Sandug Muma ma moketie singruok mane Jehova Nyasaye otimo e kinde gi jo-Israel.”
Mʼmenemo ndayikamo Bokosi la Chipangano, mmene muli pangano la Yehova limene anapangana ndi ana a Israeli.”
12 Eka Solomon nochungʼ e nyim kendo mar misango mar Jehova Nyasaye e nyim oganda duto mar jo-Israel kendo norieyo bedene kochomo malo.
Pamenepo Solomoni anayimirira patsogolo pa guwa lansembe la Yehova patsogolo pa gulu lonse la Aisraeli ndipo anakweza manja ake.
13 Noseloso raidhi mar mula ma borne gi lachne romo fut aboro to borne kadhi malo en fut abich mokete e dier laru ma oko. Ne ochungʼ e raidhino mi ogoyo chonge piny e nyim oganda duto mar jo-Israel kendo norieyo bedene kochomo polo.
Iyeyo anali atapanga nsanja yamkuwa, kutalika kwake kunali mamita awiri, mulifupi mwake munali mamita awiri, msinkhu wake unali mita imodzi ndi theka ndipo nsanjayo anayimika pakati pa bwalo lakunja. Iye anayimirira pa nsanjapo nagwada pamaso pa gulu lonse la Aisraeli ndipo anakweza manja ake kumwamba.
14 Kowacho niya, “Yaye Jehova Nyasaye ma Nyasach Israel, onge Nyasaye moro e polo kata e piny machal kodi. In e Nyasaye marito singruok mar herane ni jotichne maluwo yoreni gi chunygi duto.
Iye anati, “Inu Yehova, Mulungu wa Israeli, palibe Mulungu wofanana nanu kumwamba kapena pa dziko. Inu amene mumasunga pangano ndi kuonetsa chikondi chosasinthika kwa atumiki anu amene amayenda pamaso panu ndi mtima wawo wonse.
15 Iserito singruokni mane itimo gi jatichni Daudi wuora, ne isingori gi dhogi kendo isechopo singruokno gi lweti, mana kaka en kawuononi.
Inu mwasunga lonjezo lanu kwa abambo anga Davide, mtumiki wanu. Inde zimene munalonjeza ndi pakamwa panu, mwazikwaniritsa ndi manja anu monga mmene tikuonera lero lino.
16 “To koro Jehova Nyasaye ma Nyasach Israel rit singruok mane itimo gi jatichni Daudi wuora kiwachone niya, ‘Ok inibed maonge ngʼama bet e nyima e kom loch Israel ka nyikwayi onono kaka giwuotho e nyima kaka chikna dwaro mana kaka isetimo.’
“Ndipo tsopano, Inu Yehova Mulungu wa Israeli, sungani zimene munalonjeza kwa abambo anga Davide, mtumiki wanu pamene munati, ‘Sudzasowa munthu wokhala pamaso panga pa mpando waufumu wa Israeli, ngati ana ako adzasamalira mayendedwe awo ndi kusunga malamulo anga monga iwe wachitira.’
17 To koro, yaye Jehova Nyasaye ma Nyasach Israel yie mondo wach mane isingo ni jatichni Daudi wuora otimre mana kaka ne isingo.
Ndipo tsopano Inu Yehova, Mulungu wa Israeli, lolani kuti mawu anu akwaniritsidwe amene munalonjeza mtumiki wanu Davide.
18 “To bende Nyasaye nyalo dak e piny kod ji? Kata polo malo kata polo mabor ok nyal romi, to koro hekalu mageroni to diromi nade!
“Kodi Mulungu angakhaledi pa dziko lapansi ndi munthu? Mlengalenga ngakhale kumwamba kwenikweni sikungakukwaneni. Nanga kuli bwanji ndi Nyumba iyi imene ndamanga!
19 Kata kamano chik iti ni lamo jatichni gi kwayone mar ngʼwono yaye Jehova Nyasaye Nyasacha. Winji ywak gi lemo ma jatichni lamo e nyimi.
Koma Inu Yehova, Mulungu wanga, imvani pemphero ndi pembedzero la mtumiki wanu. Imvani kulira ndi pemphero la mtumiki wanu limene ndikupempha pamaso panu.
20 Mad wangʼi rang hekaluni odiechiengʼ kod otieno, kama niwacho ni Nyingi nobedie. Yie iwinji lemo ma jatichni lamo kochomo odni.
Maso anu azikhala otsekuka kuyangʼana Nyumba ino usana ndi usiku, malo ano amene Inu munati mudzayikamo Dzina lanu, imvani pemphero la mtumiki wanu limene akupemphera pa malo ano.
