< 1 Samuel 28 >
1 E ndalogo jo-Filistia nochoko jolwenjgi mondo oked gi Israel. Akish nowacho ni Daudi niya, “Nyaka ingʼe ni in gi jogi udhi koda e lweny.”
Mʼmasiku amenewo Afilisti anasonkhanitsa ankhondo awo kuti akamenyane ndi Aisraeli. Akisi anawuza Davide kuti, “Udziwe kuti iwe pamodzi ndi anthu ako mudzapita nane ku nkhondo.”
2 Daudi nowachone niya, “To koro inine gi wangʼi gima jatiji nyalo timo.” Akish nodwoke niya, “Mano ber, abiro keti jaritna e ndalo duto mar ngimana.”
Davide anayankha kuti, “Tsono inu mudzaona zimene mtumiki wanune ndingachite.” Akisi anayankha kuti, “Chabwino ine ndidzakuyika iwe kukhala mlonda wanga moyo wako wonse.”
3 Samuel nosetho kendo Israel duto noywage mine giike e dalane man Rama. Saulo noseriembo ajuoke, gi jo-nyakalondo oa e piny.
Nthawi imeneyi nʼkuti Samueli atamwalira, ndipo Aisraeli onse anamulira namuyika mʼmanda ku mzinda wake wa Rama. Sauli anali atachotsa mʼdzikomo anthu owombeza mawula ndi woyankhula ndi mizimu ya anthu akufa.
4 Jo-Filistia nochokore mobiro mojot e Shunem, ka Saulo bende nochoko jo-Israel duto modhi ojot Gilboa.
Tsono Afilisti anasonkhana nabwera kudzamanga misasa yawo ku Sunemu. Nayenso Sauli anasonkhanitsa Aisraeli onse ndi kumanga misasa yawo ku Gilibowa.
5 Ka Saulo noneno jolwenj jo-Filistia luoro gi kihondko nomake.
Sauli ataona gulu lankhondo la Afilisti anaopa ndipo ananjenjemera kwambiri.
6 Nopenjo Jehova Nyasaye wach, to Jehova Nyasaye ne ok odwoke e yor lek kata gi Urim kata gi dho jonabi.
Choncho Sauli anafunsa nzeru kwa Yehova koma Yehova sanamuyankhe ngakhale kudzera mʼmaloto, kapena mwa Urimu ngakhalenso kudzera mwa aneneri.
7 Eka Saulo nowachone joma tiyone niya, “Dwarnauru dhako ma ja-nyakalondo, mondo adhi apenje wach.” Negidwoke niya, “Nitie moro Endor.”
Kenaka Sauli anawuza nduna zake kuti, “Mundipezere mkazi amene amawombeza mawula kuti ndipite ndikafunse kwa iye.” Nduna zakezo zinamuyankha kuti, “Alipo mkazi woyankhula ndi mizimu ya anthu akufa ku Endori.”
8 Mi Saulo notemo loko nenruokne korwako lewni mopogore opogore, eka en gi ji ariyo moko negidhi ir dhako ma ja-nyakalondo gotieno. Nowacho niya, “Penjna wach kuom chuny ngʼat motho kendo ikelna ngʼatno mabiro nyisi nyinge.”
Kotero Sauli anadzizimbayitsa navala zovala zachilendo. Tsono iye pamodzi ndi anthu awiri anapita nakafika kwa mkazi uja usiku, ndipo anamupempha kuti, “Chonde ndifunsireni nzeru kwa mizimu ya anthu akufa. Koma makamaka munditulutsire mzimu wa amene ndimutchule.”
9 Eka dhakono nowachone niya, “Chutho ingʼeyo gima Saulo nosetimo. Osetieko jo-nyakalondo gi ajuoke e piny. Angʼo momiyo ichiko obadho ne ngimana, mondo okelna tho?”
Koma mkaziyo anayankha kuti, “Ndithu inu mukudziwa chimene Sauli anachita. Paja iye anachotsa mʼdziko muno anthu onse owombeza ndi woyankhula ndi mizimu ya anthu akufa. Chifukwa chiyani mukutchera moyo wanga msampha kuti ndiphedwe?”
10 Saulo nokwongʼore gi nying Jehova Nyasaye niya, “Akwongʼora gi nying Jehova Nyasaye mangima ni ok nokumi kuom timo ma.”
Koma Sauli analonjeza mkaziyo molumbira nati, “Pali Yehova wamoyo, iweyo sudzalangidwa chifukwa cha zimenezi.”
11 Eka dhakoni nopenje niya, “En ngʼa ma idwaro mondo agolni?” Nowachne niya, “Golna Samuel.”
Kenaka mkaziyo anafunsa, “Ndikuyitanireni yani?” Iye anati, “Undiyitanire Samueli.”
12 Kane dhakono oneno Samuel noywak gi dwol maduongʼ mowachone Saulo niya, “Angʼo momiyo isewuonda? In Saulo!”
Pamene mkaziyo anaona Samueli anakuwa kwambiri, nawuza Sauli kuti, “Nʼchifukwa chiyani inu mwandipusitsa? Inu ndinu Sauli!”
13 Ruoth nowachone niya, “Kik ibed maluor. Angʼo ma ineno?” To dhakono nowachone niya, “Aneno chuny ngʼama nosetho kawuok e lowo.”
Mfumuyo inamuwuza kuti, “Usaope. Kodi ukuona chiyani?” Mkaziyo anayankha kuti, “Ndikuona mzimu ukutuluka pansi.”
