< Žalmy 88 >

1 Píseň a žalm synů Chóre, přednímu zpěváku na machalat k zpívání, vyučující, složený od Hémana Ezrachitského. Hospodine, Bože spasení mého, ve dne i v noci k tobě volám.
Salimo la ana a Kora. Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a nyimbo yoti: “Pa Matenda ndi pa Mazunzo.” Ndakatulo ya Hemani, wa banja la Ezara. Inu Yehova, Mulungu amene mumandipulumutsa, usana ndi usiku ndimalira pamaso panu.
2 Vstupiž před oblíčej tvůj modlitba má, nakloň ucha svého k volání mému.
Pemphero langa lifike pamaso panu; tcherani khutu lanu kuti mumve kulira kwanga.
3 Neboť jest naplněna trápeními duše má, a život můj až k hrobu se přiblížil. (Sheol h7585)
Pakuti ndili ndi mavuto ambiri ndipo moyo wanga ukuyandikira ku manda. (Sheol h7585)
4 Počten jsem mezi ty, kteříž se dostávají do jámy; připodobněn jsem člověku beze vší síly.
Ndikuwerengedwa pamodzi ndi iwo amene akutsikira ku dzenje; ndine munthu wopanda mphamvu.
5 Mezi mrtvé jsem odložen, jako zmordovaní ležící v hrobě, na něž nezpomínáš více, kteříž od ruky tvé vyhlazeni jsou.
Ndayikidwa pambali pamodzi ndi anthu akufa, monga ophedwa amene agona mʼmanda, amene Inu simuwakumbukiranso, amene achotsedwa pa chisamaliro chanu.
6 Spustils mne do jámy nejzpodnější, do nejtemnějšího a nejhlubšího místa.
Mwandiyika pansi pa dzenje penipeni, mʼmalo akuya a mdima waukulu.
7 Dolehla na mne prchlivost tvá, a vším vlnobitím svým přikvačil jsi mne. (Sélah)
Ukali wanu ukundipsinja kwambiri, mwandiopseza kwambiri ndi mafunde anu onse. (Sela)
8 Daleko jsi vzdálil mé známé ode mne, jimž jsi mne velice zošklivil, a tak jsem sevřín, že mi nelze nijakž vyjíti.
Mwandichotsa pakati pa abwenzi anga enieni ndipo mwachititsa kuti ndikhale chonyansa kwa iwo. Ndatsekerezedwa ndipo sindingathe kuthawa;
9 Zrak můj hyne trápením; na každý den vzývám tě, Hospodine, ruce své před tebou rozprostíraje.
maso anga ada ndi chisoni. Ndimayitana Inu Yehova tsiku lililonse; ndimakweza manja anga kwa Inu.
10 Zdali před mrtvými učiníš zázrak? Aneb vstanou-liž mrtví, aby tě oslavovali? (Sélah)
Kodi mumaonetsa zozizwitsa zanu kwa anthu akufa? Kodi iwo amene afa amaukanso ndi kutamanda Inu? (Sela)
11 I zdali bude ohlašováno v hrobě milosrdenství tvé, a pravda tvá v zahynutí?
Kodi chikondi chanu chimalalikidwa mʼmanda, za kukhulupirika kwanu ku malo a chiwonongeko?
12 Zdaliž v známost přichází ve tmách div tvůj, a spravedlnost tvá v zemi zapomenutí?
Kodi zozizwitsa zanu zimadziwika ku malo a mdima, kapena ntchito zanu zolungama ku dziko la anthu oyiwalika?
13 Já pak, Hospodine, k tobě volám, a každého jitra předchází tě modlitba má.
Inu Yehova, Ine ndimalirira thandizo; mmawa mapemphero anga amafika pamaso panu.
14 Pročež, ó Hospodine, zamítáš mne, a tvář svou skrýváš přede mnou?
Inu Yehova nʼchifukwa chiyani mukundikana ndi kundibisira nkhope yanu?
15 Ztrápený jsem, jako hned maje umříti od násilí; snáším hrůzy tvé, a děsím se.
Kuyambira ubwana wanga ndakhala ndikuzunzika pafupi kufa; ndakhala ndikuchita mantha ndipo ndine wothedwa nzeru.
16 Hněv tvůj přísný na mne se obořil, a hrůzy tvé krutě sevřely mne.
Ukali wanu wandimiza; zoopsa zanu zandiwononga.
17 Obkličují mne jako voda, na každý den obstupují mne hromadně.
Tsiku lonse zimandizungulira ngati chigumula; zandimiza kwathunthu.
18 Vzdálil jsi ode mne přítele a tovaryše, a známým svým jsem ve tmě.
Inu mwatenga anzanga ndi okondedwa anga kuwachotsa pamaso panga; mdima ndiye bwenzi langa lenileni.

< Žalmy 88 >