< Salme 87 >

1 Af Koras Sønner. En Salme. En Sang. Sin Stad, grundfæstet paa hellige Bjerge, har HERREN kær,
Salimo la Ana a Kora. Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
2 Zions Porte fremfor alle Jakobs Boliger.
Yehova amakonda zipata za Ziyoni kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
3 Der siges herlige Ting om dig, du Guds Stad. (Sela)
Za ulemerero wako zimakambidwa, Iwe mzinda wa Mulungu: (Sela)
4 Jeg nævner Rahab og Babel blandt dem, der kender HERREN, Filisterland, Tyrus og Kusj: en fødtes her, en anden der.
“Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni pakati pa iwo amene amandidziwa. Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi, ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’”
5 Men Zion kalder man Moder, der fødtes enhver, den Højeste holder det selv ved Magt.
Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti, “Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye, ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
6 HERREN tæller efter i Folkeslagenes Liste, en fødtes her, en anden der. (Sela)
Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina: “Uyu anabadwira mʼZiyoni.” (Sela)
7 Syngende og dansende siger de: »Alle mine Kilder er i dig!«
Oyimba ndi ovina omwe adzati, “Akasupe anga onse ali mwa iwe.”

< Salme 87 >