< Žalmy 8 >

1 Přednímu zpěváku na gittejský nástroj, žalm Davidův. Hospodine Pane náš, jak důstojné jest jméno tvé na vší zemi! Nebo jsi vyvýšil slávu svou nad nebesa.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa gititi. Salimo la Davide. Inu Yehova Ambuye athu, dzina lanu ndi la lamphamvudi pa dziko lonse lapansi! Inu mwakhazikitsa ulemerero wanu mʼmayiko onse akumwamba.
2 Z úst nemluvňátek a těch, jenž prsí požívají, mocně dokazuješ síly z příčiny svých nepřátel, abys přítrž učinil protivníku a vymstívajícímu se.
Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda, Inu mwakhazikitsa mphamvu chifukwa cha adani anu, kukhazikitsa bata adani ndi anthu obwezera zoyipa.
3 Když spatřuji nebesa tvá, dílo prstů tvých, měsíc a hvězdy, kteréž jsi tak upevnil, říkám:
Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba, ntchito ya zala zanu, mwezi ndi nyenyezi, zimene mwaziyika pa malo ake,
4 Co jest člověk, že jsi naň pamětliv, a syn člověka, že jej navštěvuješ?
munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira, ndi mwana wa munthu kuti inu mumacheza naye?
5 Nebo učinil jsi ho málo menšího andělů, slávou a ctí korunoval jsi jej.
Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba ndipo mwamuveka ulemerero ndi ulemu.
6 Pánem jsi ho učinil nad dílem rukou svých, všecko jsi podložil pod nohy jeho:
Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu; munayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake;
7 Ovce i voly všecky, také i zvěř polní,
nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi ndi nyama zakuthengo,
8 Ptactvo nebeské, i ryby mořské, a cožkoli chodí stezkami mořskými.
mbalame zamlengalenga ndi nsomba zamʼnyanja zonse zimene zimayenda pansi pa nyanja.
9 Hospodine Pane náš, jak důstojné jest jméno tvé na vší zemi!
Inu Yehova, Ambuye athu, dzina lanu ndi lamphamvudi pa dziko lonse lapansi!

< Žalmy 8 >