< Žalmy 16 >

1 Zlatý zpěv Davidův. Ostříhej mne, Bože silný, neboť v tebe doufám.
Mikitamu ya Davide. Ndisungeni Inu Mulungu, pakuti ine ndimathawira kwa Inu.
2 Rciž, duše má, Hospodinu: Ty jsi Pán můj, dobrota má nic tobě neprospěje.
Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga; popanda Inu, ine ndilibe chinthu chinanso chabwino.”
3 Ale svatým, kteříž jsou na zemi, a znamenitým, v nichž všecka líbost má.
Kunena za oyera mtima amene ali pa dziko, amenewa ndi olemekezeka, amene ndimakondwera nawo.
4 Rozmnožují bolesti své ti, kteříž k cizímu bohu chvátají; neokusím obětí jejich ze krve, aniž vezmu jména jejich ve rty své.
Anthu amene amathamangira kwa milungu ina mavuto awo adzachulukadi. Ine sindidzathira nawo nsembe zawo zamagazi kapena kutchula mayina awo ndi pakamwa panga.
5 Hospodin jest částka dílu mého a kalicha mého; ty zdržuješ los můj.
Yehova, Inu mwandipatsa cholowa changa ndi chikho changa; mwateteza kolimba gawo langa.
6 Provazcové padli mi na místech veselých, a dědictví rozkošné dostalo se mi.
Malire a malo anga akhala pabwino; ndithudi, ine ndili cholowa chokondweretsa kwambiri.
7 Dobrořečiti budu Hospodinu, kterýž mi radí; nebo i v noci vyučují mne ledví má.
Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu; ngakhale usiku mtima wanga umandilangiza.
8 Představuji Hospodina před oblíčej svůj vždycky, a kdyžť jest mi po pravici, nikoli se nepohnu.
Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse. Popeza Iyeyo ali kudzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.
9 Z té příčiny rozveselilo se srdce mé, a zplésala sláva má, ano i tělo mé v bezpečnosti přebývati bude.
Choncho mtima wanga ndi wosangalala ndipo pakamwa panga pakukondwera; thupi langanso lidzakhala pabwino,
10 Nebo nenecháš duše mé v pekle, aniž dopustíš svatému svému viděti porušení. (Sheol h7585)
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol h7585)
11 Známou učiníš mi cestu života; sytost hojného veselí jest před oblíčejem tvým, a dokonalé utěšení po pravici tvé až na věky.
Inu mwandidziwitsa njira ya moyo; mudzandidzaza ndi chimwemwe pamaso panu, ndidzasangalala mpaka muyaya pa dzanja lanu lamanja.

< Žalmy 16 >