< Salme 42 >
1 Til Sangmesteren; en Undervisning; af Koras Børn.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Ndakatulo ya ana a Kora. Monga mbawala ipuma wefuwefu kufunafuna mitsinje yamadzi, kotero moyo wanga upuma wefuwefu kufunafuna Inu Mulungu.
2 Ligesom en Hjort skriger efter Vandstrømme, saa skriger min Sjæl til dig, o Gud!
Moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Mulungu, lofuna Mulungu wamoyo. Kodi ndipite liti kukakumana ndi Mulungu?
3 Min Sjæl tørster efter Gud, efter den levende Gud; naar skal jeg dog komme og ses for Guds Ansigt?
Misozi yanga yakhala chakudya changa usana ndi usiku, pamene anthu akunena kwa ine tsiku lonse kuti, “Mulungu wako ali kuti?”
4 Min Graad er bleven mit Brød Dag og Nat, da man siger til mig den ganske Dag: Hvor er din Gud?
Zinthu izi ndimazikumbukira pamene ndikukhuthula moyo wanga: momwe ndinkapitira ndi gulu lalikulu, kutsogolera mayendedwe a ku Nyumba ya Mulungu ndi mfuwu yachimwemwe ndi mayamiko pakati pa anthu a pa chikondwerero.
5 Det vil jeg komme i Hu og udøse min Sjæl i mit Inderste: At jeg gik frem med Hoben og gik af Sted med den til Guds Hus, med Frydeskrigs- og Taksigelsesrøst, i den Hob, som holdt Højtid.
Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni, iwe moyo wanga? Nʼchifukwa chiyani wakhumudwa iwe mʼkati mwanga? Yembekezera Mulungu, pakuti ndidzamulambirabe, Mpulumutsi wanga ndi
6 Hvorfor nedbøjer du dig, min Sjæl, og bruser i mit Indre? bi efter Gud, thi jeg skal endnu takke ham for Frelsen for hans Ansigt.
Mulungu wanga. Moyo wanga uli ndi chisoni mʼkati mwanga kotero ndidzakumbukira Inu kuchokera ku dziko la Yorodani, ku mitunda ya Herimoni kuchokera ku phiri la Mizara.
7 Min Gud! min Sjæl nedbøjer sig i mit Inderste; derfor kommer jeg dig i Hu fra Jordans Land og Hermon, fra det lille Bjerg.
Madzi akuya akuyitana madzi akuya mu mkokomo wa mathithi anu; mafunde anu onse obwera mwamphamvu andimiza.
8 Afgrund raaber til Afgrund efter Lyden af dine Sluser, alle dine Brændinger og dine Bølger ere gaaede over mig.
Koma usana Yehova amalamulira chikondi chake, nthawi ya usiku nyimbo yake ili nane; pemphero kwa Mulungu wa moyo wanga.
9 Herren skal befale sin Miskundhed om Dagen, og om Natten skal hans Sang være hos mig, en Bøn til mit Livs Gud.
Ine ndikuti kwa Mulungu Thanthwe langa, “Nʼchifukwa chiyani mwandiyiwala? Nʼchifukwa chiyani ndiyenera kuyenda ndikulira, woponderezedwa ndi mdani?”
10 Jeg vil sige til Gud, min Klippe: Hvorfor har du glemt mig? hvorfor maa jeg gaa i Sørgeklæder, idet Fjenden trænger mig?
Mafupa anga ali ndi ululu wakufa nawo pamene adani anga akundinyoza, tsiku lonse akunena kuti, “Mulungu wako ali kuti?”
11 Under Dødssmerterne i mine Ben forhaane mine Fjender mig, idet de sige den ganske Dag til mig: Hvor er din Gud? Hvorfor nedbøjer du dig, min Sjæl? hvorfor bruser du i mit Indre? Bi efter Gud; thi jeg skal endnu takke ham, mit Ansigts Frelse og min Gud.
Bwanji ukumva chisoni, iwe mtima wanga? Chifukwa chiyani ukuvutika chonchi mʼkati mwanga? Khulupirira Mulungu, pakuti ndidzamutamandanso, Iye amene ali thandizo langa ndi Mulungu wanga.