< Første Krønikebog 25 >

1 Og David og Stridshøvedsmændene udtoge til Tjeneste af Asafs og Hemans og Jeduthuns Børn dem, som skulde profetere med Harper og med Psaltre og med Cymbler, og Tallet paa Mændene efter deres Embedsgerning var:
Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
2 Af Asafs Børn: Sakur og Josef og Nathania og Asareela, Asafs Sønner, under Asaf, som profeterede efter Kongens Anvisning;
Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
3 af Jeduthun: Jeduthuns Sønner vare: Gedalja og Zeri og Jesaja og Hasabja og Mathithja, i alt seks, med Harper, under deres Fader Jeduthun, som profeterede ved at takke og love Herren;
Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
4 af Heman: Hemans Sønner vare: Bukkija, Mathanja, Ussiel, Sebuel og Jerimoth, Hananja, Hanani, Eliatha, Giddalthi og Romamthi-Eser, Josbekasa, Mallothi, Hothir, Mahasioth.
Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
5 Alle disse vare Sønner af Heman, Kongens Seer i Guds Ord, de skulde lade Hornet lyde; og Gud havde givet Heman fjorten Sønner og tre Døtre.
Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
6 Alle disse vare under deres Fædre ved Sangen i Herrens Hus, med Cymbler, Psaltre og Harper til Guds Hus's Tjeneste, efter Kongens, Asafs og Jeduthuns og Hemans Anvisning.
Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
7 Og deres Tal tillige med deres Brødres, som vare oplærte i Herrens Sang, alle Mestrene vare to Hundrede, otte og firsindstyve.
Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
8 Og de kastede Lod om, hvad de skulde tage Vare paa, saavel den yngste som den ældste, saavel Mesteren som Lærlingen.
Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
9 Og den første Lod kom ud for Asaf, nemlig for Josef; den anden for Gedalja, ham og hans Brødre og hans Sønner, i alt tolv;
Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
10 den tredje for Sakur, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
11 den fjerde for Jizri, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
12 den femte for Nethania, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
13 den sjette for Bukkija, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
14 den syvende for Isareela, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
15 den ottende for Jesaja, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
16 den niende for Mathanja, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
17 den tiende for Simei, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
18 den ellevte for Asareel, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
19 den tolvte for Hasabia, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
20 den trettende for Subael, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
21 den fjortende for Mathithja, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
22 den femtende for Jerimoth, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
23 den sekstende for Hananja, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
24 den syttende for Josbekasa, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
25 den attende for Hanani, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
26 den nittende for Mallothi, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
27 den tyvende for Eliatha, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
28 den en og tyvende for Hothir, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
29 den to og tyvende for Giddalthi, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
30 den tre og tyvende for Mahesioth, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv;
Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
31 den fire og tyvende for Romamthi-Eser, hans Sønner og hans Brødre, i alt tolv.
Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.

< Første Krønikebog 25 >