< Salme 52 >
1 Til Sangmesteren; en Undervisning af David,
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe, ndakatulo ya Davide; pamene Doegi Mwedomu anapita kwa Sauli ndi kunena kuti “Davide wapita ku nyumba ya Ahimeleki.” Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira ndi zoyipa, iwe munthu wamphamvu? Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira tsiku lonse, iwe munthu wochititsa manyazi pamaso pa Mulungu?
2 der Edomiteren Doeg kom med Underretning til Saul og sagde til ham: David er kommen i Akimeleks Hus.
Tsiku lonse umakhalira kuganizira za kuwononga ena; lilime lako lili ngati lumo lakuthwa, ntchito yako nʼkunyenga.
3 Hvorfor roser du dig af Ondskab, du vældige? Guds Miskundhed varer den ganske Dag.
Iwe umakonda choyipa mʼmalo mwa kuyankhula choonadi. Umakonda kunama kupambana kuyankhula zoona. (Sela)
4 Paa idel Skade arbejder din Tunge, som en skærpet Ragekniv, du, som øver Svig!
Umakonda mawu onse opweteka, iwe lilime lachinyengo!
5 Du elsker ondt mere end godt, Løgn fremfor at tale Retfærdighed. (Sela)
Zoonadi Mulungu adzakutsitsa kupita ku chiwonongeko chamuyaya: iye adzakukwatula ndi kukuchotsa mʼtenti yako; iye adzakuzula kuchoka mʼdziko la amoyo.
6 Du elsker alle fordærvelige Ord, du svigefulde Tunge!
Olungama adzaona zimenezi ndi kuchita mantha; adzamuseka nʼkumanena kuti,
7 Men Gud skal og nedbryde dig for evig Tid; han skal borttage dig og udrydde dig af Teltet, ja, oprykke dig med Rode af de levendes Land. (Sela)
“Pano tsopano pali munthu amene sanayese Mulungu linga lake, koma anakhulupirira chuma chake chambiri nalimbika kuchita zoyipa!”
8 Og de retfærdige skulle se det og frygte og spotte over ham og sige:
Koma ine ndili ngati mtengo wa olivi wobiriwira bwino mʼnyumba ya Mulungu; ndimadalira chikondi chosatha cha Mulungu kwa nthawi za nthawi.
9 Se der den Mand, som ikke holdt Gud for sin Styrke, men forlod sig paa sin megen Rigdom, blev stærk ved sin Ondskab! Men jeg er som et grønt Olietræ i Guds Hus; jeg forlader mig paa Guds Miskundhed evindelig og altid. Jeg vil takke dig evindelig, thi du gjorde det; og jeg vil bie efter dit Navn — thi det er godt — i Paasyn af dine hellige.
Ine ndidzakutamandani kwamuyaya chifukwa cha zimene mwachita; chifukwa cha zimene mwachita; mʼdzina lanu ndidzayembekezera pakuti dzina lanulo ndi labwino. Ndidzakutamandani pamaso pa oyera mtima anu.