< Žalmy 122 >

1 Píseň stupňů, Davidova. Veselím se z toho, že mi říkáno bývá: Poďme do domu Hospodinova,
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndinakondwera atandiwuza kuti, “Tiyeni ku nyumba ya Yehova.”
2 A že se postavují nohy naše v branách tvých, ó Jeruzaléme.
Mapazi athu akuyima mʼzipata zako, Iwe Yerusalemu.
3 Jižtě Jeruzalém ušlechtile vystaven, a jako v město k sobě vespolek připojen.
Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda umene uli wothithikana pamodzi.
4 Do něhož vstupují pokolení, pokolení Hospodinova, k svědectví Izraelovu, aby oslavovali jméno Hospodinovo.
Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko, mafuko a Yehova, umboni wa kwa Israeli, kuti atamande dzina la Yehova.
5 Nebo tamť jsou postaveny stolice soudu, stolice domu Davidova.
Kumeneko anayikako mipando yaufumu yachiweruzo, mipando yaufumu ya nyumba ya Davide.
6 Žádejtež pokoje Jeruzalému, řkouce: Dějž se pokojně těm, kteříž tě milují.
Pemphererani mtendere wa Yerusalemu: “Iwo amene amakukonda iwe zinthu ziwayendere bwino.
7 Budiž pokoj v předhradí tvém, a upokojení na palácích tvých.
Mukhale mtendere mʼkati mwa makoma ako, ndipo mʼnyumba zako zaufumu mukhale chitetezo.”
8 Pro bratří své a přátely své žádati budu pokoje tobě.
Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga ndidzati, “Mtendere ukhale mʼkati mwako.”
9 Pro dům Hospodina Boha našeho budu tvého dobrého hledati.
Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu, ndidzakufunira zabwino.

< Žalmy 122 >