< Ester 10 >
1 Derefter lagde Kong Ahasverus Skat paa Landet og Øerne i Havet.
Mfumu Ahasiwero anakhometsa msonkho mʼdziko lake lonse mpaka ku zilumba zonse.
2 Men al hans Magt og hans Vældes Gerninger og Beretninger om Mardokajs Magt, som Kongen havde hævet ham til, ere de Ting ikke skrevne i Kongerne af Mediens og Persiens Krøniker?
Ndipo ntchito zonse zochitika ndi mphamvu zake komanso ndi zonse zofotokoza za ukulu wa Mordekai, kukwezedwa kwake ndi mfumu, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a ku Mediya ndi Peresiya?
3 Thi Jøden Mardokaj var den anden efter Kong Ahasverus og mægtig hos Jøderne og behagelig for sine Brødres Mangfoldighed, da han søgte sit Folks Vel og talte til Bedste for al sin Slægt.
Pakuti Mordekai Myuda uja anali wachiwiri wa mfumu Ahasiwero. Kwa Ayuda onse Mordekai anali munthu wamkulu ndipo ankamukonda chifukwa ankachitira zabwino mtundu wake ndi kufunira mtendere abale ake.