< Jób 25 >
1 Tedy odpovídaje Bildad Suchský, řekl:
Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
2 Panování a hrůza Boží působí pokoj na výsostech jeho.
“Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
3 Zdaliž jest počet vojskům jeho? A nad kým nevzchází světlo jeho?
Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
4 Jakž by tedy spravedliv býti mohl bídný člověk před Bohem silným, aneb jak čist býti narozený z ženy?
Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
5 Hle, ani měsíc nesvítil by, ani hvězdy nebyly by čisté před očima jeho,
Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
6 Nadto pak smrtelný člověk, jsa jako červ, a syn člověka, jako hmyz.
nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”