< Salme 44 >
1 Til Sangmesteren; af Koras Børn; en Undervisning.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Ndakatulo ya ana a Kora. Ife tamva ndi makutu athu, Inu Mulungu; makolo athu atiwuza zimene munachita mʼmasiku awo, masiku akalekalewo.
2 Gud! vi have hørt det med vore Øren, vore Fædre have fortalt os det, den Gerning du gjorde i deres Dage, i fordums Dage.
Ndi dzanja lanu munathamangitsa mitundu ya anthu ena ndi kudzala makolo athu; Inu munakantha mitundu ya anthu, koma makolo athuwo Inu munawapatsa ufulu.
3 Du fordrev Hedningerne ved din Haand, men dem plantede du; du handlede ilde med Folkene, men dem udbredte du.
Sanalande dziko ndi lupanga lawo, si mkono wawo umene unawabweretsera chigonjetso, koma ndi dzanja lanu lamanja, mkono wanu ndi kuwala kwa nkhope yanu, pakuti munawakonda.
4 Thi ikke ved deres Sværd indtoge de Landet, og deres Arm hjalp dem ikke, men din højre Haand og din Arm og dit Ansigts Lys, fordi du havde Behagelighed til dem.
Inu ndinu Mfumu yanga ndi Mulungu wanga amene mumalamulira chigonjetso cha Yakobo.
5 Gud! du, ja, du er min Konge; befal Jakobs Frelse at komme!
Kudzera kwa inu ife timabweza adani athu; kudzera mʼdzina lanu timapondereza otiwukirawo.
6 Ved dig ville vi nedstøde vore Fjender; i dit Navn ville vi nedtræde dem, som staa op imod os.
Sindidalira uta wanga, lupanga langa silindibweretsera chigonjetso;
7 Thi jeg forlader mig ikke paa min Bue, og mit Sværd kan ikke frelse mig.
koma Inu mumatigonjetsera adani athu, mumachititsa manyazi amene amadana nafe.
8 Men du har frelst os fra vore Fjender, og du har beskæmmet dem, som os hadede.
Timanyadira mwa Mulungu wathu tsiku lonse, ndipo tidzatamanda dzina lanu kwamuyaya.
9 Vi prise Gud den ganske Dag, og vi takke dit Navn evindelig. (Sela)
Koma tsopano mwatikana ndi kutichepetsa; Inu simupitanso ndi ankhondo athu.
10 Alligevel har du forkastet os og ladet os beskæmmes og vil ikke drage ud med vore Hære.
Munachititsa ife kubwerera mʼmbuyo pamaso pa mdani ndipo amene amadana nafe atilanda katundu.
11 Du lader os vige tilbage for Modstanderen, og de, som os hade, have gjort sig Bytte.
Inu munatipereka kuti tiwonongedwe monga nkhosa ndipo mwatibalalitsa pakati pa anthu a mitundu ina.
12 Du giver os hen som Faar til at fortæres og har spredt os iblandt Hedningerne.
Inu munagulitsa anthu anu pa mtengo wotsika, osapindulapo kanthu pa malondawo.
13 Du sælger dit Folk, og det for intet, og du fik ingen stor Pris for dem.
Mwachititsa kuti tikhale chochititsa manyazi kwa anthu a mitundu ina, chonyozeka ndi chothetsa nzeru kwa iwo amene atizungulira.
14 Du gør os til Skændsel for vore Naboer, til Spot og Haan for dem, som ere trindt omkring os.
Mwachititsa kuti tikhale onyozeka pakati pa anthu a mitundu ina; anthu amapukusa mitu yawo akationa.
15 Du gør os til et Ordsprog iblandt Hedningerne, saa man ryster Hovedet over os iblandt Folkene.
Manyazi anga ali pamaso panga tsiku lonse ndipo nkhope yanga yaphimbidwa ndi manyazi
16 Min Forsmædelse er den ganske Dag for mig, og Bluelse har bedækket mit Ansigt
chifukwa cha mawu otonza a iwo amene amandinyoza ndi kundichita chipongwe, chifukwa cha mdani amene watsimikiza kubwezera.
17 for hans Røsts Skyld, som bespotter og forhaaner, for Fjendens og den hævngerriges Skyld.
Zonsezi zinatichitikira ngakhale kuti ifeyo sitinayiwale Inu kapena kuonetsa kusakhulupirika pa pangano lanu.
18 Alt dette er kommet over os, dog have vi ikke glemt dig, og vi have ikke handlet falskelig imod din Pagt.
Mitima yathu sinabwerere mʼmbuyo; mapazi athu sanatayike pa njira yanu.
19 Vort Hjerte vendte sig ikke bort, og vor Gang bøjede ikke af fra din Vej,
Koma Inu mwatiphwanya ndi kuchititsa kuti tikhale ozunzidwa ndi ankhandwe ndipo mwatiphimba ndi mdima waukulu.
20 saa at du skulde knuse os i Dragers Bo og skjule os med Dødens Skygge.
Tikanayiwala dzina la Mulungu wathu kapena kutambasulira manja athu kwa mulungu wachilendo,
21 Dersom vi havde glemt vor Guds Navn og udbredt vore Hænder til en fremmed Gud,
kodi Mulungu wathu sakanazidziwa zimenezi, pakuti Iye amadziwa zinsinsi zamumtima?
22 skulde Gud da ikke udfinde det? efterdi han kender Hjertets skjulte Tanker.
Komabe chifukwa cha Inu timakumana ndi imfa tsiku lonse, tili ngati nkhosa zoyenera kuti ziphedwe.
23 Men vi blive ihjelslagne for din Skyld den ganske Dag, vi ere regnede som Slagtefaar.
Dzukani Ambuye! Nʼchifukwa chiyani mukugona! Dziwutseni nokha! Musatikane kwamuyaya.
24 Vaagn op, hvorfor vil du sove, Herre? Vaagn op, forkast os ikke evindelig!
Nʼchifukwa chiyani mukubisa nkhope yanu, ndi kuyiwala mavuto athu ndi kuponderezedwa kwathu?
25 Hvorfor vil du skjule dit Ansigt, glemme vor Elendighed og vor Trængsel?
Tatsitsidwa pansi mpaka pa fumbi; matupi athu amatirira pa dothi.
26 Thi vor Sjæl er nedbøjet i Støvet, vor Krop hænger ved Jorden. Rejs dig til vor Hjælp og forløs os for din Miskundheds Skyld!
Imirirani ndi kutithandiza, tiwomboleni chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika.