< Príslovia 12 >

1 Kdo miluje cvičení, miluje umění; kdož pak nenávidí domlouvání, nemoudrý jest.
Munthu amene amakonda mwambo amakonda kudziwa zinthu, koma amene amadana ndi chidzudzulo ndi wopusa.
2 Dobrý nalézá lásku u Hospodina, ale muže nešlechetného potupí Bůh.
Munthu wabwino amapeza kuyanja pamaso pa Yehova, koma Yehova amatsutsa munthu wochita chinyengo.
3 Nebývá trvánlivý člověk v bezbožnosti, kořen pak spravedlivých nepohne se.
Munthu sangakhazikike bwino pochita zoyipa, koma maziko a anthu olungama sadzatekeseka.
4 Žena statečná jest koruna muže svého, ale jako hnis v kostech jeho ta, kteráž k hanbě přivodí.
Mkazi wakhalidwe labwino ali ngati chipewa chaufumu kwa mwamuna wake, koma mkazi wochititsa manyazi ali ngati chilonda cha mafinya kwa mwamuna wake.
5 Myšlení spravedlivých jsou pravá, rady pak bezbožných lstivé.
Maganizo a anthu olungama ndi owongoka, koma malangizo a anthu oyipa ndi achinyengo.
6 Slova bezbožných úklady činí krvi, ústa pak spravedlivých vytrhují je.
Mawu a anthu oyipa ndi ophetsa, koma mawu a anthu olungama amapulumutsa.
7 Vyvráceni bývají bezbožní tak, aby jich nebylo, ale dům spravedlivých ostojí.
Anthu oyipa amagonjetsedwa ndipo amayiwalika, koma nyumba ya anthu olungama idzakhalabe.
8 Podlé toho, jakž rozumný jest, chválen bývá muž, převráceného pak srdce bude v pohrdání.
Munthu amatamandidwa malinga ndi nzeru zake, koma anthu amitima yokhota amanyozedwa.
9 Lepší jest nevzácný, kterýž má služebníka, nežli ten, kterýž sobě slavně počíná, a nemá chleba.
Nʼkwabwino kukhala munthu wonyozeka koma wodzigwirira ntchito nʼkukhala ndi zonse zofunika, kuposa kukhala wodzikuza koma ulibe ndi chakudya chomwe.
10 Pečuje spravedlivý o život hovádka svého, srdce pak bezbožných ukrutné jest.
Munthu wolungama amasamalira moyo wa ziweto zake, koma chifundo cha munthu woyipa ndi chakhanza.
11 Kdo dělá zemi svou, nasycen bývá chlebem; ale kdož následuje zahalečů, blázen jest.
Wolima mʼmunda mwake mwakhama adzakhala ndi chakudya chochuluka, koma wotsata zopanda pake alibe nzeru.
12 Žádostiv jest bezbožný obrany proti zlému, ale kořen spravedlivých způsobuje ji.
Munthu woyipa amalakalaka zofunkha za anthu oyipa, koma mizu ya anthu olungama imabereka zipatso.
13 Do přestoupení rtů zapletá se zlostník, ale spravedlivý vychází z ssoužení.
Munthu woyipa amakodwa mu msampha wa mayankhulidwe ake oyipa; koma munthu wolungama amatuluka mʼmavuto.
14 Z ovoce úst každý nasycen bude dobrým, a odplatu za skutky člověka dá jemu Bůh.
Munthu amakhala ndi zabwino zambiri chifukwa cha mawu ake ndipo ntchito zimene munthu agwira ndi manja ake zimamupindulira.
15 Cesta blázna přímá se zdá jemu, ale kdo poslouchá rady, moudrý jest.
Zochita za chitsiru mwini wakeyo amaziona ngati zabwino, koma munthu wanzeru amamvera malangizo.
16 Hněv blázna v tentýž den poznán bývá, ale opatrný hanbu skrývá.
Mkwiyo wa chitsiru umadziwika nthawi yomweyo, koma munthu wanzeru sasamala kunyozedwa.
17 Kdož mluví pravdu, ohlašuje spravedlnost, svědek pak falešný lest.
Woyankhula zoona amapereka umboni woona, koma mboni yabodza imafotokoza zonama.
18 Někdo vynáší řeči podobné meči probodujícímu, ale jazyk moudrých jest lékařství.
Munthu woyankhula mosasamala mawu ake amalasa ngati lupanga, koma mawu a munthu wanzeru amachiritsa.
19 Rtové pravdomluvní utvrzeni budou na věky, ale na kratičko jazyk lživý.
Mawu woona amakhala mpaka muyaya koma mawu abodza sakhalitsa.
20 V srdci těch, kteříž zlé obmýšlejí, bývá lest, v těch pak, kteříž radí ku pokoji, veselí.
Mʼmitima ya anthu amene amakonza zoyipa muli chinyengo; koma anthu olimbikitsa za mtendere amakhala ndi chimwemwe.
21 Nepotká spravedlivého žádná těžkost, bezbožní pak naplněni budou zlým.
Palibe choyipa chimene chimagwera munthu wolungama, koma munthu woyipa mavuto samuthera.
22 Ohavností jsou Hospodinu rtové lživí, ale ti, jenž činí pravdu, líbí se jemu.
Pakamwa pa bodza pamamunyansa Yehova, koma amakondwera ndi anthu oyankhula zoona.
23 Člověk opatrný tají umění, ale srdce bláznů vyvolává bláznovství.
Munthu wochenjera amabisa nzeru zake, koma munthu wopusa amaonetsa uchitsiru wake poyera.
24 Ruka pracovitých panovati bude, lstivá pak musí dávati plat.
Ogwira ntchito mwakhama adzalamulira, koma aulesi adzakhala ngati kapolo.
25 Starost v srdci člověka snižuje ji, ale věc dobrá obveseluje ji.
Nkhawa imakhala ngati katundu wolemera mu mtima mwa munthu, koma mawu abwino amamusangalatsa.
26 Vzácnější jest nad bližního svého spravedlivý, cesta pak bezbožných svodí je.
Munthu wolungama amatsogolera mnansi wake, koma ntchito za anthu oyipa zimawasocheretsa.
27 Nebude péci fortelný, což ulovil, ale člověk bedlivý statku drahého nabude.
Munthu waulesi sapeza chimene akufuna, koma munthu wakhama amapeza chuma chamtengo wapatali.
28 Na stezce spravedlnosti jest život, a cesta stezky její nesmrtelná jest.
Mʼnjira yachilungamo muli moyo; koma njira ya munthu woyipa imafikitsa ku imfa.

< Príslovia 12 >