21 Winji lamo mar jatichni kaachiel gi jogi Israel ka gilamo ka gichomo odni. Winji gi e polo kar dakni kendo kiwinjo to iwenwa richowa.
Imvani mapembedzero a mtumiki wanu ndi a anthu anu Aisraeli pamene akupemphera akuyangʼana malo ano. Imvani kumwambako, malo anu amene mumakhala; ndipo mukamva muzitikhululukira.
22 “Ka ngʼato oketho ni wadgi kendo dwarore ni mondo okwongʼre kendo obiro mokwongʼore e nyim kendo mar misango manie hekaluni,
“Munthu akalakwira mnzake, nawuzidwa kuti alumbire, akabwera kudzalumbira patsogolo pa guwa lansembe la Nyumba ino,
23 to iwinji gi e polo kendo itim kaka owinjore. Ngʼad bura e kind jotichni kikumo joketho kendo iket richogi e wigi bende joma onge ketho iket kare kaluwore gi timgi makare.
imvani kumwambako ndi kuchitapo kanthu. Weruzani atumiki anuwo, wochimwa mugamule kuti ndi wolakwa ndipo alangidwe chifukwa cha zimene wachita. Wosachimwa mugamule kuti wosalakwa, ndipo muonetse kusalakwa kwakeko.
24 “Ka jogi Israel olo e lweny gi jowasikgi nikech gisekethoni to bangʼe gilokore mi gipako nyingi, ka gilamo kendo gikwayo e hekaluni,
“Anthu anu Aisraeli akagonja kwa adani awo chifukwa akuchimwirani ndipo akatembenukira kwa Inu ndi kuvomereza Dzina lanu, kupemphera ndi kupembedzera pamaso panu mʼNyumba ino,
25 to iwinjgi gi e polo kendo iwe richo jogi Israel kendo iduog-gi e piny mane imiyogi kod kweregi.
pamenepo imvani kumwambako ndi kukhululukira tchimo la anthu anu Aisraeli ndi kuwabweretsa ku dziko limene munawapatsa iwo ndi makolo awo.
26 “Ka polo olor kendo koth onge nikech jogi osekethoni to ka gilemo kaeni ka gipako nyingi kendo ka gilokore giweyo richogi nikech isekelonegi chandruok,
“Pamene kumwamba kwatsekeka ndipo mvula sikugwa chifukwa anthu anu akuchimwirani, ndipo pamene apemphera akuyangʼana malo ano ndi kuvomereza Dzina lanu ndi kutembenuka kuchoka ku machimo awo chifukwa inu mwawalanga,
27 to yie mondo iwinjgi gie polo kendo iwene jotichni ma jo-Israel richogi. Puonjgi yo makare mar dak kendo iornegi koth e piny mane imiyo jogi kaka girkeni margi.
pamenepo imvani kumwambako ndipo muwakhululukire atumiki anu, anthu anu Aisraeli. Aphunzitseni makhalidwe oyenera, ndipo gwetsani mvula mʼdziko limene munapereka kwa anthu anu monga cholowa chawo.
28 “Ka kech kata dera omako piny kata ka abach omako cham kata tuo ewi dongo, kata ka bonyo kata kungu, kata ka jowasigu olworo miechgi madongo, kata ka midekre kata tuo omakogi,
“Pamene mʼdziko mwagwa njala kapena mliri, chinoni kapena chiwawu, dzombe kapena kapuchi, kapena pamene adani azungulira mzinda wawo wina uliwonse, kaya mavuto kapena matenda abwera,
29 to ka ngʼato kuom jogi ma jo-Israel olemo kata okwayi, ka gingʼeyo gima chando chunygi kod lit ka girieyo bedegi kochomo hekaluni,
ndipo wina aliyense mwa Aisraeli akapemphera kapena kukudandaulirani, aliyense wa iwo akadziwa masautso ake ndi ululu wake, ndi kukweza manja awo kuloza Nyumba ino,
30 to yie iwinji gie polo kama idakie. Wenegi richogi kendo tim ne ngʼato ka ngʼato gima owinjore gi gik motimo nikech ingʼeyo chunygi (nikech in kendi ema ingʼeyo chuny dhano),
pamenepo imvani kumwambako, malo anu wokhalamo. Khululukani ndipo muchitire aliyense molingana ndi zonse zimene anachita popeza Inu mumadziwa mtima wake, (pakuti ndinu nokha amene mumadziwa mitima ya anthu),
31 mondo omi gilwori kendo giwuoth e yoreni ndalogi duto ma gin-go e piny mane imiyo kwerewa.
motero iwo adzakuopani ndipo adzayenda mʼnjira zanu masiku onse amene adzakhale mʼdziko limene munalipereka kwa makolo athu.
