< Salme 41 >

1 Til Sangmesteren. En Salme af David.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Wodala ndi munthu amene amaganizira anthu osauka; Yehova amamuwombola pa nthawi yamsautso.
2 Salig den Mand, der tager sig af de svage, ham frelser HERREN paa Ulykkens Dag;
Yehova adzamuteteza ndi kusunga moyo wake; Yehova adzamudalitsa iye mʼdziko ndipo sadzamupereka ku zofuna za adani ake.
3 HERREN vogter ham, holder ham i Live, det gaar ham vel i Landet, han giver ham ikke i Fjendevold.
Yehova adzamuthandiza pamene akudwala ndipo adzamuchiritsa pa bedi lake la matenda.
4 Paa Sottesengen staar HERREN ham bi, hans Smertensleje gør du ham let.
Ndinati, “Inu Yehova, mundichitire chifundo; chiritseni pakuti ndakuchimwirani.”
5 Saa siger jeg da: Vær mig naadig, HERRE, helbred min Sjæl, jeg har syndet mod dig!
Adani anga mwankhwidzi amanena za ine kuti, “Kodi munthu ameneyu adzafa liti kuti ayiwalike?”
6 Mine Fjender ønsker mig ondt: »Hvornaar mon han dør og hans Navn udslettes?«
Pamene wina abwera kudzandiona, amayankhula mwachinyengo, pomwe mtima wake ukusonkhanitsa zachipongwe; kenaka iye amatuluka ndi kukalengeza kunja.
7 Kommer en i Besøg, saa fører han hyklerisk Tale, hans Hjerte samler paa ondt, og saa gaar han bort og taler derom.
Adani anga onse amanongʼonezana pamodzi kulimbana nane, iwo amalingalira zoyipa kwambiri za ine, ponena kuti,
8 Mine Avindsmænd hvisker sammen imod mig, alle regner de med, at det gaar mig ilde:
“Matenda owopsa amugwira; sadzaukapo pamalo pamene wagona.”
9 »En dødelig Sot har grebet ham; han ligger der — kommer aldrig op!«
Ngakhale bwenzi langa la pamtima amene ndinamudalira, iye amene amadya pamodzi ndi ine watukula chidendene chake kulimbana nane.
10 Endog min Ven, som jeg stolede paa, som spiste mit Brød, har løftet Hælen imod mig.
Koma Yehova mundichititre chifundo, dzutseni kuti ndiwabwezere.
11 Men du, o HERRE, vær mig naadig og rejs mig, saa jeg kan øve Gengæld imod dem.
Ine ndikudziwa kuti mukukondwera nane, pakuti mdani wanga sandigonjetsa.
12 Deraf kan jeg kende, at du har mig kær, at min Fjende ikke skal juble over mig.
Mu ungwiro wanga Inu mumandisunga ndi kundiyimika pamaso panu kwamuyaya.
13 Du holder mig oppe i Kraft af min Uskyld, lader mig staa for dit Aasyn til evig Tid. Lovet være HERREN, Israels Gud, fra Evighed og til Evighed, Amen, Amen!
Atamandike Yehova Mulungu wa Israeli kuchokera muyaya mpaka muyaya. Ameni ndi Ameni.

< Salme 41 >