< Esajas 17 >

1 Profeti imod Damaskus. Se, Damaskus skal ikke mere være en Stad, men den skal være en sammenstyrtet Stenhob.
Uthenga wonena za Damasiko: “Taonani, mzinda wa Damasiko sudzakhalanso mzinda, koma udzasanduka bwinja.
2 Aroers Stæder skulle blive forladte; de skulle være for Hjorde, og disse skulle ligge der, og ingen skal forfærde dem.
Mizinda ya Aroeri idzakhala yopanda anthu ndipo idzakhala ya ziweto, zimene zidzagona pansi popanda wina woziopseza.
3 Og det skal være forbi med Befæstningen for Efraim og med Kongedømmet for Damaskus og for det overblevne af Syrerne; de skulle være som Israels Børns Herlighed, siger den Herre Zebaoth.
Ku Efereimu sikudzakhalanso linga, ndipo ku Damasiko sikudzakhalanso ufumu; Otsalira a ku Siriya adzachotsedwa ulemu monga anthu a ku Israeli,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
4 Og det skal ske paa den Dag, da skal Jakobs Herlighed blive ringe, og hans Køds Fedme skal blive mager.
“Tsiku limenelo ulemerero wa Yakobo udzazimirira; ndipo chuma chake chidzasanduka umphawi.
5 Og det skal gaa, som naar en Høstmand griber om det stagende Korn, og hans Arm høster Aksene; og det skal gaa, som naar een samler Aks i Refaims Dal.
Israeli adzakhala ngati munda wa tirigu umene anatsiriza kukolola. Adzakhalanso ngati munda wa mʼchigwa cha Refaimu anthu atatha kukunkha ngala za tirigu.
6 Og der skal blive en Efterslet tilovers derudi, som naar man ryster et Olietræ: To eller tre Bær i den øverste Top, fire eller fem paa de frugtbare Kviste, siger Herren, Israels Gud.
Komabe Aisraeli ochepa okha ndiwo ati adzatsale monga mʼmene zimatsalira zipatso ziwiri kapena zitatu pa nthambi ya pamwamba penipeni kapena zipatso zisanu pa nthambi za mʼmunsi mwa mtengo wa olivi akawugwedeza,” akutero Yehova, Mulungu wa Israeli.
7 Paa den Dag skal Mennesket se hen til den, som har skabt ham, og hans Øjne skulle se hen til den Hellige i Israel.
Tsiku limenelo anthu adzayangʼana Mlengi wawo ndipo adzatembenukira kwa Woyerayo wa Israeli.
8 Og han skal ikke se hen til Altrene, hans Hænders Gerning, og ikke se til det, som hans Fingre have gjort, hverken til Astartes eller Solens Billeder.
Iwo sadzakhulupiriranso maguwa ansembe, ntchito ya manja awo, ndipo sadzadaliranso mitengo ya mafano a Asera, ndiponso maguwa ofukizirapo lubani amene manja awo anapanga.
9 Paa den Dag skulle hans faste Stæder vorde som de forladte Skove og Højder, som man havde forladt for Israels Børns Skyld, og der skal blive en Ørk.
Tsiku limenelo mizinda yawo yamphamvu, imene anasiya chifukwa cha Aisraeli, idzakhala ngati malo osiyidwa kuti awirire ndi kumera ziyangoyango. Ndipo yonse idzakhala mabwinja.
10 Thi du har glemt din Frelses Gud og ikke ihukommet din Styrkes Klippe; derfor planter du liflige Plantninger og besætter din Vingaard med fremmede Ranker.
Inu mwayiwalatu Mulungu Mpulumutsi wanu; simunakumbukire Thanthwe, linga lanu. Choncho, ngakhale munadzala mbewu zabwino, ndi kuyitanitsa kunja mitengo ya mpesa,
11 Paa den Dag, du planter, gærder du derom, og om Morgenen bringer du din Sæd til at grønnes; men flygtet er Høsten paa Sygdommens og den ulægelige Smertes Dag.
nimuyembekeza kuti zikule tsiku lomwelo ndi kuphukira maluwa mmawa mwake, komabe zimenezi sizidzakupindulirani pa tsiku la mavuto.
12 Ve, en Brusen af mange Folkeslag! de bruse som Havets Brusen; og et Bulder af Folkefærd! de buldre, som mægtige Vande buldre.
Aa, mkokomo wa anthu a mitundu yambiri, akusokosa ngati kukokoma kwa nyanja! Aa, phokoso la anthu a mitundu ina, akusokosa ngati mkokomo wa madzi amphamvu!
13 Folkene buldre som store Vandes Bulder, men han truer dem, saa de fly langt bort; og de bortjages som Avner paa Bjergene for Vejret og som en Hvirvel for Hvirvelvind.
Ngakhale ankhondo a mitundu ina akubwera ndi mkokomo ngati wa madzi ambiri, koma adzathawira kutali Mulungu akadzawadzudzula. Yehova adzawapirikitsa ngati mankhusu owuluka ndi mphepo pa phiri, ndi ngati fumbi la kamvuluvulu asanayambe.
14 Ved Aftenstid — se, da er der Forskrækkelse! førend Morgenen kommer, da ere de ikke mere; dette er deres Del, som plyndre os, og deres Lod, som berøve os.
Pofika nthawi yamadzulo zoopsa zidzayamba kuchitika, ndipo zidzakhala zitatha pofika mmawa. Izi ndizo zidzachitikire anthu otilanda zinthu, gawo la amene amatibera zinthu zathu.

< Esajas 17 >