< Žalmy 26 >

1 Žalm Davidův. Suď mne, Hospodine, nebo já v upřímnosti své chodím, a v tě Hospodina doufám, nepohnuť se.
Salimo la Davide. Weruzeni Inu Yehova pakuti ndakhala moyo wosalakwa. Ndadalira Yehova popanda kugwedezeka.
2 Zprubujž mne, Hospodine, a zkus mne, přepal ledví má i srdce mé.
Patseni mayeso, Inu Yehova ndipo ndiyeseni, santhulani mtima wanga ndi maganizo anga;
3 Milosrdenství tvé zajisté před očima mýma jest, a chodím stále v pravdě tvé.
pakuti chikondi chanu chili pamaso panga nthawi zonse, ndipo ndimayenda mʼchoonadi chanu nthawi zonse.
4 S lidmi marnými nesedám, a s pokrytci v spolek nevcházím.
Ine sindikhala pansi pamodzi ndi anthu achinyengo, kapena kufunsa nzeru kwa achiphamaso.
5 V nenávisti mám shromáždění zlostníků, a s bezbožnými se neusazuji.
Ndimanyansidwa ndi msonkhano wa anthu ochita zoyipa ndipo ndimakana kukhala pansi pamodzi ndi oyipa.
6 Umývám v nevinnosti ruce své, postavuji se při oltáři tvém, Hospodine,
Ndimasamba mʼmanja mwanga kuonetsa kusalakwa kwanga ndi kupita kukatumikira pa guwa lanu la nsembe, Inu Yehova,
7 Abych tě hlasitě chválil, a vypravoval všecky divné skutky tvé.
kulengeza mofuwula za matamando anu ndi kuwuza onse za ntchito zanu zodabwitsa.
8 Hospodine, jáť miluji obydlí domu tvého, a místo příbytku slávy tvé.
Ndimakonda Nyumba imene Inu Yehova mumakhalamo, malo amene ulemerero wanu umapezekako.
9 Nezahrnujž s hříšnými duše mé, a s lidmi vražedlnými života mého,
Musachotse moyo wanga pamodzi ndi ochimwa, moyo wanga pamodzi ndi anthu akupha anzawo,
10 V jejichž rukou jest nešlechetnost, a pravice jejich vzátků plná.
amene mʼmanja mwawo muli ndondomeko zoyipa, dzanja lawo lamanja ladzaza ndi ziphuphu.
11 Já pak v upřímnosti své chodím, vykupiž mne, a smiluj se nade mnou.
Koma ine ndimakhala moyo wosalakwa; mu msonkhano wa anthu anu ndidzatamanda Yehova.
12 Noha má stojí na rovině, v shromážděních svatých dobrořečiti budu Hospodinu.
Ndayima pa malo wopanda zovuta ndipo ndidzatamanda Yehova mu msonkhano waukulu.

< Žalmy 26 >