< Žalmy 67 >

1 Přednějšímu z kantorů na neginot, žalm k zpívání. Bože, smiluj se nad námi, a požehnej nám, zasvěť oblíčej svůj nad námi, (Sélah)
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo. Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa, achititse kuti nkhope yake itiwalire.
2 Tak aby poznali na zemi cestu tvou, mezi všemi národy spasení tvé.
Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi, chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.
3 I budou tě oslavovati národové, ó Bože, oslavovati tě budou všickni lidé.
Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
4 Veseliti se a prozpěvovati budou národové; nebo ty souditi budeš lidi v pravosti, a národy spravovati budeš na zemi. (Sélah)
Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe, pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.
5 I budou tě oslavovati národové, ó Bože, oslavovati tě budou všickni lidé.
Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.
6 Země také vydá úrodu svou. Požehnání svého uděliž nám Bůh, Bůh náš;
Nthaka yabereka zokolola zake; tidalitseni Mulungu wathu.
7 Požehnej nás Bůh, a bojtež se jeho všecky končiny země.
Mulungu atidalitse kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.

< Žalmy 67 >