< Žalmy 4 >
1 Přednímu zpěváku na neginot, žalm Davidův. Když volám, vyslyš mne, Bože spravedlnosti mé. Ty jsi mi v úzkosti prostranství způsoboval, smiluj se nade mnou, a vyslyš modlitbu mou.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe wa zida za zingwe. Salimo la Davide. Ndiyankheni pamene ndiyitana Inu, Inu Mulungu wa chilungamo changa. Pumulitseni ku zowawa zanga; chitireni chifundo ndi kumva pemphero langa.
2 Synové lidští, dokudž sláva má v potupě bude? Dlouho-liž marnost milovati a lži hledati budete? (Sélah)
Anthu inu, mpaka liti mudzakhala mukusandutsa ulemerero wanga kukhala manyazi? Mpaka liti mudzakonda zachabe ndi kufuna milungu yabodza? (Sela)
3 Vězte, žeť jest oddělil Hospodin sobě milého. Vyslyšíť mne Hospodin, když k němu volati budu.
Dziwani kuti Yehova wadziyikira padera anthu okhulupirika; Yehova adzamva pamene ndidzamuyitana.
4 Uleknětež se a nehřešte, přemyšlujte o tom v srdci svém, na ložci svém, a umlkněte. (Sélah)
Kwiyani koma musachimwe; pamene muli pa mabedi anu, santhulani mitima yanu ndi kukhala chete. (Sela)
5 Obětujte oběti spravedlnosti, a doufejte v Hospodina.
Perekani nsembe zolungama ndipo dalirani Yehova.
6 Mnozí říkají: Ó bychom viděti mohli dobré věci. Hospodine, pozdvihni nad námi jasného oblíčeje svého,
Ambiri akufunsa kuti, “Ndani angationetse chabwino chilichonse?” Kuwunika kwa nkhope yanu kutiwalire, Inu Yehova.
7 I způsobíš radost v srdci mém větší, než oni mívají, když obilé a víno jejich se obrodí.
Inu mwadzaza mtima wanga ndi chimwemwe chachikulu kuposa kuchuluka kwa tirigu wawo ndi vinyo watsopano.
8 Jáť u pokoji i lehnu i spáti budu; nebo ty, Hospodine, sám způsobíš mi bydlení bezpečné.
Ine ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere, pakuti Inu nokha, Inu Yehova, mumandisamalira bwino.