14 To nopenje niya, “Ochalo nadi?” Nowachone niya, “Jaduongʼ moti morwako law abola ema wuok.” Eka Saulo nongʼeyo ni en Samuel, mi nokulore nyaka e lowo monindo piny e lowo auma.
Sauli anafunsa, “Kodi mzimuwo ukuoneka motani?” Mkaziyo anayankha kuti, “Amene akutuluka ndi munthu wokalamba ndipo wavala mkanjo.” Apo Sauli anadziwa kuti anali Samueli ndipo anawerama nagunditsa nkhope yake pansi.
15 Samuel nowachone Saulo niya, “Angʼo momiyo ichanda kimiyo awuok oko?” Saulo nodwoke niya, “An gi midhiero maduongʼ. Jo-Filistia osemonja kendo kedo koda, Nyasaye bende oseweya. Tinde ok odwoka, gi dwond jonabi kata e yor lek. Mano emomiyo aluongi ni mondo iwachna gima onego atim?”
Samueli anafunsa Sauli kuti, “Nʼchifukwa chiyani wandivutitsa pondiyitana kuti ndibwere kuno?” Sauli anayankha kuti, “Ine ndavutika kwambiri mʼmaloto. Afilisti akumenyana nane, ndipo Mulungu wandifulatira. Iye sakundiyankhulanso, ngakhale kudzera mwa aneneri kapena maloto. Choncho ndakuyitanani kuti mundiwuze zoti ndichite.”
16 Samuel nowacho niya, “Angʼo momiyo ipenja wach ka Jehova Nyasaye oseweyi mobedo jasiki?
Samueli anati, “Nʼchifukwa chiyani ukundifunsa ine, pakuti tsopano Yehova wakufulatira ndipo wasanduka mdani wako?
17 Jehova Nyasaye osetimo mana gima nakoroni. Jehova Nyasaye osegolo loch e lweti mi omiye achiel kuom jobathi ma en Daudi.
Yehova wakuchita zimene ananeneratu kudzera mwa ine. Yehova wachotsa ufumu mʼmanja mwako ndipo waupereka kwa mnansi wako, kwa Davide.
18 Nikech nidagi winjo Jehova Nyasaye kendo timo kaka nochiki mondo itim ne jo-Amalek mane en-go gi mirima maduongʼ, mano emomiyo Jehova Nyasaye osetimoni gini kawuono.
Yehova wachita zimenezi lero chifukwa sunamvere mawu ake ndipo sunawawonongeretu Aamaleki.
19 Jehova Nyasaye dhi chiwo jo-Israel kaachiel kodi ni jo-Filistia, kendo kiny in kod yawuoti unubed koda. Jehova Nyasaye biro chiwo jolweny mag Israel ni jo-Filistia.”
Yehova adzapereka ndithu iweyo pamodzi ndi Aisraeli kwa Afilisti. Ndipo mmawa iweyo ndi ana ako mudzakhala ndi ine kuno. Ndithu Yehova adzapereka gulu lankhondo la Aisraeli kwa Afilisti.”
20 To gisano Saulo nogore moriere piny ka luoro omake nikech weche Samuel. Tekre norumo nikech ne pok ochiemo odiechiengʼ ngima gi otieno.
Nthawi yomweyo Sauli anagwa pansi atadzazidwa ndi mantha chifukwa cha mawu a Samueli. Analibenso mphamvu, pakuti sanadye tsiku lonse.
21 Kane dhakono obiro ir Saulo moneno kaka nobwok malich, nowacho niya, “Ne, jatichni madhako osetimo gima ne ichike. Ne akawo ngimana ka nono kane atimo gima ne iwacho ni atim.
Mkazi uja tsono anasendera kufupi ndi Sauli, ndipo ataona kuti Sauli akuchita mantha, anamuwuza kuti, “Taonani, mdzakazi wanune ndakumverani. Ndayika moyo wanga pa chiswe ndipo ndamvera zimene munandiwuza.
22 Koro yie iwinj jatichni mondo iyiena amiyi chiemo moro minyalo chamo mondo iyud teko mar dok.”
Tsono inunso mumvere mawu a mdzakazi wanune. Mundilole kuti ndikupatseni ka buledi pangʼono kuti mukhale ndi mphamvu zoyendera pa ulendo wanu.”
23 Nodagi mowacho niya, “Ok nachiem.” To joge noriwore gi dhakono kamedo kwaye, mi nowinjogi. Noa malo e lowo mobet e kom.
Iye anakana ndipo anati, “Ayi, ine sindidya.” Koma nduna zake pamodzi ndi mkaziyo anamuwumiriza, ndipo anawamvera. Choncho anadzuka pansi nakhala pa bedi.
24 Dhakono ne nigi nyarwath machwe e ode, mine oyangʼe mapiyo piyo. Nokawo mogo, modwalo motedogo makati ma ok oketie thowi.
Mkaziyo anali ndi mwana wangʼombe wonenepa ndipo anamupha mwachangu. Anatenga ufa nawukanyanga ndipo anaphika buledi wopanda yisiti.
25 Eka noketo chiemo e nyim Saulo gi joge mine gichiemo. Bangʼe ne giwuok gotienono mi gidhi.
Tsono anapereka bulediyo kwa Sauli ndi nduna zake ndipo anadya. Pambuyo pake ananyamuka kupita kwawo usiku womwewo.