< Jób 20 >

1 Odpovídaje pak Zofar Naamatský, řekl:
Pamenepo Zofari wa ku Naama anayankha kuti
2 Z příčiny té myšlení má k odpovídání tobě nutí mne, a to abych rychle učinil,
“Kuvutika kwa mʼmaganizo kwanga kwandifulumiza kuti ndiyankhe chifukwa ndasautsidwa kwambiri.
3 Že kárání k zahanbení svému slyším, pročež duch můj osvícený nutí mne, aťbych odpovídal.
Ndikumva kudzudzula kondinyoza, ndipo kumvetsetsa kwanga kwa zinthu kwandifulumiza kuti ndiyankhe.
4 Zdaž nevíš o tom, že od věků, a jakž postavil Bůh člověka na zemi,
“Ndithudi iwe ukudziwa momwe zinthu zakhala zikuchitikira kuyambira kale, kuchoka nthawi imene munthu analengedwa pa dziko lapansi,
5 Plésání bezbožných krátké jest, a veselí pokrytce jen na chvílku?
kuti chisangalalo cha woyipa nʼchosachedwa kutha, chimwemwe cha wosapembedza Mulungu nʼchakanthawi kochepa.
6 Byť pak vstoupila až k nebi pýcha jeho, a hlava jeho oblaku by se dotkla,
Ngakhale atamayenda mapewa ake ali mmwamba ndipo mutu wake uli nengʼaa,
7 Však jako lejno jeho na věky zahyne. Ti, kteříž jej vídali, řeknou: Kam se poděl?
iye adzatheratu monga momwe imatayikira ndowe yake yomwe; iwo amene ankamuona adzati, ‘Kodi uje uja ali kuti?’
8 Jako sen pomine, aniž ho naleznou; nebo uteče jako vidění noční.
Adzazimirira ngati maloto ndipo sadzapezekanso, adzachotsedwa ngati masomphenya a usiku.
9 Oko, kteréž ho vídalo, již ho nikdy neuzří, aniž více patřiti bude na něj místo jeho.
Diso limene linamuona silidzamuonanso; sadzapezekanso pamalo pake.
10 Synové jeho budou přízně u nuzných hledati, a ruce jeho musejí zase vraceti loupež svou.
Ana ake adzabwezera zonse zimene iyeyo analanda anthu osauka;
11 Kosti jeho naplněny jsou hříchy mladosti jeho, a s ním v prachu lehnou.
Mphamvu zaunyamata zimene zili mʼthupi mwake zidzagona naye limodzi mʼfumbi.
12 A ačkoli zlost sladne v ústech jeho, a chová ji pod jazykem svým;
“Ngakhale zoyipa zili zozuna mʼkamwa mwake ndipo amazibisa kunsi kwa lilime lake,
13 Kochá se v ní, a nepouští jí, ale zdržuje ji u prostřed dásní svých:
ngakhale salola kuzilavula, ndipo amazisunga mʼkamwa mwake,
14 Však pokrm ten ve střevách jeho promění se; bude jako žluč hadů nejlítějších u vnitřnostech jeho.
koma chakudya chake chidzawawasa mʼmimba mwake; chidzasanduka ngati ndulu ya njoka mʼkati mwa iyeyo.
15 Zboží nahltané vyvrátí, z břicha jeho Bůh silný je vyžene.
Adzachisanza chuma chimene anachimeza; Mulungu adzachitulutsa mʼmimba mwa munthuyo.
16 Jed hadů lítých ssáti bude, zabije ho jazyk ještěrčí.
Iye adzayamwa ndulu ya njoka ndipo ululu wa mphiri udzamupha.
17 Neuzří pramenů potoků a řek medu a másla.
Sadzasangalala ndi timitsinje, mitsinje yoyenda uchi ndi mafuta.
18 Navrátí úsilé cizí, a nezažive ho, vedlé nátisku svého rozličného; nebude na ně vesel.
Ayenera kubweza zimene anazigwirira ntchito osazidya; sadzasangalala ndi phindu la malonda ake.
19 Nebo utiskal a opouštěl nuzné, dům zloupil a nestavěl ho.
Pakuti iye anapondereza anthu osauka ndipo anawasiya wopanda thandizo; iyeyo analanda nyumba zimene sanamange.
20 Pročež nesezná nic pokojného v životě svém, aniž které nejrozkošnější své věci bude moci zachovati.
“Chifukwa choti umbombo wake sutha, sadzatha kusunga chilichonse chimene amakondwera nacho.
21 Nic mu nepozůstane z pokrmu jeho, tak že nebude míti, čím by se troštoval.
Palibe chatsala kuti iye adye; chuma chake sichidzachedwa kutha.
22 Byť pak i dovršena byla hojnost jeho, ssoužení míti bude; každá ruka trapiče oboří se na něj.
Ngakhale ndi munthu wachuma, mavuto adzamugwera; mavuto aakulu adzamugwera.
23 By měl čím naplniti břicho své, dopustí na něj Bůh prchlivost hněvu svého, kterouž na něj dštíti bude i na pokrm jeho.
Akadya nʼkukhuta, Mulungu adzamugwetsera ukali wamoto ngati mvula yosalekeza.
24 Když utíkati bude před zbrojí železnou, prostřelí ho lučiště ocelivé.
Ngakhale athawe mkondo wachitsulo, muvi wamkuwa wosongoka udzamulasa.
25 Střela vyňata bude z toulu a vystřelena, nadto meč pronikne žluč jeho; a když odcházeti bude, přikvačí jej hrůzy.
Muviwo adzawutulutsira ku msana, songa yake yowala kuchoka mʼmphafa mwake. Adzagwidwa ndi mantha aakulu;
26 Všeliká neštěstí jsou polečena v skrýších jeho, zžíře jej oheň nerozdmýchaný, zle se povede i pozůstalému v stanu jeho.
mdima wandiweyani ukudikira chuma chake. Moto wopanda wowukoleza udzamupsereza ndi kuwononga zonse zotsala mʼnyumba yake.
27 Odkryjí nebesa nepravost jeho, a země povstane proti němu.
Zamumlengalenga zidzawulula kulakwa kwake; dziko lapansi lidzamuwukira.
28 Rozptýlena bude úroda domu jeho, rozplyne se v den hněvu jeho.
Chigumula cha madzi chidzawononga nyumba yake, katundu wake adzatengedwa pa tsiku la ukali wa Mulungu.
29 Tenť jest podíl člověka bezbožného od Boha, to, pravím, dědictví vyrčené jemu od Boha silného.
Izi ndi zimene Mulungu amasungira anthu oyipa, mphotho imene Mulungu amayikira iwowo.”

< Jób 20 >