32 “To kuom jadak ma ok achiel kuom jogi Israel moa e piny mabor nikech nyingi maduongʼ kendo lweti maratego kod badi marabora moriere, ka gibiro ma gilemo ka gichomo hekaluni,
“Ndipo kunena za mlendo amene si mmodzi wa anthu anu Aisraeli, koma wabwera kuchokera ku dziko lakutali chifukwa cha dzina lanu lotchukali, ndiponso za dzanja lanu lamphamvu ndi lochita zazikulu, kudzapemphera akuyangʼana Nyumba ino,
33 to yie mondo iwinji gie polo kama idakie kendo tim gimoro amora ma jadakno okwayi mondo ogendini duto mag piny ongʼe nyingi kendo oluori mana kaka jogi Israel kendo mondo gingʼe ni ot ma asegeroni luongo nyingi.
pamenepo imvani kumwambako, malo anu okhalamo, ndipo muchite zonse zimene mlendoyo akukupemphani, kotero kuti anthu onse a dziko lapansi adziwe dzina lanu ndi kukuopani monga amachitira anthu anu Aisraeli, ndipo adziwe kuti nyumba ino imene ndakumangirani imadziwika ndi dzina lanu.
34 “Ka jogi odhi kedo gi jowasikgi kamoro amora ma ibiro orogie ka gilami kagichomo dalani miseyiero kendo hekalu masegero maluongo nyingi,
“Anthu akapita ku nkhondo kukamenyana ndi adani awo, kulikonse kumene mungawatume, ndipo akapemphera moyangʼana mzinda uno umene mwausankha ndi Nyumba yanu imene ndakumangirani,
35 to yie iwinji gie polo lamogi kod kwayogi kendo konygi.
pamenepo imvani kumwamba pemphero lawo ndi kupempha kwawo ndipo muwapulumutse.
36 “To ka giketho e nyimi, nimar onge ngʼato kata achiel ma ok jaketho mi ikecho kodgi kendo ichiwogi e lwet wasigu mi giterogi e twech e piny mabor kata machiegni,
“Pamene achimwira inu, pakuti palibe amene sachimwa, ndipo inu mwawakwiyira ndi kuwapereka kwa adani awo, amene awatenga ukapolo ku dziko lawo lakutali kapena pafupi.
37 kendo ka chunygi olokore e piny mane otergi e twech kendo giweyo richogi kendo gikwayi e piny wasikgi mane otweyogi kagiwacho niya, ‘Wasetimo richo kendo waseketho bende wasetimo mamono;’
Ngati asintha mitima yawo ku dziko limene ali akapolo ndi kulapa ndi kukudandaulirani inu mʼdziko la ukapolo wawo ndi kunena kuti, ‘Ife tachimwa, tachita zolakwa ndipo tachita moyipa kwambiri.’
38 to ka gidwogo iri gi chunygi duto kod ngimagi duto e piny mane otergi e twech, kendo gilemo ka girango pinygi mane imiyo kweregi, kod dala maduongʼ miseyiero kod hekalu ma asegero ni nyingi,
Ndipo ngati atembenukira kwa inu ndi mtima ndi moyo wawo wonse mʼdziko lawo la ukapolo kumene anatengedwako ndi kupemphera moyangʼana dziko limene inu munalipereka kwa makolo awo, moyangʼana Nyumba yanu imene ndakumangirani;
39 to yie iwinji lemogi gi kwayogi gie polo kar dakni kendo ikonygi. Kendo iwe ni jogi mosetimo richo e nyimi.
pamenepo imvani kumwamba, malo anu okhala, pemphero lawo ndi kudandaula kwawo, ndipo muwapulumutse. Ndipo mukhululukire anthu anu, amene akuchimwirani.
40 “Koro Nyasacha, yie mondo wengegi oyawre kendo itgi mondo owinj maber lemo ma wachiwo kaeni.
“Tsono Inu Mulungu wanga, tsekulani maso anu ndi makutu anu kuti mumve mapemphero ochitikira pa malo ano.
41 “Yaye Jehova Nyasaye, koro chungʼ malo kendo idonj e kar yweyo,
“Tsopano dzukani Inu Yehova Mulungu, ndipo bwerani ku malo anu ampumulo,
42 Yaye Jehova Nyasaye, kik ikwed ngʼatno misewiro.
Inu Yehova Mulungu musamukane wodzozedwa wanu.

< 2 Weche Mag Ndalo 6 >