< Salme 150 >
1 Halleluja! Pris Gud i hans Helligdom, pris ham i hans stærke Hvælving,
Tamandani Yehova. Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika; mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.
2 pris ham for hans vældige Gerninger, pris ham for hans mægtige Storhed;
Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu; mutamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana.
3 pris ham med Hornets Klang, pris ham med Harpe og Citer,
Mutamandeni poyimba malipenga, mutamandeni ndi pangwe ndi zeze.
4 pris ham med Pauke og Dans, pris ham med Strengeleg og Fløjte,
Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina, mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.
5 pris ham med klingre Cymbler, pris ham med gjaldende Cymbler;
Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga, mutamandeni ndi ziwaya zolira kwambiri.
6 alt hvad der ånder, pris HERREN! Halleluja!
Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova. Tamandani Yehova.