< Žalmy 87 >

1 Synům Chóre, žalm a píseň. Základ svůj na horách svatých.
Salimo la Ana a Kora. Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
2 Milujeť Hospodin, totiž brány Sionské, nade všecky příbytky Jákobovy.
Yehova amakonda zipata za Ziyoni kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
3 Přeslavnéť jsou to věci, kteréž se o tobě hlásají, ó město Boží. (Sélah)
Za ulemerero wako zimakambidwa, Iwe mzinda wa Mulungu: (Sela)
4 Připomínati budu Egypt a Babylon před svými známými, ano i Filistinské a Tyrské i Mouřeníny, že se tu každý z nich narodil.
“Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni pakati pa iwo amene amandidziwa. Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi, ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’”
5 An i o Sionu praveno bude: Ten i onen jest rodem z něho, sám pak Nejvyšší utvrdí jej.
Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti, “Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye, ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
6 Sečteť Hospodin při popisu národy, a dí, že tento se tu narodil. (Sélah)
Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina: “Uyu anabadwira mʼZiyoni.” (Sela)
7 Tou příčinou zpívají s plésáním o tobě všecky moci života mého.
Oyimba ndi ovina omwe adzati, “Akasupe anga onse ali mwa iwe.”

< Žalmy 87 >