< 1 Kronická 25 >

1 I oddělil David a knížata vojska k službě syny Azafovy a Hémanovy a Jedutunovy, kteříž by prorokovali při harfách, při loutnách a při cimbálích. Byl pak počet jejich, totiž mužů těch, jenž práci vedli v přisluhování svém,
Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
2 Z synů Azafových: Zakur, Jozef, Netaniáš a Asarela, synové Azafovi, pod spravou Azafavou byli, kterýž prorokoval k rozkazu královu.
Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
3 Z Jedutuna synů Jedutunových bylo šest: Godoliáš, Zeri, Izaiáš, Chasabiáš, Mattitiáš a Simei, pod spravou otce jejich Jedutuna, kterýž prorokoval při harfě k slavení a chválení Hospodina.
Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
4 Z Hémana synové Hémanovi: Bukkiáš, Mataniáš, Uziel, Sebuel, Jerimot, Chananiáš, Chanani, Eliata, Giddalti, Romantiezer, Jazbekasa, Malloti, Hotir a Machaziot.
Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
5 Všickni ti synové Hémanovi, proroka králova v slovích Božských, k vyvyšování moci. A dal Bůh Hémanovi synů čtrnácte a dcery tři.
Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
6 Všickni ti byli pod spravou otce svého, při zpívání v domě Hospodinově na cymbálích, loutnách a harfách, k službě v domě Božím vedlé poručení králova Azafovi, Jedutunovi a Hémanovi.
Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
7 Byl pak počet jich s bratřími jejich, těmi, kteříž byli vycvičení v zpěvích Hospodinových, všech mistrů dvě stě osmdesát osm.
Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
8 Tedy metali losy, houf držících stráž naproti druhému, jakž malý, tak veliký, mistr i učedlník.
Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
9 I padl první los v čeledi Azaf na Jozefa, na Godoliáše s bratřími a syny jeho druhý, jichž bylo dvanáct.
Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
10 Třetí na Zakura, synům jeho a bratřím jeho dvanácti.
Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
11 Ètvrtý na Izara, synům jeho a bratřím jeho dvanácti.
Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
12 Pátý na Netaniáše, synům jeho a bratřím jeho dvanácti.
Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
13 Šestý na Bukkiáše, synům jeho a bratřím jeho dvanácti.
Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
14 Sedmý na Jesarele, synům jeho a bratřím jeho dvanácti.
Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
15 Osmý na Izaiáše, synům jeho a bratřím jeho dvanácti.
Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
16 Devátý na Mataniáše, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
17 Desátý na Simei, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
18 Jedenáctý na Azarele, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
19 Dvanáctý na Chasabiáše, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
20 Třináctý na Subaele, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
21 Ètrnáctý na Mattitiáše, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
22 Patnáctý na Jerimota, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
23 Šestnáctý na Chananiáše, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
24 Sedmnáctý na Jazbekasa, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
25 Osmnáctý na Chanani, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
26 Devatenáctý na Malloti, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
27 Dvadcátý na Eliatu, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
28 Jedenmecítmý na Hotira, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
29 Dvamecítmý na Giddalta, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
30 Třímecítmý na Machaziota, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
31 Ètyřmecítmý na Romantiezera, synům a bratřím jeho dvanácti.
Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.

< 1 Kronická 25 >