< Nehemias 10 >

1 Den beseglede Skrivelse er underskrevet af: Statholderen Nehemias, Hakaljas Søn, og Zidkija,
Amene anasindikiza chidindo anali awa: Nehemiya, bwanamkubwa uja, mwana wa Hakaliya. Zedekiya,
2 Seraja, Azarja, Jirmeja,
Seraya, Azariya, Yeremiya
3 Pasjhur, Amarja, Malkija,
Pasuri, Amariya, Malikiya,
4 Hattusj, Sjebanja, Malluk,
Hatusi, Sebaniya, Maluki,
5 Harim, Meremot, Obadja,
Harimu, Meremoti, Obadiya,
6 Daniel, Ginneton, Baruk,
Danieli, Ginetoni, Baruki,
7 Mesjullam, Abija, Mijjamin,
Mesulamu, Abiya, Miyamini
8 Ma'azja, Bilgaj og Sjemaja det var Præsterne.
Maziya, Biligai ndi Semaya Awa anali ansembe.
9 Leviterne Jesua, Azanjas Søn, Binnuj af Henadads Sønner, Kadmiel
Alevi anali awa: Yesuwa mwana wa Azaniya, Binuyi wa fuko la Henadadi, Kadimieli,
10 og deres Brødre Sjebanja, Hodija, Kelita, Pelaja, Hanan,
ndi abale awo awa: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,
11 Mika, Rehob, Hasjabja,
Mika, Rehobu, Hasabiya,
12 Zakkur, Sjerebja, Sjebanja,
Zakuri, Serebiya, Sebaniya,
13 Hodija, Bani og Beninu.
Hodiya, Bani ndi Beninu.
14 Folkets Overhoveder Par'osj, Pahat-Moab, Elam, Zattu, Bani,
Atsogoleri a anthu anali awa: Parosi, Pahati-Mowabu, Elamu, Zatu, Bani,
15 Bunni Azgad, Bebaj,
Buni, Azigadi, Bebai,
16 Adonija, Bigvaj, Adin,
Adoniya, Bigivai, Adini,
17 Ater, Hizkija, Azzur,
Ateri, Hezekiya, Azuri,
18 Hodija, Hasjum, Bezaj,
Hodiya, Hasumu, Bezayi
19 Harif, Anatot, Nebaj,
Harifu, Anatoti, Nebayi,
20 Magpiasj, Mesjullam, Hezir,
Magipiyasi, Mesulamu, Heziri
21 Mesjezab'el, Zadok Jaddua,
Mesezabeli, Zadoki, Yaduwa
22 Pelatja, Hanan, Anaja,
Pelatiya, Hanani, Ananiya,
23 Hosea, Hananja, Hassjub,
Hoseya, Hananiya, Hasubu
24 Hallohesj, Pilha, Sjobek,
Halohesi, Piliha, Sobeki,
25 Rehum, Hasjabna, Ma'aseja,
Rehumu, Hasabiya, Maaseya,
26 Ahija, Hanan, Anan,
Ahiya, Hanani, Anani,
27 Malluk, Harim og Ba'ana.
Maluki, Harimu ndi Baana.
28 Og det øvrige Folk, Præsterne, Leviterne, Dørvogterne, Sangerne, Tempeltrællene og alle de, der har skilt sig ud fra Hedningerne for at holde sig til Guds Lov, med deres Hustruer, Sønner og Døtre, for så vidt de har Forstand til at fatte det,
Ife otsalafe, ndiye kuti ansembe, Alevi, alonda a ku Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu, onse amene anadzipatula pakati pa anthu a mitundu ina kuti atsate malamulo a Yehova, pamodzi ndi akazi athu, ana athu ndi onse amene ali ndi nzeru,
29 slutter sig til deres højere stående Brødre og underkaster sig Forbandelsen og Eden om at ville følge Guds Lov, der er givet os ved Guds Tjener Moses, og overholde og udføre alle HERRENs, vor Herres, Bud, Bestemmelser og Anordninger:
tikuphatikana ndi abale athu wolemekezeka, ndipo tikulonjeza molumbira kuti tidzayenda motsata malamulo a Mulungu amene anapereka kudzera mwa Mose mtumiki wa Mulungu. Tilonjeza kumvera ndi kutsata bwino mawu onse, miyambo yonse ndi malangizo onse a Yehova. Yehova atilange ngati sitidzachita zimenezi.
30 Vi vil ikke give Hedningerne i Landet vore Døtre eller tage deres Døtre til Hustruer for vore Sønner;
“Ife tikulonjeza kuti sitidzapereka ana athu aakazi kuti akwatiwe ndi amuna a mayiko ena kapena kutenga ana awo aakazi kuti akwatiwe ndi ana athu aamuna.
31 vi vil ikke på Sabbaten eller nogen Helligdag købe noget af Hedningerne i Landet, når de på Sabbaten kommer med deres Varer og al Slags Korn og falbyder det; vi vil hvert syvende År lade Landet ligge hen og give Afkald på enhver Fordring;
“Ngati anthu a mitundu ina abwera ndi zinthu za malonda, monga tirigu, kudzagulitsa pa tsiku la Sabata, sitidzawagula pa tsiku la Sabata kapena pa tsiku lina lililonse loyera. Pa chaka chilichonse cha chisanu ndi chiwiri tidzagoneka munda wosawulima ndipo tidzafafaniza ngongole zonse.
