< Žalmy 82 >

1 Žalm Azafův. Bůh stojí v shromáždění Božím, u prostřed bohů soud čině, a dí:
Salimo la Asafu. Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu; Iye akuweruza pakati pa “milungu.”
2 Dokudž souditi budete nespravedlivě, a osoby nešlechetných přijímati? (Sélah)
“Mudzateteza osalungama mpaka liti, ndi kukondera anthu oyipa?
3 Zastávejte bídného a sirotka, utištěného a chudého spravedliva vyhlašujte.
Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye; mukhazikitse ufulu wa anthu osauka ndi ozunzika.
4 Vytrhněte bídného a nuzného, z ruky nešlechetných vytrhněte ho.
Landitsani anthu ofowoka ndi osowa; apulumutseni mʼdzanja la anthu oyipa.
5 Ale nevědí nic, nerozumějí nic; ve tmách ustavně chodí, až se proto všickni základové země pohybují.
“Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse. Amayendayenda mu mdima; maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.
6 Řeklť jsem já byl: Bohové jste, a synové Nejvyššího vy všickni;
“Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu, nonsenu ndinu ana a Wammwambamwamba.’
7 A však jako i jiní lidé zemřete, a jako jeden z knížat padnete.
Koma mudzafa ngati anthu wamba; mudzagwa ngati wolamula wina aliyense.”
8 Povstaniž, ó Bože, suď zemi; nebo ty dědičně vládneš všemi národy.
Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, pakuti mayiko onse ndi cholowa chanu.

< Žalmy 82 >