< Salme 108 >
1 En Sang, en Psalme af David.
Nyimbo. Salimo la Davide. Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu; ndidzayimba nyimbo, inde ndidzayimba nyimbo zotamanda ndi moyo wanga wonse.
2 Trøstigt er mit Hjerte, o Gud! jeg vil synge, jeg vil lege paa Harpe, ogsaa min Ære skal juble.
Dzukani, zeze ndi pangwe! Ine ndidzadzutsa mʼbandakucha.
3 Vaagn op, Psalter og Harpe! jeg vil vække Morgenrøden.
Ndidzakutamandani Yehova, pakati pa anthu a mitundu ina; ndidzayimba za Inu pakati pa anthu a mitundu ina.
4 Jeg vil takke dig, Herre! iblandt Folkene og lege paa Harpe for dig iblandt Folkestammer.
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kutalika kwake kuposa kumwamba; kukhulupirika kwanu kumafika mlengalenga.
5 Thi din Miskundhed er stor over Himlene og din Sandhed indtil Skyerne.
Kwezekani Inu Mulungu, kuposa mayiko akumwamba, ndipo ulemerero wanu uphimbe dziko lonse lapansi.
6 Ophøj dig, Gud! over Himlene, og din Ære være over al Jorden!
Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja kuti iwo amene mumawakonda apulumutsidwe.
7 Paa det dine elskelige maa udfries, saa frels med din højre Haand og bønhør os!
Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika: “Mwachipambano Ine ndidzagawa Sekemu ndipo ndidzayesa chigwa cha Sukoti.
8 Gud har talt i sin Helligdom, jeg vil fryde mig; jeg vil uddele Sikem og opmaale Sukots Dal.
Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso; Efereimu ndi chipewa changa chodzitetezera, Yuda ndi ndodo yanga yaufumu.
9 Mig hører Gilead til, mig hører Manasse til, og Efraim er mit Hoveds Værn, Juda er min Herskerstav.
Mowabu ndi mbale yanga yosambiramo ndidzaponya nsapato zanga pa Edomu; ndidzafuwula mopambana pa Filisitiya.”
10 Moab er mit Vadskefad; jeg vil kaste min Sko til Edom; bryd ud i Jubel over mig, du Filisterland!
Ndani adzandifikitsa ku mzinda wotetezedwa? Ndani adzanditsogolera ku Edomu?
11 Hvo vil føre mig tilden faste Stad? hvo har ledet mig til Edom?
Kodi sindinu Mulungu, Inu amene mwatikana ndipo simuperekezanso magulu athu ankhondo?
12 Mon ikke du, Gud, som har forkastet os? og vil du, Gud, ikke uddrage med vore Hære?
Tithandizeni ife kulimbana ndi mdani, pakuti thandizo la munthu ndi lopanda pake.
13 Fly os Hjælp af Nød; thi Menneskers Hjælp er Forfængelighed. Ved Gud ville vi vinde Kraft; og han skal nedtræde vore Fjender.
Chifukwa cha Mulungu wathu, ife tidzapeza chipambano, ndipo adzapondereza pansi adani athu.