32 vi vil påtage os en årlig Skat på en Tredjedel Sekel til Tjenesten i vor Guds Hus,
“Tikulonjezanso molumbira kuti chaka ndi chaka tizipereka magalamu anayi a siliva kuti zithandize ntchito ya ku Nyumba ya Mulungu wathu.
33 til Skuebrødene, det daglige Afgrødeoffer, det daglige Brændoffer, Ofrene på Sabbaterne, Nymånedagene og Højtiderne, Helligofrene og Syndofrene til Soning for Israel og til alt Arbejde ved vor Guds Hus.
Ndalamayi izithandiza kulipirira buledi wa pa tebulo, chopereka cha chakudya cha nthawi zonse, zopereka zopsereza za nthawi zonse, zopereka za pa tsiku la Sabata, za pachikondwerero cha Mwezi Watsopano, za pa masiku a chikondwerero osankhika, zopereka za zinthu zopatulika, zopereka za nsembe yopepesera machimo a Aisraeli ndi ntchito ina iliyonse ya ku Nyumba ya Mulungu.
34 Hvad Brænde der ydes, har vi, Præsterne, Leviterne og Folket, kastet Lod om at bringe til vor Guds Hus, Fædrenehus for Fædrenehus, til fastsat Tid År efter År for at skaffe Ild på HERREN vor Guds Alter, som det er foreskrevet i Loven.
“Ife ansembe, Alevi ndi anthu onse, tachita maere kuti tidziwe pamene banja lathu lililonse lidzabweretsa ku nyumba ya Mulungu wathu pa nthawi yoyikika ya chaka zopereka za nkhuni zoyaka pa guwa lansembe la Yehova Mulungu wathu, monga momwe zinalembedwera mʼMalamulo.”
35 Vi vil År for År bringe Førstegrøden af vor Jord og af alle Frugttræer til HERRENs Hus,
“Tilonjezanso kuti tidzabwera ndi zipatso zoyamba kucha za mʼminda yathu ndi zipatso zoyamba kucha za mtengo uliwonse wa zipatso chaka ndi chaka kuti tidzapereke ku Nyumba ya Mulungu wathu.”
36 og vi vil bringe det førstefødte af vore Sønner og vort Kvæg, som det er foreskrevet i Loven, og det førstefødte af vort Hornkvæg og Småkvæg til vor Guds Hus til Præsterne, som gør Tjeneste i vor Guds Hus;
“Tidzabweranso nawo ku Nyumba ya Mulungu, kwa ansembe amene amatumikira ku Nyumba ya Mulungu ana athu aamuna oyamba kubadwa ndi ana angʼombe oyamba kubadwa monga zalembedwera mu Malamulo. Tidzaperekanso ana oyamba kubadwa a ziweto zathu ndi ana ankhosa oyamba kubadwa.”
37 og Førstegrøden af vort Grovmel og af Frugten af alle Slags Træer, af Most og Olie vil vi bringe til Kamrene i vor Guds Hus til Præsterne og Tienden af vore Marker til Leviterne. Leviterne samler selv Tienden ind i alle de Byer, hvor vi har vort Agerbrug;
“Ndiponso ku zipinda za Nyumba ya Mulungu wathu, kwa ansembe tidzaperekanso mtanda wathu wa buledi wa ufa ndi mphatso zina monga zipatso za mtengo uliwonse, vinyo ndi mafuta. Tidzaperekanso kwa alevi chakhumi cha mbewu zathu pakuti alevi ndiwo amasonkhanitsa chakhumi mʼmidzi yathu yonse.
38 og Præsten, Arons Søn, er til Stede hos Leviterne, når de indsamler Tienden; og Leviterne bringer Tiende af Tienden til vor Guds Hus, til Forrådshusets Kamre.
Wansembe, mdzukulu wa Aaroni azikhala pamodzi ndi Alevi pamene akulandira chakhumi. Ndipo Alevi azibwera ndi chakhumicho ku nyumba ya Mulungu wathu, kuzipinda zosungiramo chuma.”
39 Thi Israeliterne og Levis Efterkommere bringer Offerydelsen af Kornet, Mosten og Olien til Kamrene, hvor Helligdommens Kar og de tjenstgørende Præster, Dørvogterne og Sangerne er. Vi vil således ikke svigte vor Guds Hus.
Choncho Israeli, kuphatikiza zidzukulu za Alevi, azipititsa zopereka za tirigu, vinyo ndi mafuta ku zipinda zosungiramo katundu wopatulika, komanso kokhala ansembe amene akutumikira pamodzi ndi alonda a ku Nyumba ya Mulungu ndi anthu oyimba nyimbo. “Kwambiri ife sitidzaleka kusamala Nyumba ya Mulungu.”

< Nehemias 10 >