< Izaiáš 50 >

1 Takto praví Hospodin: Kdež jest lístek zapuzení matky vaší, kterýmž jsem ji propustil? Aneb kdo jest z věřitelů mých, jemuž jsem vás prodal? Aj, nepravostmi svými prodali jste sebe, a pro převrácenosti vaše propuštěna jest matka vaše.
Yehova akuti, “Kalata imene ndinasudzulira amayi anu ili kuti? Kapena mwa anthu amene ndili nawo ngongole, ndinakugulitsani kwa ati? Inu munagulitsidwa ku ukapolo chifukwa cha machimo anu; amayi anu anachotsedwa chifukwa cha kulakwa kwanu.
2 Proč, když přicházím, není žádného, když volám, žádný se neozývá? Zdaliž jest naprosto ukrácena ruka má, aby nemohla vykoupiti? A žádné-liž není ve mně moci k vysvobození? Aj, žehráním svým vysušuji moře, obracím řeky v poušť, až se smrazují ryby jejich, proto že nebývá vody, a mrou žízní.
Nʼchifukwa chiyani pamene ndinabwera kudzakupulumutsani panalibe munthu? Pamene ndinayitana, nʼchifukwa chiyani panalibe wondiyankha? Kodi dzanja langa ndi lalifupi kuti nʼkulephera kukuwombolani? Kodi ndilibe mphamvu zokupulumutsirani? Ndi kudzudzula kokha ndinawumitsa nyanja yayikulu, mitsinje ndinayisandutsa chipululu; nsomba za mʼmenemo zinawola chifukwa chosowa madzi; ndipo zinafa ndi ludzu.
3 Obláčím nebesa v smutek, a žíni dávám jim za oděv.
Ndinaphimba thambo ndi mdima ndipo chiguduli chinakhala chofunda chake.”
4 Panovník Hospodin dal mi jazyk umělý, abych uměl příhodně ustalému mluviti slova. Probuzuje každého jitra, probuzuje mi uši, abych slyšel, tak jako pilně se učící.
Ambuye Yehova anandiphunzitsa mawu oyenera kuyankhula kudziwa mawu olimbitsa mtima anthu ofowoka. Mmawa mulimonse amandidzutsa, amathwetsa khutu langa kuti ndimve monga amachitira munthu amene akuphunzira.
5 Panovník Hospodin otvírá mi uši, a já se nepostavuji zpurně, aniž se nazpět odvracím.
Ambuye Yehova wanditsekula makutu anga, ndipo sindinakhale munthu wowukira ndipo sindinabwerere mʼmbuyo.
6 Těla svého nastavuji bijícím, a líce svého rvoucím mne, tváři své neskrývám od pohanění a plvání.
Ndinapereka msana wanga kwa ondimenya masaya anga ndinawapereka kwa anthu ondizula ndevu; sindinawabisire nkhope yanga anthu ondinyoza ndi ondilavulira.
7 Nebo Panovník Hospodin spomáhá mi, pročež nebývám zahanben. Pro touž příčinu nastavuji tváři své jako škřemene; nebo vím, že nebudu zahanben.
Popeza Ambuye Yehova amandithandiza, sindidzachita manyazi. Tsono ndalimba mtima ngati msangalabwi, chifukwa ndikudziwa kuti sindidzachita manyazi.
8 Blízkoť jest ten, kterýž mne ospravedlňuje. Kdož se nesnadniti bude se mnou? Postavme se spolu; kdo jest odpůrce můj, nechť přistoupí ke mně.
Wondikhalira kumbuyo ali pafupi, ndaninso amene adzandiyimba mlandu? Abwere kuti tionane maso ndi maso! Mdani wanga ndi ndani? Abweretu kuti tilimbane!
9 Aj, Panovník Hospodin spomáhati mi bude. Kdož jest, ješto by mne potupil? Aj, všickni takoví jako roucho zvetšejí, mol sžíře je.
Ambuye Yehova ndiye amene amandithandiza. Ndaninso amene adzanditsutsa? Onse adzatha ngati chovala chodyedwa ndi njenjete.
10 Kdo jest mezi vámi, ješto se bojí Hospodina, poslouchej hlasu služebníka jeho. Kdo jest, ješto chodí v temnostech, a nemá žádného světla, doufej ve jméno Hospodinovo, a zpolehni na Boha svého.
Ndani mwa inu amaopa Yehova ndi kumvera mawu a mtumiki wake? Aliyense woyenda mu mdima, popanda chomuwunikira, iye akhulupirire dzina la Yehova ndi kudalira Mulungu wake.
11 Aj, vy všickni, kteříž zaněcujete oheň, a jiskrami se přepasujete, choďtež v blesku ohně svého, a v jiskrách, kteréž jste roznítili. Od ruky mé toto se vám stane, že v bolesti ležeti budete.
Koma tsopano inu nonse amene mumasonkha moto ndi kuyatsa sakali za moto kufuna kuwononga anzanu, lowani mʼmoto wanu womwewo. Pitani mu sakali za moto zimene mwayatsa. Ndipo ine Yehova ndiye amene ndidzakugwetsereni mazunzowo.

< Izaiáš 50 >