< Salme 48 >

1 En Sang, en Psalme af Koras Børn.
Nyimbo. Salimo la ana a Kora. Wamkulu ndi Yehova, ndi woyenera kwambiri matamando mu mzinda wa Mulungu wathu, phiri lake loyera.
2 Herren er stor og saare priselig, i vor Guds Stad, paa hans hellige Bjerg.
Lokongola mu utali mwake, chimwemwe cha dziko lonse lapansi. Malo aatali kwambiri a Zafoni ndiye Phiri la Ziyoni, mzinda wa Mfumu yayikulu.
3 Zions Bjerg hæver sig smukt, er det ganske Lands Glæde, yderst imod Nord, den store Konges Stad.
Mulungu ali mu malinga ake; Iye wadzionetsa yekha kuti ndiye malinga akewo.
4 Gud i dens Paladser er kendt som en fast Borg.
Pamene mafumu anasonkhana pamodzi, pamene anayendera pamodzi kudzalimbana nafe,
5 Thi se, Kongerne havde samlet sig; de forsvandt til Hobe.
iwo anaona mzindawo ndipo anadabwa kwambiri; anathawa ndi mantha aakulu.
6 De saa, straks forundrede de sig; de forfærdedes, de hastede bort.
Pomwepo anagwidwa nako kunjenjemera, ululu wonga wa mkazi woyembekezera pa nthawi yochira.
7 Bævelse betog dem der, Angest som en Kvindes, der føder.
Inu munawawononga monga sitima zapamadzi za ku Tarisisi zitawonongeka ndi mphepo ya kummawa.
8 Ved Østenvejr sønderbryder du Tharsis's Skibe.
Monga momwe tinamvera, kotero ife tinaona mu mzinda wa Yehova Wamphamvuzonse, mu mzinda wa Mulungu wathu. Mulungu adzawuteteza kwamuyaya.
9 Ligesom vi havde hørt, saaledes saa vi det i den Herre Zebaoths Stad, i vor Guds Stad; Gud befæster den indtil evig Tid. (Sela)
Mʼkati mwa Nyumba yanu Mulungu, ife timalingaliramo zachikondi chanu chosasinthika.
10 O Gud! vi tænke paa din Miskundhed midt i dit Tempel.
Monga dzina lanu, Inu Mulungu, matamando anu amafika ku malekezero a dziko lapansi dzanja lanu lamanja ladzaza ndi chilungamo.
11 O Gud! som dit Navn er, saa er din Pris indtil Jordens Ender; din højre Haand er fuld af Retfærdighed.
Phiri la Ziyoni likukondwera, midzi ya Yuda ndi yosangalala chifukwa cha maweruzo anu.
12 Zions Bjerg glæder sig, Judas Døtre fryde sig for dine Dommes Skyld.
Yendayendani mu Ziyoni, uzungulireni mzindawo, werengani nsanja zake.
13 Gaar omkring Zion, rundt omkring den, tæller dens Taarne!
Yangʼanitsitsani bwino mipanda yake, penyetsetsani malinga ake, kuti mudzafotokoze za izo ku mʼbado wotsatira.
14 Lægger Mærke til dens Mur, betragter nøje dens Paladser, at I kunne fortælle det for den Slægt, som kommer. Thi her er Gud, vor Gud, evindelig og altid, han skal ledsage os til evige Tider.
Pakuti Mulungu uyu ndi Mulungu wathu ku nthawi zosatha; Iye adzakhala mtsogoleri wathu mpaka ku mapeto.

< Salme 48 >