< Første Krønikebog 25 >
1 Derpaa udskilte David og Hærførerne til Tjenesten Asafs, Hemans og Jedutuns Sønner, som i profetisk Henrykkelse spillede paa Citre, Harper og Cymbler; og Tallet paa de Mænd, der havde med denne Tjeneste at gøre, var:
Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
2 Af Asafs Sønner: Zakkur, Josef, Netanja og Asar'ela, Asafs Sønner under Ledelse af Asaf, der spillede i profetisk Henrykkelse under Kongens Ledelse.
Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
3 Af Jedutun: Jedutuns Sønner Gedalja, Jizri, Jesja'ja, Sjim'i, Hasjabja og Mattitja, seks, under Ledelse af deres Fader Jedutun, der i profetisk Henrykkelse spillede paa Citer, naar HERREN blev lovet og priset.
Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
4 Af Heman: Hemans Sønner Bukkija, Mattanja, Uzziel, Sjubael, Jerimot, Hananja, Hanani, Eliata, Giddalti, Romamti-Ezer, Josjbekasja, Malloti, Hotir og Mahaziot.
Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
5 Alle disse var Sønner af Heman, Kongens Seer i Guds Ord; for at løfte hans Horn gav Gud Heman fjorten Sønner og tre Døtre.
Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
6 Alle disse spillede under deres Faders Ledelse ved Sangen i HERRENS Hus paa Cymbler, Harper og Citre for saaledes at gøre Tjeneste i Guds Hus under Ledelse af Kongen, Asaf, Jedutun og Heman.
Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
7 Deres Tal, sammenregnet med deres Brødre, der var oplært til at synge HERRENS Sange, var 288, kyndige Folk til Hobe.
Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
8 De kastede Lod om Ordningen af Tjenesten med lige Kaar baade for smaa og for store, Mestre og Lærlinge.
Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
9 Det første Lod traf Josef, ham selv med hans Brødre og Sønner, tolv; det andet Gedalja, ham selv med hans Brødre og Sønner, tolv;
Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
10 det tredje Zakkur, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
11 det fjerde Jizri, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
12 det femte Netanja, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
13 det sjette Bukkija, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
14 det syvende Jesar'ela, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
15 det ottende Jesja'ja, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
16 det niende Mattanja, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
17 det tiende Sjim'i, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
18 det ellevte Uzziel, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
19 det tolvte Hasjabja, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
20 det trettende Sjubael, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
21 det fjortende Mattitja, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
22 det femtende Jeremot, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
23 det sekstende Hananja, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
24 det syttende Josjbekasja, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
25 det attende Hanani, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
26 det nittende Malloti, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
27 det tyvende Eliata, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
28 det een og tyvende Hotir, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
29 det to og tyvende Giddalti, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
30 det tre og tyvende Mahaziot, hans Sønner og Brødre, tolv;
Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
31 det fire og tyvende Romamti-Ezer, hans Sønner og Brødre, tolv.
Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.