< Žalmy 100 >

1 Žalm k díků činění. Prokřikuj Hospodinu všecka země.
Salimo. Nyimbo yothokoza. Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
2 Služte Hospodinu s veselím, předstupte před oblíčej jeho s prozpěvováním.
Mulambireni Yehova mosangalala; bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
3 Vězte, že Hospodin jest Bůh; on učinil nás, a ne my sami sebe, abychom byli lid jeho, a ovce pastvy jeho.
Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu. Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake; ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
4 Vcházejte do bran jeho s díkčiněním, a do síní jeho s chvalami; oslavujte jej, a dobrořečte jménu jeho.
Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko ndi ku mabwalo ake ndi matamando; muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
5 Nebo dobrý jest Hospodin, na věky milosrdenství jeho, a od národu až do pronárodu pravda jeho.
Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya; kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.

< Žalmy 100 >